20/06/2026
TSIKU LA 171 MU CHAKA CHA 2026 (20/06/2026)
‼️ MAWU OPATSA MOYO ‼️
Yohane 3:3
"Yesu anayankha nati, Ndithu ndithu ndikunena kwa iwe, munthu akapanda kubadwanso, sangathe kuona Ufumu wa Mulungu."
Phunziro: Moyo osatha tidzaupeza tikabadwa mwatsopano ndikulandira Yesu.
Goodmorning saints 😊