06/06/2025
Mulungu amadzionetsera yekha
EKSODO 14:13-14
Mulungu anamuuza mose k*t awuze ana a Israel k*t aziyendabe chitsogolo asacheuke mbuyo
Ndimati ndikambe nanu abale wokondedwa k*t pamene tikukhala mmoyo wasautso tiyeni tisayang'ane mbuyo koma tipitebe chitsogolo pak*t mavuto tikudutsamo leroli simudzawawonaso ingakhale anthu atipeputse bwanj kaya k*tinyoza osadandaula kalikose pak*t Mulungu nthawi zonse amakhala pakati pathu
Limbani mtima, maso Anu penyani kwa Mulungu, Fuulirani kwa iye pak*t ndiko kuli mayankho a nyengo zanu