Hermanus Grace Of God Living Church GGLC

Hermanus Grace Of God Living Church GGLC The Grace of God Living Church has a defining focus on legalism.

The Grace of God Living Church believes that they are the β€œtrue Church of God that stands apart from this religious Babylon,” meaning all other Christian denominations.

02/04/2026

*TAWAUZAN ADANI ANUWO KT ZOMWE MUKUNENA ZOKHUDZA INEYO SIZITHEKA AKUTERO YEHOVA πŸ™πŸ½πŸ’ͺ🏽πŸ’ͺ🏽*
Yesaya : 7 : 4-74. Ukamuwuze k*ti, β€˜Chenjera, khala phee ndipo usaope. Usataye mtima chifukwa cha zitsa ziwiri zomwe zikufuka, chifukwa cha ukali woopsa wa Rezini ndi Siriya, ndiponso wa Peka mwana wa Remaliya.7. Komabe zimene akunena Ambuye Yehova ndi izi: β€œ β€˜Zimenezo sizidzatheka, sizidzachitika konse,
*Hallelujah πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½!!Munauzidwapo inu kt musavutike ai mawa simufika,kmaso iiiii!!! Akt atan akapambana andifuse ndye munthu wake siineyo ai,Apita ku ma interview!? Akabwererako palibe comwe angakapange,Kd inu or anawo angakhale ndi amene aja Hehehede iri πŸ˜‚,Mwava kd ati apeza mamunatu likakhala banja mudzandifuse,!!Iyi imakhala nyengo omwe adan afika polepheretsa ciriconse cako ndipo bas iweyo kukhala pa zero,Indeee azibale anga akt or Naye Ahazi inafika nthaw iyi,omwe Yerusalemu anazunguliridwa kt athiridwe nkhondo,Kma Yesaya ndk*t pa nthaw iyi atapangidwa kukhala m'neneri ndipo ak*tumidwa kupita kukakumana ndi Ahazi,ndkukamuuza zomwe Yehova akunena zokhudza adan ake,Abale anga tisadere nkhawa ai,tisaope ai,tisagwedezeke ai,auzen anebawo kt Mulungu akt zomwe mukuganizazo zokhudza ine sizitheka ai ndipo Yesaya 54:16,17,Kmaso Eksodo 14:14,Eksodo 15:3,Wauza ine lero ndipo adani anga sandipambana ai πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ’ͺ🏽πŸ’ͺ🏽πŸ’ͺ🏽πŸ’ͺ🏽*

02/04/2026

*TIYENI TIGWIRITSITSENI CABWINONO-CO OR ENA ANENE ZOIPA ZA ICO πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*
Romans : 14 : 16-17.Musalole k*ti chimene muchiyesa chabwino achinene ngati choyipa.17. Pak*ti Ufumu wa Mulungu si nkhani yakudya ndi kumwa, koma chilungamo, mtendere ndi chimwemwe mwa Mzimu Woyera.
*Hallelujah πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½!!Tiripo ena masiku ano tinasiya kupemphera cifukwa ca maganizo a anthu ena,Ena analipo otiuza kt aaaaa!! Kd inuso ku church kwa daily daily muzikataniko,or Bible limat muzipita daily,Ndipo izi tinazivera ndkusiya kupita ku church daily,Masalimo 122:1,Davide anat anasangalala atati tiye ku nyumba a Atate,Kmaso Davide emweyi pa Masalimo 37:10 Anat cinthu cinodzi comwe ndicikonda ndico kupezeka nyumba a Atate,Tiripo ena amene timakakamizidwa kunena bodza pakt ena akt titero,Mukawerenga Numeri 22:18Nkhan a Baalamu ndi Balaki, Akt Baalamu anati or atandipasa nyumba odzaza ndi golide kmaso silva kma sindingacite ciriconse cacikulu or cacing'ono kuposa comwe Mulungu wanena,Indeee azibale anga tiyen tigwiritsitsen cilungamo nthaw zonse ndipo tikatero or enewa adzasowa mpata oticitira coipa or k*tineneza bodza πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½*

