Islamic strength's

Islamic strength's Qur'an recitation, Hadith lessons,Teachings from scholars, Fiqih and Islamic advice

26/05/2026

A Lesson from Hazrat Ibrahim Aalayih salaam

20/05/2026

CHIFUKWA CHIYANI TIMAPHA NYAMA YOPEREKA NSEMBE

Kodi bambo angakwanitse bwanji kukweza mpeni pa mwana wake yekha? Yankho lili pa cholinga cha Eid al-Adha ndi tanthauzo lenileni la kupereka nsembe.

Nkhani ya Mneneri Ibrahim عليه السلام ndi mwana wake Ismail عليه السلام si mbiri chabe. Ndi maziko a Qurban ndi phunziro la kudzipereka lomwe mibadwo yonse iyenera kukumbukira.

Mayeso Omwe Anayamba ndi Maloto

Ibrahim عليه السلام anadalitsidwa ndi mwana, Ismail, atapemphera kwa zaka zambiri. Koma Allah amayesa omwe Iye amawakonda kwambiri.

Usiku wina, Ibrahim analota kuti akupha mwana wake. Kwa mneneri, maloto ndi vumbulutso lochokera kwa Allah.

قَالَ يَا بُنَيَّ إِنِّي أَرَىٰ فِي الْمَنَامِ أَنِّي أَذْبَحُكَ فَانظُرْ مَاذَا تَرَىٰ
_“O mwana wanga, ndalota kuti ndikuzinge monga nsembe yopereka kwa Mulungu, iwe ukuganiza bwanji.”_ [Surah As-Saaffat 37:102]

Ibrahim sanabisire lamuloli. Anauza mwana wake momasuka ndi kufunsa maganizo ake.

Yankho la Ismail: Pamwamba pa Kudzipereka

Ismail anali wokhwima mokwanira kumvetsetsa kulemera kwa lamuloli. Yankho lake linakhala chitsanzo chosatha cha chikhulupiriro.

قَالَ يَا أَبَتِ افْعَلْ مَا تُؤْمَرُ ۖ سَتَجِدُنِي إِن شَاءَ اللَّهُ مِنَ الصَّابِرِينَ
_“O bambo anga, chitan zomwe mwalamulidwa, ngati Allah afuna, mudzandipeza mgulu la anthu opilira”_ [Surah As-Saaffat 37:102]

Onse awiri bambo ndi mwana anadzipereka kwathunthu. Ibrahim anagoneka Ismail chafupi ndi pansi kuti akwaniritse lamulo popanda kukayika.

فَلَمَّا أَسْلَمَا وَتَلَّهُ لِلْجَبِينِ
_“Ndipo pamene onse awiri anadzipereka, ndipo anamugoneka pachifuwa.”_ [Surah As-Saaffat 37:103]

Pa nthawi imeneyo ya kudzipereka kwathunthu, Allah analowererapo.

Kusintha kwa Chifuniro cha Allah

Allah sakanafuna kuti Ismail aphedwe. Mayeso anali okhudza kufuna ndi kumvera. Pomwe izi zinatsimikizika, Allah anasinthanitsa Ismail ndi nkhosa yaikulu.

وَفَدَيْنَاهُ بِذِبْحٍ عَظِيمٍ
_“Ndipo tinamuwombola ndi nsembe yaikulu.”_ [Surah As-Saaffat 37:107]

Check more in comment section

19/05/2026

Taswali koma Fajir yalero?or chidwi chathu chili pakukangana nkhani ya tsiku la Aarafah basi😢
Allah atichitire chisoni

15/05/2026

JUMMUA MUBARAK
MAY ALLAH ACCEPT OUR DUAS Islamic strength's

You can register if you are out of Lilongwe.Study with ICAM and become a technician accountant  FOR MORE INFORMATION@
08/05/2026

You can register if you are out of Lilongwe.
Study with ICAM and become a technician accountant
FOR MORE INFORMATION
@

02/05/2026

Osafowoka pazabwino zochepa mukupanga
Osayan'ganira zolakwika zochepa mukupanga
MALANGIZO OPINDULITSA

30/04/2026

Funso
Ndi Nthawi itiyo yomwe bodza limasanduka kukhala lokakamizidwa?waajib and kukhala lololedwa(Halaal)?

AL MOEENI CHARITY TRUSTالسلام عليكم ورحمة الله وبركاتهHope everyone is doing fine.we would like to communicate on our ne...
23/04/2026

AL MOEENI CHARITY TRUST

السلام عليكم ورحمة الله وبركاته
Hope everyone is doing fine.we would like to communicate on our new project which is Qurban and humbly request from your generous hearts to support the project

We have set a minimum of at least getting five goats for Qurban sadaqah and we believe we can since you have showed us already in the previous project that if we hold hands together everything is possible

May Allah soften our hearts and grant us more riziq as we are starting this new project ameen

21/04/2026

ALHAMDULILLAH
الحمد لله على نعمة الإسلام
zikomo Allah potipanga kukhala asilamu.

EID MUBARAK
21/03/2026

EID MUBARAK

20/03/2026

Friday lotsiriza mmwezi wa Ramadan
Allah atilipire zabwino zochuluka pa ibaadah yathu ameen.
JUMMUA MUBARAK

Address

Durban

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Islamic strength's posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share