28/01/2026
Today we saw God who lifts the useless, lifting us
Mulungu okweza zonyozeka takumana naye
Mulungu yemwe adakakakokolola Jephtah ku Tobu naye watisuzumila ndipo apitilize kukumana nanu konse komwe muli
Kuli bwino kukanidwa ndi anthu bola udzikondedwa ndi Mulungu, Jephtah abale ake adamukana koma mulungu adamuvomera