02/04/2026

*KD INUYO MISSION ANU NDIOTAN πŸ€·πŸ½β€β™‚οΈπŸ€·πŸ½β€β™‚οΈπŸ€·πŸ½β€β™‚οΈ*
Mateyu 20:28 CCL
[28] Momwenso Mwana wa Munthu sanabwere kudzatumikiridwa, koma kudzatumikira, ndi kupereka moyo wake kukhala dipo la anthu ambiri.”
*Hallelujah πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½!!Aliyese akamapanga zinthu amakhala ndi colinga,ndipo amayesetsa kt colinga cakeco citheke,Citsanzo ndiri ku South Africa,colinga canga ndkt ndipeze ndalama a business kmaso ndimange nyumba,ena ali kuno kt adzamwe mowa kmaso kukwatira akaz akuno,ena agule galimoto kt akapangire business, enaso anabwera kudzangoonako south africa,Kd nanga inuyo mission anu a umzimu ndiotan!? Ambiri masiku ano akusangalala akamat Atsogoleri, Abusa,Abishop or atumiki kma or ziri conco iwowo mission ao akungofuna kukwaniritsa lemba la Mateyu 23 Lija,ndipo colinga cao ndkupeza phindu mu mΚΌdzina la Ubusa kapena Atsogoleri, enaso akufuna apeze ulemu ndkulambiridwa momo,Yesu Khristu akt sindinabwere pano kudzatumikiridwa kma kudzatumikira,Pamene inuyo pakt akt ndinu abusa mukufuna k*tumikiridwa,Ai,Pa Mateyu 28,Yesu Khristu anakupasan ntchito,ntchito ake ndiyo kukalalikira za uthenga wabwino ndkuwabatiza anthu mu mdzina la Atate,Mwana ndi Mzimu,Kd inuyo mission anu ndiotan!? Indeee tikhale osamala pakt tikacita cibwana paja si onse amene amat Ambuye Ambuye akalowe mu umfumu wakumwamba Mateyu 7:21 πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*

😭😭😭😭😭😭😭😭okondedwa pano tili pa deport tikudikira bus Kuti tikwere, ndiye ofunika nthawi zonse tizikhala okonzeka , Lero ...
20/10/2025

😭😭😭😭😭😭😭😭
okondedwa pano tili pa deport tikudikira bus Kuti tikwere, ndiye ofunika nthawi zonse tizikhala okonzeka ,
Lero mmawa ndakandira uthenga Kuti mayi Happiness dauka Phiri amwalira ndipo ndidagwidaa ndi chisoni chifukwa lachitatu lomwelo ndayankhula nawo timakambiran Za Ku church , Ku ndilande .
Mudwala atinayamba dZana usiku mkumwalira , Tiyeni tiziyemda okonzeka ,
Mayi happiness dauka akukira Ku ndilande Koma kumudzi kwawo nsiku chiladzulo , Moti maliro pano Ali Ku chiladzulo, Mayi dauka adaki mlembi WA amayi ampingo wathu Ku Malawi, sitizaiwla ZABWINO amachita, ndipo magwira ntchito Ngati yolipidwa anaki ndi changu Koma tathedwa nzeru.
R I P

20/09/2025

Aroma : 13 :10-11
10. Chikondi sichichitira mnzake zoyipa. Chifukwa chake chikondi ndicho chokwaniritsa lamulo.11. Ndipo chitani ichi pozindikira nthawi ino. Nthawi yafika yoti inu mudzuke k*tulo, chifukwa chipulumutso chathu chili pafupi tsopano kuposa pamene tinayamba kukhulupirira.
*Hallelujah πŸ™ŒπŸ™ŒπŸ™πŸ™!!Mwadzuka bwanji acimwene!? Wina akt iwe wapenga kodi !? Ukat ndadzuka bwino nthaw zino,Indeee tulo iti situlo mukuganizato ai,kma tulo iti ndi tulo tocita zoipa,monga kaya mukupembedza ziwanda,uhule,kuba,kupha miseche mudziwe kt mukugona,ndipo mukuyenera kudzuka,Paulo anat dzuka wamtulo iwe,wakufa iwe ndipo Yesu Khristu adzakuwalira Aefeso 5:14,Indeee tiyen tidzuken pakucita zabwino,Tikatero tidzakhala odzuka mwakucita ntchito zabwino zomwe zimatanthauza kusagona mu umzimu πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*

15/09/2025

*CHIPULUMUTSO NDI WEKHA πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*
Genesis : 19 :26-27
26. Koma mkazi wa Loti anachewuka ndipo anasanduka mwala wa mchere.27. Mmawa mwake, Abrahamu ananyamuka nabwerera kumalo kumene anakumana ndi Yehova kuja.
*Hallelujah πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½!!Anthu ambiri masiku ano sitipemphera cifukwa cakt abambo anga ndi abusa,aprophet,bishop kmaso wansembe,ndipo timadziva ngat cipulumutso cafika cake,Ai ndipo ai si conco ndi mkaz wake anatuluka limodzi munzinda muja,ndipo onse ndkumapita malo opulumukirapo,kma mkaz wa Loti pakusavera kwake,anaceuka ndipo pompo anasanduka culu ca mchere,Ndipo taonan Loti akt tsiku lotsatira lake akupita pamalo amene anakuma ndi Mulungu akukaona zomwe zacitikira nzinda uja,Kd nthaw iyi mkaz wake alkt!? Indee ndye kt wasanduka mwala wamchere(chulu) Azibale anga cipulumutso ndi wekha,titha kupemphererana pa matenda,ntchito,nyengo kma kt munthu upulumuke ku mkwiyo wa Yehova zimafunika iweyo mwini utengepo step wekha πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*

