12/06/2025
YESAYA 60:22
22Wamng'ono adzasanduka cikwi, ndi wocepa adzasanduka mtundu wamphamvu; Ine Yehova ndidzafulumiza ici m'nthawi yace.
OKONDEDWA IKAKHALA NTHAWI YA KUMWAMBA NGAKHALE ZITACHEDWA KOMA ZIKAFIKA SUPANGA REGRET. VUTO PHUMA, CHANGU INUYO, KAYA MUKUTHAMANGILA KUTI?
*AMBUYE ATITHANDIZE KUDIKILA PA IYE*