Caring the God's Covenant

Caring the God's Covenant preaching about Gospel

18/12/2022

YOHANE (JOHN) 3 VS 16
Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi, kotero anatuma mwana wake obadwa yekha kuti yense wakukhulipilira our asataike, koma akhale nawo moyo osatha

🔹🔹🔹🔹🔹🔹🔹🔹🔹🔹🔹🔹🔹🔹🔹

Kodi okondedwa mukamakhala mimadziwa kuti Mulungu amakukondani? Nanga kodi mumadziwa kuti Yesu anafa chifukwa cha inu? Nanga mumakhulupilira kuti Yesu ndiye mpulumutsi wamoyo wanu?
Malemba akuti; ine ndine Njira ndi choonadi ndi moyo palibe munthu adza kwa Agate Loma mwa one ndekha.

Zachidziwikire kuti sitingakapeze moyo osatha ngati sitiyenda naye Yesu
Muloleni Yesu kuti akhale mbuye ndi mpulumutsi wa moyo wanu, mukatero mukhilupilire kuti anafa kamba ka inu, ndipo anadzuka ataikidwa mmanda kotero imfa sinakhalenso ndi mphamvu pa iye, ndiye ngati mukhulupilira iye simudzafai ndipo mudzakhala ndi moyo mpaka muyaya.

Chikhulupiliro ndiye gwero la moyo wosatha, tamkhulupilirani ndikuyamba kuyenda naye muon ngati sakucgitirani zazikulu pamoyo wanu. Tamuyesani muone zomwe amapanga.
Yesu ndiye yankho la chilichonse cha moyo wanu, bwerani chifupi ndi iye mukatero mudzapeza mtendere pa moyo wanu wa mtsiku ndi tsiku.

Mukhale ndi tsiku lopambana pamene mukupanga chisankho choyenda ndi Yesu. AMEN

17/12/2022

WELCOME ALL FRIENDS IN CHRIST, THIS IS THE PAGE WHICH WILL HELP US GROW UP IN SPIRITUAL LIFE.

Address

386 On Voortriker Load, Immaculate Conception Parish
Cape Town

Opening Hours

Monday 09:00 - 17:00
Tuesday 09:00 - 17:00
Wednesday 09:00 - 17:00
Thursday 09:00 - 17:00
Friday 09:00 - 17:00

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Caring the God's Covenant posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share