GRACE of GOD living Church

GRACE of GOD living  Church Receive updates of how the radical love of Jesus is changing peoples lives and setting them on fire with the Holy Spirit ! Also see info on future events.

MUTU 12 KUTHA KWA   BANJA Tiyeni tione mwa zina zomwe zimachitika ngati banja latha. Nthawi zambiri banja limakathera ku...
28/01/2026

MUTU 12
KUTHA KWA BANJA

Tiyeni tione mwa zina zomwe zimachitika ngati banja latha. Nthawi zambiri banja limakathera kukhoti, mwamuna kapena mkazi akakasuma.
Yesaya 41:10
Usaope, pakuti Ine ndili pamodzi ndi iwe; usaopsedwe, pakuti Ine ndine Mulungu wako; ndidzakulimbitsa; inde, ndidzakuthangata; inde, ndidzakuchirikiza ndi dzanja langa lamanja la chilungamo.
Ngati wachotsedwa ku banja opanda chifukwa chokwanira Yehova amakhala nawe nthawi zonse.
Mukasankha kuti banja lithe, mungalandidwe mwana, nyumba kapena kulipira ndalama. Mungayesetse kudandaulira woweruza koma mwina iye sangasinthe chigamulo. Mapeto ake woweruzayo, yemwe mwina simukudziwana naye n’komwe, angakuuzeni masiku amene muyenera kukaona mwana wanu pa mwezi, ndiponso ndalama zimene muyenera kumamupatsa. Zimene woweruzayu angakulamuleni kuchita zingakhale zosiyana kwambiri ndi zimene inuyo mukanachita panokha.
1 Akorinto 1:10
Koma ndikudandaulirani inu, abale, mwa dzina la Ambuye wathu Yesu Khristu, kuti munene chimodzimodzi inu nonse, ndi kuti pasakhale malekano pakati pa inu; koma mumangike mu mtima womwewo ndi m'chiweruziro chomwecho.
Nthawi zambiri kuthetsa banja kumangoyambitsa mavuto ena. Chilichonse chimasintha, kungoyambira kokhala komanso ndalama, ndipo nthawi zambiri kusintha kwake kumakhala kopweteka. Komanso kutha kwa banja kumawakhudza kwambiri ana.

Mateyu 19:9
Ndipo Ine ndinena kwa inu, Amene aliyense akachotsa mkazi wake, kosakhala chifukwa cha chigololo, nadzakwatira wina, achita chigololo: ndipo iye amene akwatira wochotsedwayo, achita chigololo.
Ena amathetsa banja ati chifukwa mkazi sakubereka kapena mwamunsa koma tizindikire mawu ochokera ku Genesis 25:21, Ndipo Isaki anampembedzera mkazi wake kwa Yehova popeza anali wouma: ndipo Yehova analola kupembedza kwake, ndipo Rebeka mkazi wake anatenga pakati.

21/11/2025

*MULUNGU SADZACOKA KUMWAMBA KUDZAJUCENJEZAN AMAGWIRITSA NTCHITO ANTHU OMWEWA πŸ™πŸΎπŸ™πŸΎπŸ™ŒπŸΎπŸ™ŒπŸΎ*
Machitidwe : 23 :12-16
12. Kutacha Ayuda ena anakonza chiwembu ndipo analumbira kuti sadya kapena kumwa mpaka atapha Paulo.16. Koma mwana wa mlongo wake wa Paulo atamva za chiwembuchi, anapita ku malo a asilikali aja namufotokozera Paulo.
*Hallelujah πŸ™πŸΎπŸ™πŸΎπŸ™ŒπŸΎπŸ™ŒπŸΎ!! Davide atapha Uriya Mulungu anagwiritsa ntchito Natan kukamuuza zonse izo zacitika ndiizo Mulungu adzacitire Davide, mzinda wa Ninive utaipa ndi macimo Mulungu anagwiritsa ntchito Yona ndipo anthu aja analapa, Indee taonan azibale anga apaso Mulungu akugwiritsa ntchito mwana wang'ono kukacenjeza Paulo za ciwembu ico akoza Ayuda, kd cikanacitika ndican Paulo akanangozera,!? Mwacidziwikire akanaphdwa, Azibale anga tiyen tiven mauthenga omwe anthuwa akutiuz pakt akucita kutumidwa ndipo tikapanda kuvera tidzafa or kupeza vuto πŸ™πŸΎπŸ™πŸΎπŸ™ŒπŸΎπŸ™ŒπŸΎ*

