Christ Embassy Zomba Online

Christ Embassy Zomba Online Giving your life a meaning

Let's talk Dating, Courtship and Marriage on Saturday this same week!!
27/09/2022

Let's talk Dating, Courtship and Marriage on Saturday this same week!!

Join us Tomorrow and Saturday as we make power available to align the world with the perfect purpose of God.
23/06/2022

Join us Tomorrow and Saturday as we make power available to align the world with the perfect purpose of God.

*Rhapsody of Realities**By Pastor Chris**(Chichewa Version)**lamulungu 19, June 2022* *MKWATULO SI NKHANI YABODZA*  Paku...
19/06/2022

*Rhapsody of Realities*
*By Pastor Chris*
*(Chichewa Version)*

*lamulungu 19, June 2022*

*MKWATULO SI NKHANI YABODZA*

Pakuti n'kanthawi kochepa chabe,
Iye amene akubwera adzabwera
ndipo sadzachedwa ayi!
*(Ahebri 10:37 CCL).*

Anthu ena amakhulupirira kuti Mkwatulo
wa Mpingo ndi chinyengo. Potsutsa
zamkwatulozi iwo amanena kuti mawu akuti
“mkwatulo” sapezeka paliponse m’Baibulo, ndipo
ngakhale Yesu sanalankhulepo zokhudza zimenezi.
Inde, pali zinthu zambiri zimene Yesu sanazifotokoze
kwambiri. Mwachitsanzo, ophunzira ake anali Naye
kwa zaka zochepa zimene Iye anatumikira padziko
lapansi, komabe iwo sankadziwa kanthu za kulandira
chipulumutso kwa Amitundu. Ngakhale adawaphunzitsa
zinthu zambiri, iwo sadapeze chilichonse chomwe
chidakawapangitsa kumvetsetsa bwino kuti Amitundu
adzabweretsedwa ku chipulumutso.

https://chat.whatsapp.com/GebTAZOadei6pJNA9apS61

Ndipo Petulo pamene adapita kunyumba ya
Korneliyo, Mkulu wa Kenturiyo wachiroma ophunzira
ena atamva zimenezi, sanasangalale naye. Iye
adawafotokozera zimene adakumana nazo ndi Mzimu
wa Mulungu, ndi zamomwe, mopanda chilolezo
chake (Petroyo), Mzimu Woyera anadza pa Amitundu
pamene iye anali kulankhula nawo. Kenako Yakobo
anatsegula Malemba ndi kupeza pamene aneneri
adanena kuti Amitundu adzapulumuka. Uwu unali
umboni wawo woyamba, kufikira pamene chinsinsi
komanso vumbulutso la thupi la Khristu zinaperekedwa
kwa Mtumwi Paulo.

Ndi momwemonso ndi Mkwatulo. Simungapeze
liwu lakuti “mkwatulo” m’ndime iriyonse chifukwa,
panthawi imene amalemba, Paulo analongosola kuti
mkwatulo ndi chinsinsi: “Taonani, ndikuuzani chinsinsi;
sitidzagona tonse, koma tonse tidzasandulika.” (1
Akorinto 15:51) Pa 1 Atesalonika 4:17, Malemba amati,
‘tidzakwatulidwa”. Liwuli muchi Greek ndi “harpazo”
kutanthauza kulanda ndi kuchotsa. Matanthauziridwe
a Chilatini ndi “raptura”, amene m’Chichewa ndi
“mkwatulo”; kotero ndikulakwitsa kuti munthu anene
kuti mulibe mkwatulo m’Baibulo.

Koma musalole kuti wina aliyense akunamizeni,
Mkwatulo uchitika nthawi ina iliyonse posachedwapa.
Wayandikira kuposa kale. Zidzachitika
mofulumira kotero kuti iwo omwe sanakonzekere
ndikuwuyembekezera sadzakhala ndi nthawi
yokonzekera ndipo adzasiyidwa. Musadzakhale
inu osiyidwa. “…Khristunso ataperekedwa nsembe
kamodzi kukasenza machimo a ambiri, adzaonekera
pa nthawi yachiwiri, wopanda uchimo, kwa iwo
amene amlindirira, kufikira chipulumutso” (Ahebri
9:28).

*PEMPHERO*
Wokondedwa Atate, ndikukuthokozani chifukwa cha
mwayi wondiululira zozama zochokera m’Mawu
anu. Zikomo pondidziwitsa ine mwa Mzimu wanu
chenicheni cha Mkwatulo, ndikuti kwayandikira
kwambiri. Ndine odzipereka kukonzekeretsa anthu
ku mkwatulo, pamene ndikuyembekezera mwachidwi
kubweranso kwa Ambuye posachedwa. Amen.

