08/07/2026
*Uthenga wa malilo*
Mwachison ndikulengenga za kumwalila kwa okondedwa Deacon chiyembekezo lisongwe wa pa mpingo wa misenza,koma anasamukila ku chidzenje,
Malingana ndi akubanja a priest Emanuel lisongwe Deacon chiyembekezo amwalila mmawa wa lelo pa 08/07/2026,
Dongosolo latsiku loyika ati uzabe akubanja akakhalilana pasi,
Uzimu wa Deacon chiyembekezo uwuse mu mtendele,
Zikomo
Ine Dr stonard madziayenda.