Prophet David Kubali

Prophet David Kubali Leader and founder of the Oracle Global Christian church and Yadah Investments.

Tsiku lanu linali bwanji?,Pali chokhumudwitsa chilichonse mwakumana nacho lero ku ntchito kaya ku business kwanu so that...
02/05/2026

Tsiku lanu linali bwanji?,
Pali chokhumudwitsa chilichonse mwakumana nacho lero ku ntchito kaya ku business kwanu so that tithandizane kumangilirana mwa Ambuye?

02/05/2026

MONI
KOMANSO NDINU MUDALITSO WANGA

02/05/2026

Angati ali online?, ndilowe online just to greet you

02/05/2026

Okondedwa Ambuye?, Dzikomo β™₯οΈπŸ‘

02/05/2026

Lero mwalota chani? titanthauzile malotowo!

God is with Us, Testimonies are increasing, the glory is multiplying. Everyday we are building. I prophesy that You will...
02/05/2026

God is with Us, Testimonies are increasing, the glory is multiplying. Everyday we are building. I prophesy that You will Shine everyday in Jesus name

PEMPHERO LA M'MAWA WITH PROPHET DAVID KUBALI Atate Ambuye wathu Yesu khristu takweza manja athu kulambira dzina lanu loy...
02/05/2026

PEMPHERO LA M'MAWA WITH PROPHET DAVID KUBALI

Atate Ambuye wathu Yesu khristu takweza manja athu kulambira dzina lanu loyera ndi lamphamvu mwayenera kulandira ulemu ndimatamando ochuluka nthawi zonse palibe ofanana nanu timakukondani kwambiri khalani pafupi nafe.
kwalembedwa tizikhala oyera mtima popeza ndinu oyera mtima chonde tikhulukireni zochimwa zathu zonse.

Tikuthokoza kwambiri chokera pansi pamitima
yathu kuti zikomo kwambiri mwatidzutsa amoyo mawa uno zikomo kwambiri talandira nao mphweya wa moyo.

simphamvu sinkhondo koma tabwera mozichepetsa ndimogonja pamaso panu mphamvu ya Mzimu oyera ikhale pakati pathu kutiphunzitsa Kuyenda mu chifuniro chanu.

tikhala tikupita ku malo osiyana siyani perekani chitsongozo cha bwino kwambiri chifukwa mumatikonda kwambiri komanso mumayakha mapemphero athu.
kuli azathu odwala kawapatseni machiritso anu zipatala ndi manyumbamu achitireni chifundo chodzadza ndikuyakha chosowa chathu.

kuli azathu Akusowa ntchito, chakudya, mtendere, mphamvu, chitetezo, nzeru, ndalama, chipambano kawapatseni monga mwachifundo chanu.
kuli azathu Mabanja aphwasuka kawamangeni tikumbukireni kutipatsa zokhumba zathu zosiyanasiyana mukhale nafe ndikutsogolera chitetezo chanu chikhale panjira yathu.

onse alipamaulendo muwayendese bwino
ataya okondedwa awo apukuteni misozi
onse aumphawi, amasiye, olumala, ophinjika, okalamba, akundende apatseni zosowa zao mwa Yesu khristu amen.

VERSI YA LERO
pakuona mayendendwe anu oyera ndi kuopa kwanu. 1 Petro 3:2.
mayendendwe anu akhale oyera pa maso pa Mulungu ndi kuopa Mulungu.

02/05/2026

Sunataye nthawi yako kukhala online!

LANDILA GAWO LA MAYANKHO AMAPEMPHERO AKO

Ndikulengeza pa iwe wagwira foniwe, Kumwamba kukudzidzimutse ndi m'dalitso!!
02/05/2026

Ndikulengeza pa iwe wagwira foniwe, Kumwamba kukudzidzimutse ndi m'dalitso!!

01/05/2026

Amene uli online iwe sunabetse

LANDILA MIRACLE YA NTCHITO NDI BUSINESS YAPAMWAMBA

01/05/2026

Not everyone around you is for you, some are against you.

May God give you discernment spirit and expose every hidden agenda.
If you receive it, TYPE AMEN πŸ”₯πŸ™

01/05/2026

Ati adzatifuna! Mau awa sandinvekera bwino! kaufiti kamakhalamo ! Koma ngati unalankhulidwa izi ndi wina wake ikhaleπŸ‘‰ back to sender in Jesus name .πŸ™πŸ”₯

Address

Mzuzu

Telephone

+265887456954

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Prophet David Kubali posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Place Of Worship

Send a message to Prophet David Kubali:

Share