16/11/2025

Tikadzuka ndi Moyo tiziyamika

😭😭😭😭😭😭😭😭okondedwa pano tili pa deport tikudikira bus Kuti tikwere, ndiye ofunika nthawi zonse tizikhala okonzeka , Lero ...
20/10/2025

😭😭😭😭😭😭😭😭
okondedwa pano tili pa deport tikudikira bus Kuti tikwere, ndiye ofunika nthawi zonse tizikhala okonzeka ,
Lero mmawa ndakandira uthenga Kuti mayi Happiness dauka Phiri amwalira ndipo ndidagwidaa ndi chisoni chifukwa lachitatu lomwelo ndayankhula nawo timakambiran Za Ku church , Ku ndilande .
Mudwala atinayamba dZana usiku mkumwalira , Tiyeni tiziyemda okonzeka ,
Mayi happiness dauka akukira Ku ndilande Koma kumudzi kwawo nsiku chiladzulo , Moti maliro pano Ali Ku chiladzulo, Mayi dauka adaki mlembi WA amayi ampingo wathu Ku Malawi, sitizaiwla ZABWINO amachita, ndipo magwira ntchito Ngati yolipidwa anaki ndi changu Koma tathedwa nzeru.
R I P

CHONDE TIWERENGE MOSAMALA NDIKULINGALIRA BWINO ALI M BALE WAKO ,TIYENI TIWATHANDIZE AZATHUWA .UTHENGA OCHOKERA KWA M BAL...
03/10/2025

CHONDE TIWERENGE MOSAMALA NDIKULINGALIRA BWINO ALI M BALE WAKO ,TIYENI TIWATHANDIZE AZATHUWA .
UTHENGA OCHOKERA KWA M BALE WATHU ,ALI KUMALAWI .MULANJE
Okondedwa mwa Ambuye ndabwera pano sindimayenera kutero ai koma kutengera ndimene nyengo zanga zafikira pano zafika poipa ndimafuna ngati kotheka wachifundo andithandize ndalama ya chakudya,masiku ambiri tikumagona njala chovetsa chisoni azingono anga ali form 2 moti fess ndilibeso murimose mene mungakwanisiremo kwa ine ndiyokwana mungandinthandizire panopa kutengera kuti ndipagulu komaso ndikutilemba singakwanise kufotokoza munyengo zomwe ndikudusa koma mukafunisisa kudziwa mundipeza pa number iyii WhatsApp 0982674013 chonde mochita kupepha abare ndi alongo ndiziwa ine singakwanise kukubwezerani kanthu ai koma mulungu yekha ndamene angakwanise kubweza pa mateyu chapter 5 vs 7 amati odala Ali akuchitira chifundo chifukwa azalandira chifundo chonde help meπŸ™πŸ™πŸ™

01/10/2025

*SIZOIPA ZONSE ZOMWE ZIMACOKERA KWA SATANA πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*
Danieli : 9 :12-14
12. Inu mwakwaniritsa mawu amene munayankhula otitsutsa ife ndi otsutsa otilamulira potibweretsera tsoka lalikulu. Pa dziko lapansi sipanachitikenso zinthu ngati zimene zaonekera Yerusalemu.13. Monga kunalembedwa mΚΌMalamulo a Mose, tsoka lililonse latifikira chikhalirecho sitinapemphe Yehova Mulungu wathu kuti atikomere mtima. Sitinasiye machimo athu, ndipo sitinasamale choonadi chanu.14. Choncho Yehova anakonza kuti atigwetsere tsoka limeneli, ndipo wachitadi popeza Yehova Mulungu wathu ndi wolungama mu chilichonse amachita; chikhalirecho ife sitinamumvere.
*Hallelujah πŸ™ŒπŸ™ŒπŸ™πŸ™πŸ™!!1 Mafumu 13:3-6,Yeroboamu anauma mkono pamene amafuna kutemberera munthu wa Mulungu, kd izi anapanga ndi satana!? Ai,Miriam anadwala khate tikaona pa Numeri 12,Kd khate iri anapangitsa ndi satana!? Ai,Farao anavutika ndi nthedwa zambiri kmaso muliri,kd anapanga ndi satana!? Ai nanga tikaona anthu aja anavutika ndi bokosi lacipangano aja,pa 1 Samuel 5,Anali satana!? Ai,Indeee azibale anga Zinazi timaziputa dala cifikwa cakusavera kwathu Yehova,ndkukuuzan zinazi or muzit satana coka,mumangodzivuta ngat mukucotsa satana pamene zintchito zanu zikukhalabe zoipa,Mulungu mau ake sadzapita pacabe Aroma 6:23,Mphotho a Ucimo ndi imfa πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*

