Prophet David Kubali

Prophet David Kubali Leader and founder of the Oracle Global Christian church and Yadah Investments.

Or ulibe pepala la form 4 kaya university koma ngati chisomo cha Mulungu chili pa iwe within 4 weeks from now ntchito uy...
10/06/2026

Or ulibe pepala la form 4 kaya university koma ngati chisomo cha Mulungu chili pa iwe within 4 weeks from now ntchito uyipeza ndipo uzaperekera umboni pano mu dzina la Yesu Christ

10/06/2026

Minyama yaku mtundu kwanu, Mulungu akuyichotsa lero pa iwe mu dzina la Yesu Christ

KULOTA ZOVALA KUMATANTHAUZA IZI👇👇👇🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏1.kulota zovala zoipa(dirty clothes)  zimatanthauza mzimu wa umphawi, okuth...
10/06/2026

KULOTA ZOVALA KUMATANTHAUZA IZI👇👇👇
🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏

1.kulota zovala zoipa(dirty clothes) zimatanthauza mzimu wa umphawi, okuthandiza onse a khoza kukuthawa.

2.Kulota zovala zokongola/white zimatanthauza kuti ubale wako ndi mulungu uli bwino.

3.Kugula zovala pa mtsika kutanthauza kuti mavuto a mbanja(marital problems)

4.Kugula zovala mu shopu(super market) zimatanthauza zabwino zikubwera pa moyo wako.

5.Kusintha chovala kusiya chikhalidwe chako chakale.

6.Kuvala chovala chobwereka zikutanthauza kupasirana mizimu/matenda, tembelero, ndi yemwe wakubwerekayo.

7.Kulota utavala chovala cholembedwa mawu oti alibe tanthauzo la uzimu zikutanthauza kuti pali chovala China chake chikubweretsa mavuto pa moyo wako.

8.Kulota utavala chong'ambika zikutanthauza umphawi ndi kusowa kwa zinthu pamoyo wako

9.Kulota zovala za mwana koma uli oyembekezera ndiye kuti uli pafupi kuchira.

10.Kulota chovala chopakika magazi koma uli woyembekezera ndye kuti ukhoza kupititsa padera(miscarriage) kukanika kwa zinthu.

1.kulota chovala chako chili Mmadzi zikutanthauza kuti madalitso ako amangidwa ndi mizimu ya pansi pa madzi.

1 2.Kulota chovala chako chitasowa zimatanthauza kuti maonekedwe ako satana wawasokoneza(lost beauty)

Zambiri zikubwera

🙏🙏🙏🙏🙏Follow Prophet David Kubali zisakuphonyeni
prophesy WhatsApp (+265)984153396

10/06/2026

LOCATION: SANTON

10/06/2026

AFRICA JUBEK SANTON
WA NTCHITO
- Ndikungofuna anthu awiri basi oti Sali pa ntchito ndiwapezere ntchito.

Yesani mwayi potumiza
Dzina lanu, surname WhatsApp phone number, location komwe mukhalira komanso chithuzi chanu cha full mu comment section. Ngati mwachita mwayi muyimbilidwa phone anytime today

  MULUNGU MA PLAN ONSE A AFITI ZIMAWATEMBENUKIRA OKHA   YA MOTO anditumizira message ku TikTok pa zomwe awona pa ine   K...
10/06/2026

MULUNGU MA PLAN ONSE A AFITI ZIMAWATEMBENUKIRA OKHA YA MOTO anditumizira message ku TikTok pa zomwe awona pa ine Kubali.

Ndili pano kukulimbikitsani ukamva izi osakhala ndi mantha pena amafuna uwakuluphilire kenaka ukawafunsa kuti nanga ndipange bwanji amvekere bweretsa ng'ombe or 1 million, pomwe kwa Mulungu it's for free

10/06/2026

WA NTCHITO KU SOUTH AFRICA
- Amene muli around JUBEK kuno simuli pa ntchito mufuna ntchito please WhatsApp me now now(+265)984153396

  WA MPHAMVU Ine dzina langa ndine Marry Manda ndimakhala ku South Africa.Umboni wanga ndiwoti ndimagwira ntchito ndi ab...
10/06/2026

WA MPHAMVU
Ine dzina langa ndine Marry Manda ndimakhala ku South Africa.

Umboni wanga ndiwoti ndimagwira ntchito ndi abwana ena ake konkhuno ku South Africa kwa zaka 6, then tsiku lina lake Chaka chomwechi ndinagodabwa atayimba phone kuti ku ntchito usabwerenso yatha, ndinabalalika ndipo ndinasowa mtendere chilichonse chinayima moyo wanga Palibe chimene chimayenda nayamba kuganiza zobwelera kumudzi.