15/09/2025
13/09/2025

*UTHENGA UWU UPITE KWA ONSE AMENE MASIKU ANO AKT NDI ABISHOP,ABUSA,APROPHET,CONSECO MUKUGWIRITSA NTCHITO ZIWANDA,MAFANO KMASO CIPANGIZO CIRICONSE CA SATANA*
2 Atesalonika : 2 :10-10
10. Iye adzagwiritsa ntchito mtundu uliwonse wachinyengo kupusitsa amene akuwonongeka. Iwo akuwonongeka chifukwa akukana kukonda choonadi ndi k*ti apulumutsidwe.
*Hallelujah πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½!!Condivetsa cison kwambiri ineyo ndicakt amene akuonongedwa ndi misampha a satanayi ndi azibusa,mabishop,kmaso awa akt mazi prophet-wa,Iwowa akukwaniritsa lemba la Mateyu 23,Kufuna maina abwino,ulemu kmaso dyera pandalama,ndipo iwowa ataya coonadi ndkukaniratu cipulumutso akupembedza mafano,ziwanda kmaso akugwiritsa ntchito cina ciriconse bola iwowo atchuke,alemele,kmaso apasidwe ulemu,zovetsa cison,ICHI NDICIFUKWA CHAKE NDIMAT CONDEE AZIBALE ANGA TIYEN TIPEMPHEN MZIMU WACHIDZIWITSO KT TINGAONONGEDWE NAO LIMODZI ANTHU AWA AMENE AKUONONGEKA NDI SATANA PANOPOWA πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*

13/09/2025

2 Akorinto : 11 :13-14
13. Pak*ti anthu oterewa ndi atumwi onama, antchito achinyengo, odzizimbayitsa ngati atumwi a Khristu.14. Sizododometsa zimenezi, pak*ti Satana mwini amadzizimbayitsa kuoneka ngati mngelo wowunikira anthu.
*Hallelujah πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½!!Tiri masiku otsiliza amene panopo mwa anthu 100 ndi anthu mwina awiri or atatu amene akupempha mu mchoonadi,masiku ano ambiriwa ndi satana weni weni ndipo or k*t muve uthenga wao zosiyana k*tali tali ndi Baibulo,Kmatu izi ndimphavu a satana kufuna kunyenga ambiri,inu anthu pano kupemphera kwafika pa business,kwafika pa ndale,aliyese akufuna kt mpingo wake udzaze,Indeee Yesu anat tipemphe mwini munda kt atipase antchito ena,Kma Kuno ku Hermanus ma church ali paliponse,and kt muone muona kt church cina anthu 8,mwina 7,mwina 15 akakhala ambiri zedi mwina 30,Izizi zikukwaniritsa malemba kt ndi masiku otsizadi ndithu aliyese akufuna k*tchuka ndi ndalama,Bwanji osapanga mpingo umodzi ngat mukupemphera mu mchoonadi!?? ndipo satana akugwiritsa ntchito azitsogoleri athuwa kukhala ngat opemphera pamene ai ndthu,satana wangosintha kukhala ngat m'ngero,tisamale awawa si azitumiki a Yesu Khristu ai,tiyen once again tipemphe mzimu wa cidziwitso azibale anga πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½*

Women's giude chididi msanjeβ™₯️β™₯️β™₯️β™₯️β™₯️
11/09/2025

Women's giude chididi msanjeβ™₯️β™₯️β™₯️β™₯️β™₯️

In Malawi, the "Grace of God Living Church" is connected to an orphanage and various community projects, including educa...
09/09/2025

In Malawi, the "Grace of God Living Church" is connected to an orphanage and various community projects, including education, especially for orphans
Key details about the church's activities in Malawi:
β€’ Orphanage: The organization established the Grace of God Orphanage in BLANTYRE,CHIKWAWA,MSANJE, MULANJE,SALIMA,NTCHISI,TYCHOLO, LILONGWE . In recent years, it has focused on providing education and healthcare for vulnerable children who live with relatives, in compliance with a government directive.
β€’ Community development: News posts on its pages describe ongoing projects, such as building a multipurpose hall to be used as a chapel and a school for orphans.
β€’ Leadership and ministry: from pages associated with the church identify leaders such as Bishop Japhet Lufani and Pastor Derick Mauwa.

β€’ Social media presence: The church has a page and group that provide updates on its activities and mission in Malawi.

Address

LANDLERA Street
Hermanus
7200

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Hermanus Grace Of God Living Church GGLC posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Place Of Worship

Send a message to Hermanus Grace Of God Living Church GGLC:

Share