Research CCAP Prayer House

Research CCAP Prayer House Worship Centre This page is for sharing news,inspiration messages and events taking place at our Prayer House

Research Men's ministry first Cohort, Congratulations.
14/10/2024

Research Men's ministry first Cohort, Congratulations.

14/10/2024

Research Women's Choir during yesterday's service at Bindula.

God is faithful. Akayamba ntchito sailekeza panjira. Mulungu adalitse ndipo atetedze a christu apa Research prayer house...
03/10/2024

God is faithful. Akayamba ntchito sailekeza panjira. Mulungu adalitse ndipo atetedze a christu apa Research prayer house ndi anthu onse anaikapo ndipo akuikapo dzanja pa nchitoyi

03/09/2023

Today was another beautiful Sunday not like any other Sunday but Big paper Sunday where we had Mr Naija the honorable member of parliament of the area, Mr Katema one of the guest of honor, Counsel Wester Cossam the master of ceremonies, our mother church Bindula and many more churches not forgetting the guest preacher Mr. Kalumbi from St Michaels and All Angels in Blantyre. The day was MASSIVE. For what has happened IT CAN ONLY BE GOD and to HIM BE THE GLORY. May GOD Extend your horizons forever and ever more.

M

The newly elected team
28/08/2023

The newly elected team

 BT Synod Election ResultsSynod Moderator-Rev Edina Navaya 166-Rev Moses Chitawo 58-Rev Dr Humphreys Zgyambo 237✅Vice Mo...
28/08/2023



BT Synod Election Results

Synod Moderator

-Rev Edina Navaya 166

-Rev Moses Chitawo 58

-Rev Dr Humphreys Zgyambo 237✅

Vice Moderator

-Rev Ernest Mpate 169
-Rev Chimwemwe Mitengo 63

-Rev Annie Kapinda 230✅

General Secretary

-Rev Dr Billy Gama 186
-Rev Dr Takuze Chitsulo 24
-Rev Anderson Juma 192✅
-Rev Paul Mawaya 54
-Rev Bruno Chipewa 5

 Abusa atsopano amene awadzoza kukhala otumikira mu mpingo wa CCAP Blanytre Synod awalangiza kuti akhale achitsanzo, opi...
27/08/2023



Abusa atsopano amene awadzoza kukhala otumikira mu mpingo wa CCAP Blanytre Synod awalangiza kuti akhale achitsanzo, opilira, okhulupirika ndi kulalikira Uthenga wachipulumutso mu utumiki wawo.

"Ndikupemphani kuti mumulole Mulungu akonze milomo yanu kenako muyankhule kuti Ambuye ndili pano nditumeni, adatero M'busa a William Gondwe omwenso ndi mlembi wamkulu wa sinodi ya Livingstonia.

Mu ulaliki wawo umene udatsamira pamutu wakuti ndili pano Ambuye mtumeni (Yesaya 6:8-13, Mateyu 20:25-28) M'busa Tembo adawalangiza abusawa kuti avomereze kukatumikira kulikonse ndinso kwa anthu a magulu onse kuphatikizapo ovutika.

Malangizowa awapereka pa 27 August 2023 kumwambo wa mapemphero ku St Michael and Angels mu mzinda wa Blanytre. Iyi ndi mbali imodzi ya msonkhano waukulu wa Sinodi-yi wachinambala 34.

Poyankhulanso kumwambowu M'busa Khamisa amene akuyembekezera kukhala wamkulu oyang'anira moyo wa uzimu mu Sinodi ya Livingstonia adalangiza adindowa kuti apite akatumikira Yesu Khristu mokhulupirika osati chifukwa cha zokoma ndi zoyanja.

Adapitiriza kuwalangiza kuti akonde mabanja awo ndinso akapange ubale wabwino ndi anthu onse, akakhulupirika pankhani zachuma ndi kupanga zinthu poyera kumalo amene akatumikire.

"Kapeweni zinthu zitatu izi: kufuna maudindo mwachangu, azimayi ofuna kuchita zibwenzi ndi abusa komanso chikondi cha pa ndalama. Osaiwala anthu andale" adatero M'busa Khamisa.

Abusa okwana khumi ndi awiri (12) ndiwo awapatula pa mwambowu umene adautsogolera ndi M'busa Edna Navaya amene ndi Wamkulu Woyang'anira moyo wa uzimu mu sinodi-yi.

Malingana ndi Mlembi wamkulu wa Sinodi ya Blantyre, M'busa Dr Billy Gama izi zikubweretsa chiwerengero cha abusa mu sinodi-yi kufika pa 254 tsopano.

(by Edward Abraham)

Our Sunday school participants for today with their teacher(in red)
27/08/2023

Our Sunday school participants for today with their teacher(in red)

Let's meet there.
25/08/2023

Let's meet there.

Praise team spiced the service too.
23/07/2023

Praise team spiced the service too.

Address

Limbe
Thyolo

Telephone

+265998739096

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Research CCAP Prayer House posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share