01/10/2025

Marko : 5 :19-20
19. Yesu sanamulole, koma anati, β€œPita kwanu ku banja lako ndipo ukawawuze zimene Ambuye wakuchitira, ndi chifundo chimene wakuchitira.”20. Pomwepo munthuyo anapita nayamba kuwuza anthu a ku Dekapoli zinthu zimene Yesu anamuchitira. Ndipo anthu onse anadabwa.
*Hallelujah πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½!!!Ndimakonda kunena nthaw zambiri kt,ulaliki umene panopo ukuyenda ndkuveka nthaw zina sukwanira ai kma zintchito zomwe Yesu Khristu anakucitiran ndiinuyo kucita ndi umbon kmaso uthenga okwanira,Paulo anali cigawenga,Pamene Paulo amatumikira amagwiritsa ntchito nyengo omwe anali kukhala uthenga wamphavu ndipo anthu ena amayambira pamenepo kumutsata,Azibale anga ndkt inuyo musacite kufuna ma ves mpaka 100,Tawauzan anebawo kt neba wandiona,kt ndikhale conci ndi Mulungu ndadutsa pa izi,izi kmaso izi,kd popanda Mulungu ndikanapambana !? Anthuwo akava izi ziwakoma ndkuona ukulu wa Mulungu πŸ™πŸ½, Uyu waziwandayi zitatuluka anacitira umbon za iye mwini nafeso tatiyen anthuwa tiwaonetse uko tinali ndipomwe tiri lero lino πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*

01/10/2025

1 Timoteyo : 2 :1
1. Tsono choyamba ndikukupemphani kuti mupempherere anthu onse. Mapemphero anu akhale opemba, opempha, opempherera ena ndi oyamika.
*Hallelujah πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½!!Kd azibale anga mumadziwa kt kupempherera ena pamavuto,nyengo or zosowa zao ndimadalitso akulu kwaife kuposa or owapemphererawo!? Yesu Khristu sanacimwe ai,sanapangepo ciriconse coipa ai,kma polola kubwera pano padziko lapansi kudzaombola inu ndiine,Pano Yesu Khristu ndiolemekezeka kuposa maina onse,ndmakonda kunena kt Yobu anangopempherera azake awiri aja pompo zinthu zake ndkuyamba kubwezeretsedwa,Ndkt inuyo or mulibe umfa,ndio,mwana,banja ndi zina zotero apemphereren azanu amene ali ndi vutowo ndkukuuzan mudzadalitsika kopambana kuposa momwe mumayembekezera,Ndicifukwa cake Paulo akt tizipempherera ena mopemba,mopempha kmaso oyamika πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*

01/10/2025

*Hallelujah πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½!!Nkhomaliro ikuyenda bwanji azibale anga!? Munaganizapo za Israeli!? Ena akt ndi dziko ladalitsika ena la nkhondo enaso akulinena momwe aonera,nanga Ninive,akt ndi dziko loipa kwambiri mpaka Mulungu analikwiira akanaliononga,Ndizoona!? Ndye akat dziko ndican!? Dziko ndi anthu,ndkufuna ndikuuzen kt Dziko la Ninive lilibe vuto or tchimo kma anthu adzikomo,Azibale anga akat nzinda okonda zipondereza ndye kt ndi anthu okhala munzindawo,Ndipo akt cotsatira cake ndi tsoka azibale anga tiyen tisakhalen atsoka ai nthaw zonse kma tikhale a mwai pocita zimene Mulungu amafuna,amatiuza kmaso kutipempha,tikatero Deuteronomo 28:1-13 Adzakwaniritsidwa kwa ife πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*

