Mose Wa pa Phiri

Mose Wa pa Phiri Hi people m staying on top of the mountain so there to get network is problem..m staying at MUNDA MOUNTAIN..LILONGWE..MALAWI

Amalawi anzanga ngati mukudalira kuphuzira ndi kucenjera mukutaya nthawi ,, tapenyani conde conde,, tsekulani makutu anu...
19/11/2021

Amalawi anzanga ngati mukudalira kuphuzira ndi kucenjera mukutaya nthawi ,, tapenyani conde conde,, tsekulani makutu anu kuti munvetsere zimene mulungu akufuna kucita ndi dziko amalawi tadzukani conde conde ine sindinaphuzile ngati inu koma ndimamukonda yesu..tayambani kumukonda yesu muona nyengo za dziko lathu la malawi zisintha,palibe comulaka mulungu..ndipo mulungu salakwitsa ai..tamuyesani mulungu muone,mulungu akudalitseni a MALAWI

08/11/2021

Tiyeni timumamatire YEHOVA zabwino ziripo mwa iye

Mwa YESU MBUYE WANGA NDIKUTI ZIIIIIKOOOOOOMOOOOOOO!!!!!!!!!!!!!!
24/10/2021

Mwa YESU MBUYE WANGA NDIKUTI ZIIIIIKOOOOOOMOOOOOOO!!!!!!!!!!!!!!

24/10/2021

Zikomo abale ndi alongo mwa ambuye,kwa amene adziwa mulungu ndi wokhawo amene angavomereze kuti nchito iyi siyanga koma anandituma bwana wa ma mwana ndiye yesu kristu... nchito iyi anandituma ndi mau ocokera pa yesaya 45 tiyeni tiwatsate mau a m'baibulo code conde... iyi ndiye nchito imene anandituma mulungu..kuli konza phiri kukhala mudzi wa YESU kumwamba kulandile ulemu..

Abale ndi alongo yiyeni tilimbike kupemphera pemphero ndi cida coopsya kwambiri tengani citsanzo miyara ikuonekayi ikuph...
21/09/2021

Abale ndi alongo yiyeni tilimbike kupemphera pemphero ndi cida coopsya kwambiri tengani citsanzo miyara ikuonekayi ikuphwanyidwa ndipemphero.mwa mphamvu zanga sizingatheke aiiii koma ukamudalira mulungu opanda cinyengo mulungu amakumvera pa chiri chonse..tiyeni tivale zida za pa chifuwa kuti satana angatinyengerere..tiri mmasiku otsiliza zizindikiro zikuoneka...inu azibusa a GANYUNUndi MAPULOFETI tacepetsani kwanamiza anthu anu, musazoloweze za mulandira muladira muona alandira sataana njerekezi... nthawi yolandilitsana yatha AMBUYE YESU WAIMA PAKHOMO kukonzekera zobwera kudzaweruza adzakupeza colandira kucokera kwa wabodzayo ciri kumanja udzamuyankha ciani YESU?????????

11/05/2021
12/04/2021

Be HAPY with god

MOSE IS HAPY IN HIS GARDEN AT AT THE MOUNTAIN..GOD IS GOOD
27/01/2021

MOSE IS HAPY IN HIS GARDEN AT AT THE MOUNTAIN..GOD IS GOOD

MOSE HIGH WAY.....THE WAY OF HOLLINESS
04/01/2021

MOSE HIGH WAY.....THE WAY OF HOLLINESS

MOSE VILLAGE
03/01/2021

MOSE VILLAGE

Address

Lilongwe

Telephone

+265997810293

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Mose Wa pa Phiri posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share