Malawi Assemblies of God

Malawi Assemblies of God Michiru Glorious Grace Assembly

I pray for you to be free from any kind of evil bo***ge  in Jesus name.
22/02/2026

I pray for you to be free from any kind of evil bo***ge in Jesus name.

20/02/2026

Isaiah : 58 : 1-11
1. “Fuwula kwambiri, usaleke. Mawu ako amveke ngati lipenga. Uwawuze anthu anga za kulakwa kwawo; uwuze nyumba ya Yakobo za machimo awo.
2. Pakuti tsiku ndi tsiku amafunafuna Ine; amaoneka ngati a chidwi chofuna kudziwa zimene ndimafuna, kukhala ngati kuti ndi dziko limene limachita zolondola ndipo silinasiye zolamulira za Mulungu wake. Amandipempha kuti ndigamule mlandu wawo mwachilungamo ndipo amaonetsa chidwi chofuna kukhala pafupi ndi Mulungu.
3. Anthu akufunsa kuti, ‘Chifukwa chiyani ife tasala kudya pamene Inu simukulabadirapo? Kodi ife tavutikiranji nʼkudzichepetsa pamene Inu simunasamalepo?’ ” Yehova akuti, “Komatu tsiku lanu losala kudya, mumachita zinthu zokukondweretsani, ndipo mumazunza antchito anu onse.
4. Mumati uku mukusala kudya, uku mukukangana ndi kumenyana, mpaka kumenyana ndi nkhonya zopweteka. Kusala kudya mukuchitiramu musayembekezere kuti mawu anu amveka kumwamba.
5. Kodi kusala kudya kumene ndimakufuna Ine nʼkumeneku, kungokhala tsiku loti munthu adzichepetse basi? Kodi ndi tsiku loti munthu angowerama pansi ngati bango ndi kumayala ziguduli nʼkuthirapo phulusa nʼkugonapo? Kodi ndiye mumati kusala kudya kumeneko, tsiku lokondweretsa Yehova?
6. “Kodi si uku kusala kudya kumene Ine ndimakufuna: Kumasula maunyolo ozunzizira anthu ndi kumasula zingwe za goli, kupereka ufulu kwa oponderezedwa ndi kuphwanya goli lililonse?
7. Anthu anjala kodi mwawagawira chakudya chanu? Osowa ndi ongoyendayenda, kodi mwawapatsa malo ogona? Munthu wausiwa kodi mwamupatsa chovala?
8. Mukatero chipulumutso chanu chidzabwera ngati mʼbandakucha, ndipo mabala anu adzachira msangamsanga; chilungamo chanu chidzakutsogolerani ndipo ulemerero wa Yehova udzakhala chokutchinjirizani kumbuyo kwanu.
9. Mukamadzapemphera Yehova adzakuyankhani; mukadzapempha thandizo, Iye adzati: Ine ndili pano. “Ngati muleka kuzunza anzanu, ngati musiya kuloza chala ndiponso kunena zoyipa za anzanu.
10. Ndipo ngati mudyetsa anthu anjala, ndi kuthandiza anthu oponderezedwa, p

19/02/2026

Jesus Christ is real

Heaven is real

Hell is real.

Repent now and start following the foot steps of Jesus Christ.

19/02/2026

Romans 8:15

For you did not receive a spirit that makes you a slave again to fear, but you received the Spirit of sonship. And by him we cry, "Abba, Father."

Mzimu amene inu munalandira samakusandutsani akapolo, kuti muzikhalanso amantha, koma Mzimu amakusandutsani ana. Ndipo mwa Iye ife timafuwula kuti, “Abba, Atate.”

You are all invited to this conference.
08/12/2025

You are all invited to this conference.

11/08/2025

Good morning everyone wherever you are.

You're are all invited to the Easter Conference.
30/03/2025

You're are all invited to the Easter Conference.

12/03/2024

Can I see the✋ hands for those who are blessed with us here and they are willing to see us in Botswana.

Raise up your hand please

🔥🔥🔥🔥

You are most welcome to the Easter Conference.
08/03/2024

You are most welcome to the Easter Conference.

Address

Blantyre

Telephone

+265996302028

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Malawi Assemblies of God posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share