03/06/2026
Afilipi 4:13
Ndikhoza zonse mwa iye wondipatsa mphamvuyo
Ukakhala ndikhumbo lofunisisa kupezeka kwa Mulungu Moyo mwako, kuzakhala kosavuta kulandira mayankho ukapemphera kwa Mulungu.
Khalani chifupi ndi Mulungu kuyambira pano.
Mu Dzina la Yesu.