The Grace of God church

The Grace of God church Receive updates of how the radical love of Jesus is changing peoples lives and setting them on fire

24/12/2025

Tisataye Yesu wathu pa nthawi ya zisangalalo iyi

😭😭😭😭😭😭😭😭okondedwa pano tili pa deport tikudikira bus Kuti tikwere, ndiye ofunika nthawi zonse tizikhala okonzeka , Lero ...
20/10/2025

😭😭😭😭😭😭😭😭
okondedwa pano tili pa deport tikudikira bus Kuti tikwere, ndiye ofunika nthawi zonse tizikhala okonzeka ,
Lero mmawa ndakandira uthenga Kuti mayi Happiness dauka Phiri amwalira ndipo ndidagwidaa ndi chisoni chifukwa lachitatu lomwelo ndayankhula nawo timakambiran Za Ku church , Ku ndilande .
Mudwala atinayamba dZana usiku mkumwalira , Tiyeni tiziyemda okonzeka ,
Mayi happiness dauka akukira Ku ndilande Koma kumudzi kwawo nsiku chiladzulo , Moti maliro pano Ali Ku chiladzulo, Mayi dauka adaki mlembi WA amayi ampingo wathu Ku Malawi, sitizaiwla ZABWINO amachita, ndipo magwira ntchito Ngati yolipidwa anaki ndi changu Koma tathedwa nzeru.
R I P

20/09/2025

Aroma : 13 :10-11
10. Chikondi sichichitira mnzake zoyipa. Chifukwa chake chikondi ndicho chokwaniritsa lamulo.11. Ndipo chitani ichi pozindikira nthawi ino. Nthawi yafika yoti inu mudzuke k*tulo, chifukwa chipulumutso chathu chili pafupi tsopano kuposa pamene tinayamba kukhulupirira.
*Hallelujah πŸ™ŒπŸ™ŒπŸ™πŸ™!!Mwadzuka bwanji acimwene!? Wina akt iwe wapenga kodi !? Ukat ndadzuka bwino nthaw zino,Indeee tulo iti situlo mukuganizato ai,kma tulo iti ndi tulo tocita zoipa,monga kaya mukupembedza ziwanda,uhule,kuba,kupha miseche mudziwe kt mukugona,ndipo mukuyenera kudzuka,Paulo anat dzuka wamtulo iwe,wakufa iwe ndipo Yesu Khristu adzakuwalira Aefeso 5:14,Indeee tiyen tidzuken pakucita zabwino,Tikatero tidzakhala odzuka mwakucita ntchito zabwino zomwe zimatanthauza kusagona mu umzimu πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*

16/09/2025

*TIPEMPHERE*

Oyamba ndi otsiliza ndinu YEHOVA MULUNGU wathu wamoyo, tikudza ogonja ndimodzichepetsa pamaso panu podziwa k*ti osamala ndi k*teteza ndinu

Mudzina lamphamvu lamwana wanu YESU KHRISTU wamoyo, ulemu ndimatamando zipite kwa lye AMBUYE chifukwa chotisamalira ndik*tipyoletsa kumisampha yonse yaoyipayo muwusikuwu wathau mpaka mwatidzutsa ndimoyo mosawerengera zofooka zathu

Kotero ife ana anu pakudziwa k*ti mwini mphamvu zonse ndinu tikupempha ndikuyitanira kwa lnu mutsiku ili, k*ti mutitetezere kumaplani onse awoyipayo amene wakonza paife pamodzi ndi ziwanda zake.

AMBUYE YESU ife ana anu tapempha k*thokoza ndikuyitanira kwa lnu mfumu yamafumu, Ameen

*CHIPULUMUTSO NDI WEKHA πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½* Genesis : 19 :26-27 26. Koma mkazi wa Loti anachewuka ndipo anasanduka mwala wa mchere...
15/09/2025

*CHIPULUMUTSO NDI WEKHA πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*
Genesis : 19 :26-27
26. Koma mkazi wa Loti anachewuka ndipo anasanduka mwala wa mchere.27. Mmawa mwake, Abrahamu ananyamuka nabwerera kumalo kumene anakumana ndi Yehova kuja.
*Hallelujah πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½!!Anthu ambiri masiku ano sitipemphera cifukwa cakt abambo anga ndi abusa,aprophet,bishop kmaso wansembe,ndipo timadziva ngat cipulumutso cafika cake,Ai ndipo ai si conco ndi mkaz wake anatuluka limodzi munzinda muja,ndipo onse ndkumapita malo opulumukirapo,kma mkaz wa Loti pakusavera kwake,anaceuka ndipo pompo anasanduka culu ca mchere,Ndipo taonan Loti akt tsiku lotsatira lake akupita pamalo amene anakuma ndi Mulungu akukaona zomwe zacitikira nzinda uja,Kd nthaw iyi mkaz wake alkt!? Indee ndye kt wasanduka mwala wamchere(chulu) Azibale anga cipulumutso ndi wekha,titha kupemphererana pa matenda,ntchito,nyengo kma kt munthu upulumuke ku mkwiyo wa Yehova zimafunika iweyo mwini utengepo step wekha πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*

13/09/2025

*PALIBE LEMBA NDI LIMODZI LOMWE,LOMWE LIDZAPITE PACHABE πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ’ͺ🏽πŸ’ͺ🏽πŸ’ͺ🏽*