*WERENGANINSO:*
2 Petro 3:3-4 NIV
1 Akorinto 15:51-52;
1 Atesalonika 4:15-18

*Ndondomeko Yowerenga Baibulo Chaka Chimodzi :*
*Ndondomeko Yowerenga Baibulo Zaka Ziwiri :*
Machitidwe 8:9-40 & 2 Mbiri 33-34
2 Akorinto 6:1-10 & Yesaya 5-6

For your loved ones who have *visual challenges*, those who have *difficult reading* and those who just *enjoying listening* to the Rhapsody Message, we now have the Rhapsody in *Audio format*, in the following languages, in our Groups :
*English, Xhosa, Shona, Ndebele, Setswana, Sesotho and Zulu.*

*PEMPHERO LA CHIPULUMUTSO*
Tikukhulupirira kuti mwadalitsika ndi bukuli. Ndipo tikukumemani kuti mumlandire yesu khristu kuti akhale mbuye wa moyo wanu popemphera pemphero ili:

*“Ambuye mulungu, ndi mtima wanga wonse, ndikukhulupilira mwa yesu khristu, mwana wa mulungu wamoyo. Ndikukhulupilira kuti iye adandifera ine ndipo mulungu adamuukitsa kwa akufa. ndikukhulupilira kuti iye ali ndi moyo lero. Ndikuvomereza ndi pakamwa panga kuti yesu khristu ndi ambuye a moyo wanga kuyambira lero. Kudzera mwa iye ndi mwa dzina lake, ndiri ndi moyo wosatha; ndabadwanso mwatsopano. Zikomo ambuye, populumutsa moyo wanga! ndine mwana wa mulungu tsopano. Halleluiah!”*

Mwachita bwino! Ndinu mwana wa mulungu tsopano.
..

*GREAT NEWS*
You can now receive the *Rhapsody of Realities Daily Devotional* messages, in your *mother tongue*, every morning on your phone or device, including *English Rhapsody* and *Teevo*

Currently we have the following *African Languages* available in our Groups (in Alphabetic Order):
*Afrikaans, Chichewa, Ndebele, Nyanja, Sesotho, Setswana, Shona, SiSwati, Xhosa, and Zulu*; and counting!

Also *invite* your friends, family and colleagues, to join the Group. Send them a copy of this Rhapsody, with the *JOIN the Group* Link.

*Click Here – to JOIN Our Groups*
https://chat.whatsapp.com/GebTAZOadei6pJNA9apS61

WhatsApp Group Invite

19/06/2022

Worship with us today from 9am-11am

It has started. Register now. $10 only for registration.
09/06/2022

It has started. Register now. $10 only for registration.

07/06/2022
*RHAPSODY OF REALITIES DAILY DEVOTIONAL (DOWNLOAD THE NEW RHAPSODY APP => https://bit.ly/2Z9P6P0)* *THE BATTLE HAS BEEN ...
07/06/2022

*RHAPSODY OF REALITIES DAILY DEVOTIONAL (DOWNLOAD THE NEW RHAPSODY APP => https://bit.ly/2Z9P6P0)*

*THE BATTLE HAS BEEN WON*

Wednesday, June 8th .
Pastor Chris

_*...help us, O LORD our God; for we rest on thee, and in thy name we go against this multitude. O LORD, thou art our God; let not man prevail against thee (2 Chronicles 14:11).*_

In the Scriptures, we find certain instances where God’s people were overwhelmed by their adversaries in numbers and weapons. In the days of King Asa, Judah was completely outnumbered by Zerah, the Ethiopian King, who invaded Judah with an army of a million men and three hundred chariots.

Asa cried out to the Lord and the Lord gave him supernatural victory (2 Chronicles 14:12). Then you find the story of Jehoshaphat, the King of Judah. Judah was surrounded by three enemy nations that were ready to attack her—Ammon, Moab, and Mount Seir. The king gathered all Judah together to seek the Lord in prayer and fasting, and God said through a prophetic message, _*“...fear not, nor be dismayed; to morrow go out against them: for the LORD will be with you”*_ (2 Chronicles 20:17).

God told them how to approach the war and was definite: He said, “Tomorrow, go out against them!” Not only that, He revealed the exact location of the enemies’ camp and gave them the strategy to defeat them. Employing the strategy God gave them, Jehoshaphat organized and placed singers, the Levites, in front to praise the beauty of God’s holiness.

The result was a great victory for Jehoshaphat and all Judah. Think about it; not a single sword lifted, yet God’s people recorded an overwhelming victory against three enemy nations. This is our reality as new creatures in Christ Jesus; we’re undefeatable. The battle was already won before we came on the scene. What God expects is for us to give Him praise. This is what we must do in our churches. Our churches have to be filled with songs of praise to God.

