02/04/2026
*TAWAUZAN ADANI ANUWO KT ZOMWE MUKUNENA ZOKHUDZA INEYO SIZITHEKA AKUTERO YEHOVA ππ½πͺπ½πͺπ½*
Yesaya : 7 : 4-74. Ukamuwuze k*ti, βChenjera, khala phee ndipo usaope. Usataye mtima chifukwa cha zitsa ziwiri zomwe zikufuka, chifukwa cha ukali woopsa wa Rezini ndi Siriya, ndiponso wa Peka mwana wa Remaliya.7. Komabe zimene akunena Ambuye Yehova ndi izi: β βZimenezo sizidzatheka, sizidzachitika konse,
*Hallelujah ππ½ππ½ππ½ππ½ππ½ππ½!!Munauzidwapo inu kt musavutike ai mawa simufika,kmaso iiiii!!! Akt atan akapambana andifuse ndye munthu wake siineyo ai,Apita ku ma interview!? Akabwererako palibe comwe angakapange,Kd inu or anawo angakhale ndi amene aja Hehehede iri π,Mwava kd ati apeza mamunatu likakhala banja mudzandifuse,!!Iyi imakhala nyengo omwe adan afika polepheretsa ciriconse cako ndipo bas iweyo kukhala pa zero,Indeee azibale anga akt or Naye Ahazi inafika nthaw iyi,omwe Yerusalemu anazunguliridwa kt athiridwe nkhondo,Kma Yesaya ndk*t pa nthaw iyi atapangidwa kukhala m'neneri ndipo ak*tumidwa kupita kukakumana ndi Ahazi,ndkukamuuza zomwe Yehova akunena zokhudza adan ake,Abale anga tisadere nkhawa ai,tisaope ai,tisagwedezeke ai,auzen anebawo kt Mulungu akt zomwe mukuganizazo zokhudza ine sizitheka ai ndipo Yesaya 54:16,17,Kmaso Eksodo 14:14,Eksodo 15:3,Wauza ine lero ndipo adani anga sandipambana ai ππ½ππ½ππ½ππ½ππ½ππ½πͺπ½πͺπ½πͺπ½πͺπ½*