17/05/2026
Oweruza 15:1- 14
Mulungu anabweletsa wankhondo(Samson), woti amenyane ndi afilisiti amene anali amphamvu panthawi imeneyo.
Pamavuto amene mukukumana nawo mulungu Ali ndi yankho Loti akhoza kutumiza ndikuthana ndi vutolo