The Mwauka ShoW

The Mwauka ShoW Contact information, map and directions, contact form, opening hours, services, ratings, photos, videos and announcements from The Mwauka ShoW, ginery corner, Chitipa.

NGOZI ZA PA LAKE CHILWAMonga mukudziwa ngozi za pa lake chilwa zimachitikachitika. Mwa zifukwa zina zimene zimachititsa ...
28/05/2026

NGOZI ZA PA LAKE CHILWA
Monga mukudziwa ngozi za pa lake chilwa zimachitikachitika. Mwa zifukwa zina zimene zimachititsa ngozizi ndi monga;

Nyanjayi siyakuya
Lake Chilwa ndi nyanja imodzi imene madzi ake si akuya kuno ku Malawi, izi zimapangitsa kuti ma boat aziyenda movutikila

Mphepo ya ya mwera
Nyanjayi ndi ya flat, ndipo zimapangitsa kuti pazitha kuyamba mafunde mophweka especially ikakhala nthawi ya mvula ndi ya mphepo. Kugwiritsa ntchito ma tima bwato tating'onoting'ono sitichedwa kugudubuzika.

Lake Chilwa ilibe outlet
Izi zimapangitsa kuti mudzadze michenga ndi zomera zimene zimatha kukola mwabwato kuti asamayende bwino kapena kukodwa kumene.

Chifunga
Makamaka usiku kapena mbandakucha,

Chifukwa cha zifukwa izi, Lake Chilwa imatengedwa yoopsa kwambiri kwa anthu ogwiritsa ntchito tima bwato tating'onoting'ono poyerekeza ndi nyanja zina

Wadya ndalama za ichi ndi mwamuna🤣😂 Ine ngati si 2 sms ndekuti ndi 5 sms
28/05/2026

Wadya ndalama za ichi ndi mwamuna🤣😂
Ine ngati si 2 sms ndekuti ndi 5 sms

Visit T&D logde in zombaFor conferencesParty or dinner or hangouts🍻🏘️
27/05/2026

Visit T&D logde in zomba
For conferences
Party or dinner or hangouts🍻🏘️

Bingu wa Mutharika sinali dzina lobadwa nalo, anachita kuzipatsa??Bingu wa Mutharika anabadwa mu 1934 ngati Brightson We...
27/05/2026

Bingu wa Mutharika sinali dzina lobadwa nalo, anachita kuzipatsa??

Bingu wa Mutharika anabadwa mu 1934 ngati Brightson Webster Ryson Thom, dzina limene linali lochokera kwa atsamunda. Bambo ake anali Richard Brightson Thom amene ankagwira ndi azungu ku Tea Estate ndipo mayi ake anali Eleni. Kumudzi kwao kochokela kunali mudzi mwa Kamoto mu boma la Thyolo 🇲🇼. Ndipo anamwalira mu chaka cha 2012. Anaphunzira pa Dedza Secondary School, ndipo anapeza scholarship imene anakachita maphunziro a ukachenjede a degree in Economics mu chaka cha1959 komanso masters degree in Economics mu chaka cha 1963 ku University of Delhi mu dziko la India. Komanso anatenga PhD in Development Economics ku Pacific Western University ya ku USA mu 1985. Mu zaka za 1960, ali ndi zaka zosachepela 26 anasintha dzina lake kukhala Bingu Wa Mutharika kuti lizinveka la chiMalawi osati dzina lokhala la kwa atsamunda mu kakhalidwe kaja mu chizungu amati Pan-Africanism kodana ndi ma ulamuliro atsamunda. Bingu mu Chichewa imatanthauza "Mwana wa" pamene Mutharika linali dzina la mfumu ya kalekale a "mfumu Karonga" ya mu 15 century kale kale kwambiri.
follow ?The Mwauka ShoW ShoW

Komatu Likoma Island pa map imaonetsa kuti ili mu Mozambique?Mu 15th century, Inatchuka ndi za Malonda komanso zipembezo...
25/05/2026

Komatu Likoma Island pa map imaonetsa kuti ili mu Mozambique?

Mu 15th century, Inatchuka ndi za Malonda komanso zipembezo ndi mtundu wa anthu otchedwa 'Nyanja'. Mu 18th century, gulu la zamalonda la Swahili linagundika kwambiri ndi za malonda ao pa malopa. Mu 1861 Dr David Livingstone naye anasangalatsidwa ndi kukongola kwa Likoma island. Komano mu zaka za 1890's Britain imene inkalamulira Malawi komanso Portugal imene inkalamulira Mozambique anakokana malaya pa umwini wa chilumba chimenechi. Panadziwika kuti Britain, inkafuna malowa chifukwa anali pakati pa nyanja ya Lake Nyasa, pamene Portugal inkafuna malowa pazifukwa zoziwa okha, koma ena anakhulupirira kuti Portugal inkafuna kuzikuzira malire komanso mphamvu. Mu chaka cha 1891, maiko awiriwa anachita zokambilana zimene anazitcha,The Anglo-portuguese treaty zimene zinapereka malowa. Ku mbali ya Britain pa zokambiranazi, kunali a Foreign Secretary Lord Salisbury 🇬🇧 pamene ku mbali ya Portugal kunali Minister António de Serpa Pimentel 🇵🇹. Mpingo wa Universities Mission to Central Africa (UMCA) ndi umene unathandizira kwambiri kuti Britain itenge malowa chifukwa unali ndi zochika zina pa malowa, nde sumafuna kulamuliridwa ndi ma Portuguese. Mu 20th Century, mpingo wa Anglican ndi umene unali woyamba kuzamanga pa Likoma island. Kufikira pano Likoma ili ndi anthu ochuluka a chipembezo cha chi khristu kuposa zipembezo zina. Dziko la malawi litatenga ufulu wozilamulira palokha, malowa anapitilira kukhala ku mbali ya dziko la Malawi, komano ojambula map sanasinthebe za mizere imene amaitcha international boundaries, imene imaonetsabe kuti Likoma ili mu Mozambique.
Follow this page kuti muzimva ma history obeba aja Mwauka SHOW

21/05/2026
Mayekete olowera live pa tiktok🤣🤣
21/05/2026

Mayekete olowera live pa tiktok🤣🤣

If you fail it doesn't mean it's impossible keep believing💪
20/05/2026

If you fail it doesn't mean it's impossible keep believing💪

Don't post every single achievement Keep your secret and surprise many🏆The Mwauka ShoW
20/05/2026

Don't post every single achievement
Keep your secret and surprise many🏆
The Mwauka ShoW

Address

Ginery Corner
Chitipa

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when The Mwauka ShoW posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share