New Jerusalem Pentecost Church

New Jerusalem Pentecost Church ITS GOD'S FAVOUR TO BRING US TO THIS LAND,GET ASSISTED IN PRAYERS,,,ITS TIME FOR GOD TO OVERCOME ALL BONDAGES

Good To Those Who Walk With God For Everything Becames Simple And Easy

THE MUCH AWAITED DAY...
27/12/2020

THE MUCH AWAITED DAY...

29/09/2020

Dates for our Annual general cruisade and Baptism ceremony has been shifted from 23rd october to 08th November 2020.

God bless you

12/06/2020

To God our Lord be the glory. Amen

05/05/2020

May the Restoration power from the almighty God reach you throughout this lockdown period.

God bless you

01/05/2020

Only God can help get rid of this virus, prayers will work...
Stay safe. Prevent the spread..

Remember always...
Prayer is the only weapon that can kill this virus....

03/04/2020

*MPINGO WA NEW JERUSALEM PENTECOST M'MALAWI 🇲🇼

_*Nthenda yoopya ndiso njira Zake zothanira nawo*_

*pemphero*

_Mulungu WA Ana a Israeli, Musaliiwale dziko lapansi, Musaliiwale dziko LA Malawi 🇲🇼. Tithandizeni ndukutichiritsa Tonse. Amen._

*_Uneneri WA yeremia zamthendayi_*
*_Yeremia 16 vs 1-12_*
1Ndiponso mau a Mulungu anadza kwa ine, kuti, 2Usatenge mkazi, usakhale ndi ana amuna ndi akazi m'malo muno. 3Pakuti Yehova atero za ana amuna ndi za ana akazi akubadwa m'malo muno, ndi za amai anawabala iwo, ndi za atate ao anawabala iwo m'dziko muno: 4Adzafa ndi imfa zanthenda; sadzaliridwa maliro, sadzaikidwa; adzakhala ngati ndowe panthaka; ndipo adzathedwa lupanga, ndi njala; ndipo mitembo yao idzakhala cakudya ca mbalame za kumlengalenga, ndi zirombo za dziko lapansi. 5Pakuti Yehova atero, Usalowe m'nyumba ya maliro, usanke kukacita maliro ao, kapena kuwalirira; pakuti ndacotsa mtendere wanga pa anthu awa, cifundo ndi nsoni zokoma, ati Yehova. 6Akuru ndi ang'onong'ono adzafa m'dziko muno; sadzaikidwa, anthu sadzacita maliro ao, sadzadziceka, sadzadziyeseza adazi, cifukwa ca iwo; 7anthu sadzawagawira mkate pamaliro, kuti atonthoze mitima yao cifukwa ca akufa, anthu sadzapatsa iwo cikho ca kutonthoza kuti acimwe cifukwa ca atate ao kapena mai wao. 8Usalowe m'nyumba ya madyerero kukhala nao, ndi kudya ndi kumwa. 9Pakuti atero Yehova wa makamu, Mulungu wa Israyeli; Taonani, ndidzaletsa pano, pamaso panu masiku anu, mau akukondwerera ndi mau akusangalala, mau a mkwati ndi mau a mkwatibwi. 10Ndipo padzakhala, pamene udzaonetsa anthu awa mau awa onse, ndipo iwo adzati kwa iwe, Cifukwa cace nciani kuti Yehova watinenera ife coipa cacikuru ici? mphulupulu yathu ndi yanji? cimo lathu lanji limene tacimwira Yehova Mulungu wathu? 11Pamenepo uziti kwa iwo, Cifukwa makolo anu anandisiya Ine, ati Yehova, natsata milungu yina, naitumikira, naigwadira, nandisiya Ine, osasunga cilamulo canga; 12ndipo mwacita zoipa zopambana makolo anu; pakuti, taonani, muyenda yense potsata kuumirira kwa mtima wace woipa, kuti musandimvere Ine.

*NJIRA ZOTHANIRA NAWO*

*_2Mbiri 7: 14_*

14ndipo anthu anga ochedwa dzina langa akadzicepetsa, nakapemphera, nakafuna nkhope yanga, nakatembenuka kuleka njira zao zoipa; pamenepo ndidzamvera m'Mwamba, ndi kukhululukira coipa cao, ndi kuciritsa dziko lao.

