Bible study with Mr Harry

Bible study with Mr Harry Contact information, map and directions, contact form, opening hours, services, ratings, photos, videos and announcements from Bible study with Mr Harry, Mzuzu.

Iyi ndi page yothandiza anthu kuvetsa Bible komaso kudziwitsa zina za Bible zomwe Ena sazidziwa komaso kuyankha fuso lililose lomwe anthu alinalo kuchoka Bible lomwe yankho lake limawavuta

27/05/2026

Mwagonako kuchipatala mu chakachi
Ngati ayi muyamikeni MulunguπŸ™πŸ™

25/05/2026

Kodi chifukwa chani Yesu amaphuzitsa mu mafanizo?

24/05/2026

TODAY'S VERSE Exodus 20:7
Usatchule dzina la Yehova Mulungu wako pacabe cifukwa Yehova sadzamuyesa iye wosacimwa, amene achula pacabe dzina lacelo.

16/05/2026

KWABWELA FUSO
Kod Adam ndi hava adachimwa atagonana or atadya chipatso? Tik*tsutsana kuno tithandizeni ndipo mutipase ves lake

27/03/2026

Ambiri Timalithawa fuso Ili
Kodi mumamukonda Mulungu?

14/01/2026

MAU OGONELA

YOHANE 3 : 16
PAKUTI MULUNGU ANAKONDA DZIKO LAPASI KOTELO ANAPATSA MWANA WAKE OBADWA YEKHA KUTI YESE WAKUKHULUPILIRA IYE ASATAIKE KOMA AKHALE NAWO MOYO OSATHA.

GOOD NIGHT βœ…

05/01/2026

Zinthu 5 zomwe zimapangitsa munthu kusapita chitsogolo;
1. kudzikweza
2.nsanje
3. kuiwala Mulungu kumadziva k*t zomwe uli nazo wazipeza chifukwa ndiwe wanzeru osat Mulungu
4.Kusathandiza ena koma muli ndi k*thekela
5.kusatenga mbali pa za Umulungu koma ma party, ma show , magulu , maukwati ndi pa fb za Mau a Mulungu sitipanga like or comment Koma za dziko

Tiyenela kusintha zochita zathu ngati tinamuvoneleza YESU ndi mitima yathu zitchito zathu zikhale chimodzimodzi

MULUNGU atithandize πŸ™πŸ™πŸ™

04/01/2026

Kwa omwe Timapemphela Sunday Mau a lero anachoka pa buku lanji?
ife Yohane 1:1 to 18
πŸ“–πŸ“–πŸ“–

03/01/2026

TODAY'S VERSE
MASALIMO 50:15
Ndipo undiitane tsiku la sautso,ndidzakulanditsa, ndipo iwe udzandilemekeza. πŸ™πŸ™
Ambuye akudalitseni

Address

Mzuzu

Telephone

+265993704930

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Bible study with Mr Harry posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Place Of Worship

Send a message to Bible study with Mr Harry:

Share