African Abraham Church, Chamchere Headquarters

African Abraham Church, Chamchere Headquarters God's Ministry in African Abraham Churches

16/07/2022

Nanga zomati kayambitse wako mpingo monga muja mabishop ena amachitira akapeza munthu kapena mkhristu walephera ku thupi zimatanthauza chani ? Chifukwa
1. Yesu adabwera kudzasaka chotayikacho ndipo chikhala kuti aliyense sachimwa ndiyetu bwezi kulibeko mpingo, choncho kuchotsatu ochimwa mumpingo ndikusunga okhulupirika ndikuona kuti pakukolatu
2. Munthu sangayambitse mpingo koma Yesu yekha
3. Palibe mwini wa mpingo
4. Kodi alipo mu Bible yemwe adachotsedwako mu mpingo ?
Kodi ndikulakwa kunena kuti mkhristu ndi munthu yemwe ndi wochenjera pa kachitidwe ka zinthu ? Chifukwa munthu timamutenga kukhala ochimwa kapena kuti si mkhristu kamba koti uchimo wake watulutsira poyera. Tinene kuti alipo chibadwire yemwe sachimwa? Komano simudayambe mwakhalako pansi nkulingalira kuti anthu amène mumawakhulupirira aja kuseriku amakukhumudwitsani ? Apa ndikufuna mufufuze kuti nanga angapulumuke ndi ndani ? Angapulumuke bwanji ? Nanga chipulumutso ndi chiyani ?

16/07/2022

[16/07, 22:17] Maxwell Peter Chifuniro: Pepani guys sikuwukira komano tithandizane. Ndimakonda kukhala ndi mafunso ndipo ndikukhulupirira kuti malo omwe mayankho angachokere ndi muno
Ndiyeno tatiyeni tiwunikire apa
[16/07, 22:18] Maxwell Peter Chifuniro: *Kodi kumakawalandira a Mgona muja timachitira nthawi zonse zikuchokera mu Bible? Kodi ulemu umene umapita kwa Mulungu bwanji tikupitsa kwa munthu?*
[16/07, 22:30] Maxwell Peter Chifuniro: *Kodi ndi chifukwa chiyani timalanda ndalama munthu akafuna kuyamba nawo mpingo?* *Mesa kodi Yesu adati adaufera mpingo?*
*Nangano bwanji munthu wokayamba nawo akukakamizika kupereka ndalama?*
*Kodi mwana ayenera kubatizidwa?* *, Ngati ndi ayi bwanji izi zikuchitika?*
*Kodi ubatizo ndi chiyani?, Nanga wayenera kuchitika motani?*
*Poti Yesu adati adafera mpingo osati mipingo, ndiye ndi momwe ikuchulukiramu ndiye adafera uti tsopano poti mipingoyi mulimonse imasiyana?, Nanga Kodi mpingo(church) ndi chiyani?*
*Kodi tikamati African Abraham tikutanthauza chani?, Nanga African Abraham Church ndi chiyani?*
*Ngati alipo wina angandifotozere bwinobwino chiyambi cha mpingowu, chonde achite choncho!*
*Mafunso awa akupita konse ku mipingo ya leroliyi osati okhawu chifukwa palibe kusiyana pakati pa mipingo pa dziko la pansi.*
*Kodi Bible limati chani pa nkhani ya mpingo (church)?, Nanga Yesu pomati adafera mpingo amatanthauza chiyani?*
*Zikomo kwambiri pamene mukulingalira mafunsowa ndikupereka mayankho anu*

16/07/2022

Kodi kumakawalandira a Mgona muja timachitira nthawi zonse zikuchokera mu Bible? Kodi ulemu umene umapita kwa Mulungu bwanji tikupitsa kwa munthu?

16/07/2022

Ndibwino kudziwa kuti African Abraham Church ndikulakwa koma kumanena kuti Church in Africa chifukwa the Owner of the church is Jesus Himself not African. The word church has nowadays lost its value and meaning

27/06/2022
25/05/2022

Zanyanya kwambiri moti kumati African Church yomweyi mpakana African chakuti? Kufuna chani kumeneko? God 🙏🙌 come and tell these people the Truth otherwise we'll be mislead

25/05/2022

[17/05, 21:41] Innocent Banda: Per your request, I will be speaking on the subject *THE PLACE
OF THE ANOINTING IN DIVINE ASSIGNMENTS*
[17/05, 21:41] Innocent Banda: It's a subject that will take us days for me to finish. As a matter
of fact, I will be sharing in portions
[17/05, 21:41] Innocent Banda: As I have said, I will focus on *the place of the anointing in
divine assignments.* In other words, I will focus so much on the roles of the anointing in divine
assignments.
[17/05, 21:41] Innocent Banda: One thing that has to be clear is this, *when the proper use of a
thing is not known, people misuse the thing!*
In other words, when purpose is not known, abuse is inevitable.
In the same way, one of the paramount knowledge you need on the subject of anointing is the use
or roles of the anointing. This is because without knowing the uses of the anointing, you will
easily misuse it or wrongly use it.
[17/05, 21:41] Innocent Banda: Understanding the use of the anointing must precede being
anointed.
You need to know that everyone is anointed for a purpose. Without purpose, anointing is never
unleashed.
[17/05, 21:41] Innocent Banda: Luke 4:18 KJV
The Spirit of the Lord is upon me, because he hath anointed me to preach the gospel to the poor;
he hath sent me to heal the brokenhearted, to preach deliverance to the captives, and recovering
of sight to the blind, to set at liberty them that are bruised,
[17/05, 21:41] Innocent Banda: From this scripture, you will notice that Jesus was anointed for a
purpose and He even acknowledged that purpose.
[17/05, 21:41] Innocent Banda: *THE ROLES OR PURPOSES OF THE ANOINTING*

18/02/2022

God is Great

Address

Lilongwe
L

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when African Abraham Church, Chamchere Headquarters posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Place Of Worship

Send a message to African Abraham Church, Chamchere Headquarters:

Share