Machitidwe : 4 :19-20
19. Koma Petro ndi Yohane anayankha k*ti, β€œWeruzani nokha ngati nΚΌkwabwino pamaso pa Mulungu kumvera inu koposa Mulungu.20. Ife sitingaleke kuyankhula za zimene tinaziona ndi kuzimva.”
*Hallelujah πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ‘‹πŸ½πŸ‘‹πŸ½πŸ‘‹πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½!!Kd mumagwiritsa ntchito malemba popanga zinthu zanu!? Ngat ndi conco ndkukuuzan kt indee mudzapambana πŸ’ͺ🏽,Petro ndi Yohane akuimbidwa mlandu cifukwa cakt aciritsa munthu kmaso amalalika za kuuka kwa akufa mudzina la Yesu Khristu,Ndye kuja anauzidwa kt asiye kuyankhula za kuuka kwa akufa cifukwa iwowo zimenezi samazikhulupirira ai,Kma Petro ndi Yohane akugwiritsa ntchito Mateyu 10,kmaso Marko 13,Kt tisadere nkhawa konse pamene titengeredwa kumabwalo kt kd tikayankhula can,Pakt oyankhula siife kma mzimu oyera,Ndipo akuwauza kt ifeyo sitingasiye kuyankhula za izo tinava ndkuziona,Hallelujah πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½, Indeee Yesaya 55:10,11,Akt monga vula icitira ikagwa ndkumeretsa zipatso,Nao mau a Mulungu sadzabwerera kwa Iye asanakwaniritse zomwe ananena,Azibale anga Tiyen tisaopen ai tilalikire zauthenga wabwino umenewu pakt sitiri tokha ai mzimu oyera uli mbali athu πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ’ͺ🏽πŸ’ͺ🏽πŸ’ͺπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*

13/09/2025

MULUNGU WATSEKULA KHOMO LAKO LA MACHILITSO NDI KHOMO LA MWAI,

13/09/2025

*UTHENGA UWU UPITE KWA ONSE AMENE MASIKU ANO AKT NDI ABISHOP,ABUSA,APROPHET,CONSECO MUKUGWIRITSA NTCHITO ZIWANDA,MAFANO KMASO CIPANGIZO CIRICONSE CA SATANA*
2 Atesalonika : 2 :10-10
10. Iye adzagwiritsa ntchito mtundu uliwonse wachinyengo kupusitsa amene akuwonongeka. Iwo akuwonongeka chifukwa akukana kukonda choonadi ndi k*ti apulumutsidwe.
*Hallelujah πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½!!Condivetsa cison kwambiri ineyo ndicakt amene akuonongedwa ndi misampha a satanayi ndi azibusa,mabishop,kmaso awa akt mazi prophet-wa,Iwowa akukwaniritsa lemba la Mateyu 23,Kufuna maina abwino,ulemu kmaso dyera pandalama,ndipo iwowa ataya coonadi ndkukaniratu cipulumutso akupembedza mafano,ziwanda kmaso akugwiritsa ntchito cina ciriconse bola iwowo atchuke,alemele,kmaso apasidwe ulemu,zovetsa cison,ICHI NDICIFUKWA CHAKE NDIMAT CONDEE AZIBALE ANGA TIYEN TIPEMPHEN MZIMU WACHIDZIWITSO KT TINGAONONGEDWE NAO LIMODZI ANTHU AWA AMENE AKUONONGEKA NDI SATANA PANOPOWA πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*

13/09/2025

2 Akorinto : 11 :13-14
13. Pak*ti anthu oterewa ndi atumwi onama, antchito achinyengo, odzizimbayitsa ngati atumwi a Khristu.14. Sizododometsa zimenezi, pak*ti Satana mwini amadzizimbayitsa kuoneka ngati mngelo wowunikira anthu.
*Hallelujah πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½!!Tiri masiku otsiliza amene panopo mwa anthu 100 ndi anthu mwina awiri or atatu amene akupempha mu mchoonadi,masiku ano ambiriwa ndi satana weni weni ndipo or k*t muve uthenga wao zosiyana k*tali tali ndi Baibulo,Kmatu izi ndimphavu a satana kufuna kunyenga ambiri,inu anthu pano kupemphera kwafika pa business,kwafika pa ndale,aliyese akufuna kt mpingo wake udzaze,Indeee Yesu anat tipemphe mwini munda kt atipase antchito ena,Kma Kuno ku Hermanus ma church ali paliponse,and kt muone muona kt church cina anthu 8,mwina 7,mwina 15 akakhala ambiri zedi mwina 30,Izizi zikukwaniritsa malemba kt ndi masiku otsizadi ndithu aliyese akufuna k*tchuka ndi ndalama,Bwanji osapanga mpingo umodzi ngat mukupemphera mu mchoonadi!?? ndipo satana akugwiritsa ntchito azitsogoleri athuwa kukhala ngat opemphera pamene ai ndthu,satana wangosintha kukhala ngat m'ngero,tisamale awawa si azitumiki a Yesu Khristu ai,tiyen once again tipemphe mzimu wa cidziwitso azibale anga πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½*

11/09/2025

For the majority of Baptists, Christian baptism is the immersion of a believer in water in the name of the Father, the Son, and the Holy Spirit. Baptism does not accomplish anything in itself, but is an outward personal sign that the person's sins have already been washed away by the blood of Christ's cross.

Address

LANDLERA Street
Hermanus
7200

Telephone

+27619791919

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when The Grace of God church posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Place Of Worship

Send a message to The Grace of God church:

Share