It makes no difference what you face in this world, be full of praise, and worship the Lord, because the battle has been won! No wonder He says, _*“My brethren, count it all joy when ye fall into divers temptations”*_ (James 1:2). Then in Romans 8:37, He says, _*“Nay, in all these things we are more than conquerors through him that loved us.”*_

*PRAYER*

*I thank you, Lord, for the victories, triumphs and successes that I experience always. You’re incorruptible and immortal, invisible, the only God; to you be honour and glory, majesty, might and dominion, power and authority, now and forever. Amen.*

*FURTHER STUDY:* *||* *Psalm 20:7* Some [trust] in chariots, and some in horses: but we will remember the name of the LORD our God. *||*

*||* *Hebrews 2:12-13 AMPC* For He says, I will declare Your [the Father's] name to My brethren; in the midst of the [worshiping] congregation I will sing hymns of praise to You. 13 And again He says, My trust and assured reliance and confident hope shall be fixed in Him. And yet again, Here I am, I and the children whom God has given Me. *||*

*||* *Hebrews 13:15 AMPC* Through Him, therefore, let us constantly and at all times offer up to God a sacrifice of praise, which is the fruit of lips that thankfully acknowledge and confess and glorify His name. *||*

*||* *Psalm 28:7* The LORD [is] my strength and my shield; my heart trusted in him, and I am helped: therefore my heart greatly rejoiceth; and with my song will I praise him. *||*

*DAILY SCRIPTURE READING*

*1-Year Bible Reading Plan=>* John 21:1-25 & 1 Chronicles 26-29

*2-Year Bible Reading Plan=>* 1 Corinthians 16:13-24 & Ecclesiastes 7-8

*BECOME A RHAPSODY INFLUENCER=>* https://bit.ly/3i4dtTU

*Be A Partner Of Rhapsody Of Realities Today! => www.rhapsodyofrealities.org*

Hey! Get Access to the World's Number One Daily Devotional and Bible Study Guide, Rhapsody of Realities App: Download here

07/06/2022

RHAPSODY OF REALITIES TUESDAY, JUNE 7TH.

THE POWER OF THE SPIRIT IN YOUR WORDS

It is the spirit that quickeneth; the flesh profiteth nothing: the words that I speak unto you, they are spirit, and they are life (John 6:63).

The excitement during our worship, praise and thanksgiving would not produce life if the contents of the songs aren’t delivered in words that are consistent with the New Testament of Christ. No matter the shouting, without the Spirit, it’s empty shout. The Spirit makes the difference.

When you speak the right words, the Spirit acts upon them. For example, it’s the reason we can speak from where we are and say to someone who’s thousands of miles away, “Be healed,” and a blind person in China will receive his sight, or someone in faraway Mongolia who’s been crippled from birth starts walking.

Such things happen because of the power of the Spirit in our words. Words recognize no seasons or barriers. Words are things; they’re tangible and potent with creative energy. So, don’t say, “Well, I wasn’t serious when I said it”; in the realm of the spirit, everything you say is living and active. It’ll work for you or against you. That’s the reason we emphasize speaking the Word only; speaking truth.

The Bible says, “For by thy words thou shalt be justified, and by thy words thou shalt be condemned” (Matthew 12:37). Don’t use words carelessly. Know, think, talk and sing the Word—whether in merrymaking or in praise to God! Let your life be consistent with God’s truths, and you’d be amazed at the resultant blessings in your life.

PRAYER
Dear Father, I thank you for giving me your Word to live by. I utter words that are consistent with your will, plans and purposes continually, knowing that my words are filled with power to produce results for your glory. I deal and speak wisely always; my words inspire faith in others, for healings, salvation and blessings, in Jesus’ Name. Amen

FURTHER STUDY:
1 Corinthians 2:4 AMPC And my language and my message were not set forth in persuasive (enticing and plausible) words of wisdom, but they were in demonstration of the [Holy] Spirit and power [a proof by the Spirit and power of God, operating on me and stirring in the minds of my hearers the most holy emotions and thus persuading them],

Mark 11:23 For verily I say unto you, That whosoever shall say unto this mountain, Be thou removed, and be thou cast into the sea; and shall not doubt in his heart, but shall believe that those things which he saith shall come to pass; he shall have whatsoever he saith.

DAILY SCRIPTURE READING

1-YEAR BIBLE READING PLAN
John 20:19-31 & 1 Chronicles 23-25

2-YEAR BIBLE READING PLAN
1 Corinthians 16:1-12 & Ecclesiastes 5-6

*"Every Child Is Your Child" To Support The Inner City Mission Hunger Action Initiative, Kindly Use The Link Below.*

icm.ngo/ham-lcm

God Bless You.

Join us tomorrow from 5pm -6pm for our midweek service.
07/06/2022

Join us tomorrow from 5pm -6pm for our midweek service.

Kindly register for this glorious time with our Man of God, Pastor Chris.
07/06/2022

Kindly register for this glorious time with our Man of God, Pastor Chris.

Address

Zomba Community Ground Hall
Zomba

Opening Hours

Wednesday 17:00 - 18:00
Saturday 09:00 - 10:00
Sunday 09:00 - 11:00

Telephone

+265994990979

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Christ Embassy Zomba Online posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share