*_Yesaya 43: 4-7_*

4Pokhala iwe wa mtengo wapatari pamaso panga, ndi wolemekezeka, ndipo ndakukonda iwe; Ine ndidzakuombola ndi anthu, ndi kupereka anthu m'malo mwa moyo wako. 5Usaope; pakuti Ine ndiri ndi iwe; ndidzatenga mbeu zako kucokera kum'mawa, ndi kusonkhanitsa iwe kucokera kumadzulo. 6Ine ndidzati ndi kumpoto, Pereka; ndi kumwera, Usaletse; bwera nao ana anga amuna kucokera kutari, ndi ana anga akazi kucokera ku malekezero a dziko lapansi; 7yense wochedwa dzina langa, amene ndinamlenga cifukwa ca ulemerero wanga; ndinamuumba iye; inde, ndinampanga iye.

_*2Mbiri 30: 18-20*_

18Pakuti, anthu aunyinji, ndiwo ambiri a Efraimu, ndi Manase, Isakara, ndi Zebuloni, sanadziyeretsa, koma anadya Paskha mosati monga munalembedwa. 19Koma Hezekiya anawapempherera, ndi kuti, Yehova wabwino akhululukire yense wakuika mtima wace kufuna Mulungu Yehova, Mulungu wa makolo ace, cinkana sanayeretsedwa monga mwa mayeretsedwe a malo opatulika. 20Ndipo Yehova anamvera Hezekiya, nawaciritsa anthu.

*_Deuteronomy 7:15_*

15Ndipo Yehova adzakucotserani nthenda zonse; sadzakuikirani nthenda zoipa ziri zonse za Aigupto muzidziwa zija; koma adzaziika pa onse akudana ndi inu.

*PHUNZIRO*

Nthawi zonse tikhale omvetsera, timvere ndinso Kupempha kwa Mulungu pa China chilichonse. Mulungu ndiothekera..... Kumbukirani kuti muzu wa mavuto ndi nyengo zonse za nsautso ndi kusamvera, kukonda Ndalama ndi dzina.
Tilole Mulungu atithandize ndikupatsa madalitso ndi ulemerelo omwe adalonjeza kukenani. Dziko lino sikwathu, tiyeni tikhale ngati alendo, pakuti posachedwa, tichoka padziko pano kuloza kuchiweruzilo. Tikhale odekha ndi ofatsa muchilichonse, tipemphere chipambano kuzera kwa Yehova. Ndithudi Malawi apulumutsidwa ku mtenda ya Covid 19.

Kuchokera ku banja LA mpingo WA New Jerusalem Pentecost pansi pa ulamuliro WA BP Rev Peter kachulu ndi Senior Pastor Wyson.
Tikufunirani umoyo wathanzi ndikukulimbikitsani kusamila kwa yehova nthawi zonse. Dana nachoni choyipa.

Monga mwa malemba........

*_1samueli 25: 6_*

6ndipo muzitero kwa wodalayo, Mtendere ukhale pa inu, mtendere ukhalenso pa nyumba yanu, ndi mtendere ukhale pa zonse muli nazo.

Amen.

03/04/2020

NEW JERUSALEM PENTECOST CHURCH OF MALAWI 🇲🇼
*DEADLY DISEASE AND ITS SOLUTION*

*Prayer*
_God of Israel, Do not forsake The world, Do not forsake Malawi🇲🇼, help and heal us all. Amen_

*Jeremiah's Prophesy about the disease*
*_Jeremiah 16 vs 1-12_*
1 Then the word of the LORD came to me:

2 "You must not marry and have sons or daughters in this place."

3 For this is what the LORD says about the sons and daughters born in this land and about the women who are their mothers and the men who are their fathers:

4 "They will die of deadly diseases. They will not be mourned or buried but will be like refuse lying on the ground. They will perish by sword and famine, and their dead bodies will become food for the birds of the air and the beasts of the earth."

5 For this is what the LORD says: "Do not enter a house where there is a funeral meal; do not go to mourn or show sympathy, because I have withdrawn my blessing, my love and my pity from this people," declares the LORD.

6 "Both high and low will die in this land. They will not be buried or mourned, and no one will cut himself or shave his head for them

7 No one will offer food to comfort those who mourn for the dead--not even for a father or a mother--nor will anyone give them a drink to console them.

8 "And do not enter a house where there is feasting and sit down to eat and drink.

9 For this is what the LORD Almighty, the God of Israel, says: Before your eyes and in your days I will bring an end to the sounds of joy and gladness and to the voices of bride and bridegroom in this place.

