23/05/2026
Ya Allah,titetezeni ku umphawi, mutisunge kutali ndi ngongole,
mavuto, ndi chilichonse chimene chimabweretsa manyazi.
Dzazani mitima yathu ndi chiyamiko
ndipo manja athu ndi riziki ya halal.
Tipatseni kukhutira ndi zimene Mwatipatsa,
ndipo tipatseni zofunika kuchokera ku njira
zimene sititha kuganizira. Ameen