01/10/2025

*KD TIMACITIRA ULEMU ENA MAKA MAKA OKALAMBA πŸ€·πŸ½β€β™‚οΈπŸ€·πŸ½β€β™‚οΈπŸ€·πŸ½β€β™‚οΈπŸ€·πŸ½β€β™‚οΈ*
1 Timoteyo : 5 :4
4. Koma ngati mkazi wamasiye ali ndi ana ndi zidzukulu, anawo ayambe aphunzira kukwaniritsa udindo wawo pa banja lawo moopa Mulungu, potero akubweza zabwino kwa makolo awo ndi agogo awo. Pakuti zimenezi ndiye zimakondweretsa Mulungu.
*Hallelujah πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½!!!Lemba iri ndkuona ngat ndi anthu 20 out of 100 amene analiwerengapo,ndkt lemba iri or acinyamata ambirife sitilidziwa ai,Ndiangat amene akangofika zaka 70 ndi mfiti!? Ndinavapo komwe kuno ku Eastern Cape kt anthu ayatsa nyumba ndkupha nkhalamba ina poiganizira kt ndi mfiti,sanawapeze akutamba ai,kma kuwaganizira kt ndi fiti,ndipo or ku malawi,aliyese okalamba panopo ndi mfiti,kma kd ndizoyenera kutero!? Ai akt citiran ulemu anthu okalamba ndkuwacitira zabwino,pakt mwakutero mumakhala ngat mukubweza zabwino zomwe makolo anu anakucitiran,Indeee ulemu ndiofunika ndipo akt ngat titero ndye kt tikukondweretsa Mulungu,Kd ife timakondweretsa Mulungu pocitira zabwino ena!? Mateyu 25:31-46,Yesu Khristu anat amene amacitira zabwino anthu onyozekawa amakhala kt akucitira Iyeyo πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*

01/10/2025

*NDIMATHANDIZA AMENE AMANDITUMIKIRA,NANGA OSAKUTUMIKIRANIWA BWANJI AKUTHANDIZIKANSO πŸ€·πŸ½β€β™‚οΈπŸ€·πŸ½β€β™‚οΈπŸ€·πŸ½β€β™‚οΈπŸ™πŸ½πŸ™πŸ½*
Yesaya : 66 :14-14
14. Mukadzaona zimenezi mitima yanu idzakondwera. Mudzabiriwira ngati udzu. Zimenezi zidzakulimbikitsani ndi kukupatsani moyo wamphamvu. Mudzadziwa kuti ndimathandiza amene amanditumikira ndi kuti ndimakwiyira adani anga.
*Hallelujah πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½!!Yehova akt ndmathandiza amene amanditumikira,ndipo ndmadana/Ndimakwiira ndi adan anga,Masiku ano anthu omwe akusangalala 98% ndi adan ake a Yehova amene sapemphera,tacita cifuniro ca Mulungu kma akusangalala,Indeee azibale anga izizi zikuzunguza mutu anthu ambiri ndipo anthu ambiri asiya kupemphera,Masalimo 73,kmaso Masalimo 37,Davide anayankha za anthu ocita zoipa or opeza zabwino munjira oipa,ndipo akt adzatha ngat udzu,tisakhumudwe nao ai kma ifeyo maso athu akhale kwa Mulungu nthaw zonse πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*

01/10/2025

*KUIPA KWA TECHNOLOGY PA MOYO WA UMZIMU πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*
Deuteronomo : 6 :
6. Malamulo amene ndakupatsani lero ayenera kukhala mu mtima mwanu.
*Hallelujah πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½!!Anthu ambiri masiku ano tikuona kt technology apanga zinthu zambiri zomwe zimavuta kukhala zosavuta,Kma kd munaganizapo kt technology ikuononga bwanji moyo wa Umzimu!?Apa Mose akuuza Aisrael(Ifeyo) kt malamulo amene ndakupasaniwa azikhala mumtima mwanu,Kd ndicifukwa can anatero!? Indee ndkuganiza kt Mulungu anadziwa ndthu kt idzafika nthaw omwe tidzacotse cidwi cathu mumkudziwa mau,m'malo mwake lemba lirironse ilo talifuna tizidzangopanga search bas talipeza ndikuuza anthu,Izitu masiku ano ambiri ndi abusa,asembe,Apro kmaso maina ena ambiri cifukwa ca technology itini mphatso a umzimu alibe,Technology atilanda luntha lonse lodziwa malemba panopo nthaw zonse tikudalira technology,Malamulo a Mulungu azikhala mumtima mwanu osat mu phone anu ai,kt nthaw zonse muziwalingalira kt mupambane kmaso mukhale olimba mtima Yoswa 1-8 πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™πŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½πŸ™ŒπŸ½*

Address

Salima

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when GRACE of GOD living Church posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share