Kenaka Pali mzanga wina wake amene amasathira prophet David Kubali anandiuza kuti usagwe mphwayi uyambe kusathira page ya KUBALI ndipo mauthenga ake muli uneneli, chilimbikitso komanso chiyembekezo.

Ndinayamba kusathira utumiki wake wapa Facebook TSIKU lina analemba kuti onse amene ntchito zinawathera ayimbilidwe ma phone ndima bwana awo abwereretso ku ntchito mu dzina la Yesu Christ, ine ndina tayipa AMEN wamphamvu komanso wachikhuluphiliro panagondusa matsiku ochepa abwana anga aja anandiyimbira phone kuti mawa uzibwera ku ntchito ndipo ndikunena pano ndinayambanso ntchito.

Prophet Kubali, Mulungu wanu ndiwowona komanso mumapembeza muchoona, ndikuchita kukanika kuti kaya ndingakuthokozeni ndi chani. Ambiri akumapelekera mawumboni pa zabwino Mulungu wanu akuwachitira , inenso ndawona zazikulu Mulungu wanu wandichitira ndipo ndinali munthu umodzi onyozera zopempherapemphera koma kuyambira lero ndikhala follower wanu wankhulu.

Ambuye Yesu Christ akudalitseni, ndikadakonda mukanandijoinitsa ma group anu onse awulaliki.

Dzikomo Pastor

MALOTO AWA OFUNIKA KUSALA KUDYA MKUPEMPHERA KUTSUTSANA NAWO MWACHANGU 👇👇👇👇👇🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔1.kulota mutalumidwa ndi galu zima...
10/06/2026

MALOTO AWA OFUNIKA KUSALA KUDYA MKUPEMPHERA KUTSUTSANA NAWO MWACHANGU 👇👇👇👇👇
🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔

1.kulota mutalumidwa ndi galu zimatanthauza kuti wina akukupangirani zamatsenga /za ufiti kuti alimbane ndi
👉. Ntchito yanu
👉. Banja lanu
👉Moyo wanu
2.Kulota njoka itakuluma zimatanthauza kuti satana wapanga ataki moyo wa uzimu kapena banja lanu. Paja njoka =Satana. Yesu =mkango, nkhosa. Mzimu woyera=nkhunda. Nyama zimakhala ndi tanthauzo ku uzimu.

3.Kulota ukutaya magazi zimatanthauza kuti mukhoza kutaya moyo (magazi=moyo... Levitiko 17.) pena zimatanthauza kuti satana wapanga nawe pangano kumaloto kumbukirani Abraham adapanga pangano ndi mulungu ku maloto.

4.Kulota utasemphana ndi mwayi(missed opportunity) Kupeza mayeso atatha, interview, bus yakuthawa....

5.Kulota utaponda bibi(stepping on faeces /p**p) zimatanthauza mzimu wa imfa. Kufa kwa ntchito, banja, business,...

6.Kumira mmadzi zimatanthauza kuti satana akufunitsitsa uzikhala moyo wosowa mtendere(restlessness)

7.Kugwidwa pansewu kapena kusochera zimatanthauza kuti pali zotchinga Zambiri kuti usabooleze kapena usamasulidwe. Anthu amangokulonjeza zithu koma samakwanilitsa(unfulfilled promises and disappointment).

8.Kunyamula, kugula, kuona, madzira ovunda(rotten eggs) zimatanthauza kuti mukhoza kudwala kwambiri ndi Nthenda imeneyo.

Follow Prophet David Kubali ministries
WhatsApp (+265)984153396

🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏

MALOTO OSONYEZA KUTI MULEMERA (DREAMS THAT SHOWS YOU WILL BE RICH)😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂1.kulota mukuvumbidwa mvula(yakobo 5:18)2.Ku...
09/06/2026

MALOTO OSONYEZA KUTI MULEMERA (DREAMS THAT SHOWS YOU WILL BE RICH)
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

1.kulota mukuvumbidwa mvula(yakobo 5:18)

2.Kulota ukuthandiza anthu osowa (Miyambo 19:17)

3. Kulota ukuppemphera(masalimo 34:15)

4.kulota ukuwerenga ndalama (miyambo 10:22)

5.Kulota mukupha nsomba(miyambo 16:3)

6.Kulota mutagula malo, nyumba, galimoto..(mateyu 7:7)

7.Kulota mukuthyola kapena kusonkhhanitsa zipatso(Genesis 12:8)

8.Kulota mutamenyana ndi munthu wamphamvu/wankulu/Chirombo koma mkugonjetsa(lukas10:19)

9.kuvala chovala chatsopano (Genesis 6:8)

10.Kuona kumwamba kutaseguka(2Timoteo 4:18-19)

Kumbukirani kupanga follow kuti zisamakuphonyeni

Address

Mzuzu

Telephone

+265887456954

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Prophet David Kubali posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Place Of Worship

Send a message to Prophet David Kubali:

Share