10 "When you tell these people all this and they ask you, 'Why has the LORD decreed such a great disaster against us? What wrong have we done? What sin have we committed against the LORD our God?'

11 then say to them, 'It is because your fathers forsook me,' declares the LORD, 'and followed other gods and served and worshiped them. They forsook me and did not keep my law.

12 But you have behaved more wickedly than your fathers. See how each of you is following the stubbornness of his evil heart instead of obeying me.

*SOLUTIONS*

*2Chronicles 7:14*

if my people, who are called by my name, will humble themselves and pray and seek my face and turn from their wicked ways, then will I hear from heaven and will forgive their sin and will heal their land.

*Isaiah 43:4-7*

Since you are precious and honored in my sight, and because I love you, I will give men in exchange for you, and people in exchange for your life.
5 Do not be afraid, for I am with you; I will bring your children from the east and gather you from the west.
6 I will say to the north, 'Give them up!' and to the south, 'Do not hold them back.' Bring my sons from afar and my daughters from the ends of the earth--
7 everyone who is called by my name, whom I created for my glory, whom I formed and made

*2chronicles 30 vs 18-20*

18 Although most of the many people who came from Ephraim, Manasseh, Issachar and Zebulun had not purified themselves, yet they ate the Passover, contrary to what was written. But Hezekiah prayed for them, saying, "May the LORD, who is good, pardon everyone
19 who sets his heart on seeking God--the LORD, the God of his fathers--even if he is not clean according to the rules of the sanctuary."
20 And the LORD heard Hezekiah and healed the people.

*Deuteronomy 7:15*

The LORD will keep you free from every disease. He will not inflict on you the horrible diseases you knew in Egypt, but he will inflict them on all who hate you.

*Lesson...*

Always listen, obey and ask God in everything. God is more than able... Remember the cause of every bad situation today is disobedient, love for money and many others.
Let God help us and bring us the Glory he promised us in the land of Canaan... This world is not our home, let's behave as visitors, for no sooner we will leave this world and face judgment. Be patient in everything, seek the presence of God.. Malawi will be saved from this Covid 19.

From the family of New Jerusalem Pentecost Church under the leadership of BP Rev Peter kachulu, and S. PS Wyson.
We wish you a good health and encourages you to always cling to God, abhor to what is evil.
According to.....
*1Samuel 25:6*

_*Say to him: 'Long life to you! Good health to you and your household! And good health to all that is yours!*_
Amen.

03/04/2020

NEW JERUSALEM PENTECOST CHURCH OF MALAWI 🇲🇼
*DEADLY DISEASE AND ITS SOLUTION*

*Prayer*
_God of Israel, Do not forsake The world, Do not forsake Malawi🇲🇼, help and heal us all. Amen_

*Jeremiah's Prophesy about the disease*
*_Jeremiah 16 vs 1-12_*
1 Then the word of the LORD came to me:

2 "You must not marry and have sons or daughters in this place."

3 For this is what the LORD says about the sons and daughters born in this land and about the women who are their mothers and the men who are their fathers:

4 "They will die of deadly diseases. They will not be mourned or buried but will be like refuse lying on the ground. They will perish by sword and famine, and their dead bodies will become food for the birds of the air and the beasts of the earth."

5 For this is what the LORD says: "Do not enter a house where there is a funeral meal; do not go to mourn or show sympathy, because I have withdrawn my blessing, my love and my pity from this people," declares the LORD.

6 "Both high and low will die in this land. They will not be buried or mourned, and no one will cut himself or shave his head for them

7 No one will offer food to comfort those who mourn for the dead--not even for a father or a mother--nor will anyone give them a drink to console them.

8 "And do not enter a house where there is feasting and sit down to eat and drink.

9 For this is what the LORD Almighty, the God of Israel, says: Before your eyes and in your days I will bring an end to the sounds of joy and gladness and to the voices of bride and bridegroom in this place.

10 "When you tell these people all this and they ask you, 'Why has the LORD decreed such a great disaster against us? What wrong have we done? What sin have we committed against the LORD our God?'

11 then say to them, 'It is because your fathers forsook me,' declares the LORD, 'and followed other gods and served and worshiped them. They forsook me and did not keep my law.

12 But you have behaved more wicked

Address

Box 14, Mikolongwe, Thyolo
Blantyre

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when New Jerusalem Pentecost Church posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Place Of Worship

Send a message to New Jerusalem Pentecost Church:

Share