30/04/2026
CHIKONDI CHAPA MULUNGU
Ephesians 5:2
and live a life of love, just as Christ loved us and gave himself up for us as a fragrant offering and sacrifice to God.
Thawi zambiri chifukwa chosazindikira mphamvu ya chikondi tathawitsa zithu zimene zikanatithandizira kupita chitsogolo ndikusasula misasa yapamoyo wathu,
Chikondi chili ndithambi zitatu zikuluzikulu
1-THAMBI YOSAKHA
Dziko lapansi lisanatisakhe anayamba ndi Mulungu kutisakha posawerengera zofooka zathu,ndipo Muthu Aliyense anasakhidwa ndi Mulungu ndipo zithu zake zonse Mulungu anayikiratu kuti akayendemo,koma Kodi tikuyenda muza Ambuye?
2, THAMBI YAKUPEREKA
Sunganene kuti Muthu umamukonda kapena Mulungu umamukonda koma osamampatsa kalikose.Chikondi chimafuna thawi,Now fuso mkumati ndiliti munapatulako thawi yanu mkuchezako ndi Mulungu nanga ndiliti munachezako ndiwachikondi wanu?
Umaperekaso ngakhare chuma chako chifukwa chomkonda Mulungu
3.KUDZIPEREKA NSEMBE
Mawu akuti tidzipereke nsembe yamatupi athu, ndiliti munaperekako nsembe yamatupi Anu Kwa Mulungu,
Ngat tinena kuti Mulungu timankonda,Mulunguyo amawonaso zimenezi ndipo ndipamene amafika pamoyo wamunthu ndinyengo zotsitsimutsa moyo wanu.
-Ndinu okondedwa, achikondi a MULUNGU onetsani izi nthawi zonse.
BREAKING THE CAMP AND GOING FORWARD