Life Ambassodors International Ministries

Life Ambassodors International Ministries Prophet Goodson Jeshua, The Founder And President
(1)

Afilipi 4:13Ndikhoza zonse mwa iye wondipatsa mphamvuyoUkakhala ndikhumbo lofunisisa kupezeka kwa Mulungu Moyo mwako, ku...
03/06/2026

Afilipi 4:13
Ndikhoza zonse mwa iye wondipatsa mphamvuyo

Ukakhala ndikhumbo lofunisisa kupezeka kwa Mulungu Moyo mwako, kuzakhala kosavuta kulandira mayankho ukapemphera kwa Mulungu.
Khalani chifupi ndi Mulungu kuyambira pano.
Mu Dzina la Yesu.

Mateyu 12:37Pakuti udzayesedwa wolungama ndi mau ako, ndipo ndi mau ako omwe udzatsutsidwaZingavutute motani, osafika po...
02/06/2026

Mateyu 12:37
Pakuti udzayesedwa wolungama ndi mau ako, ndipo ndi mau ako omwe udzatsutsidwa

Zingavutute motani, osafika pozitembelera, kutheka ulendo wanu moyo uno ukuwoneka ovuta koma Dziwa kuti Yehova adziwa bwino mawa lako.
Zilibwino ndi moyo wako.

JUNEWelcome to the new month of June. Filled with new opportunities waiting to be siezed. A new month with a new show se...
01/06/2026

JUNE

Welcome to the new month of June.
Filled with new opportunities waiting to be siezed.

A new month with a new show season on the way, we pray this month will be everything you've wanted and more.
In Jesus name.

Prophet Goodson Jeshua

Mulungu Akupulumuseni Kuzowawa Zamoyo wanu. mu Dzina la Yesu
31/05/2026

Mulungu Akupulumuseni Kuzowawa Zamoyo wanu.
mu Dzina la Yesu

Masalmo 23:6Inde ukoma ndi cifundo zidzanditsata masiku onse a moyo wangaNdipo ndidzakhala m'nyumba ya Yehova masiku ons...
29/05/2026

Masalmo 23:6
Inde ukoma ndi cifundo zidzanditsata masiku onse a moyo wanga
Ndipo ndidzakhala m'nyumba ya Yehova masiku onse

Tito 1:15Zonse ziyera kwa iwo amene ayera mtima; koma kwa iwo odetsedwa ndi osakhulupira kulibe kanthu koyera; komatu za...
28/05/2026

Tito 1:15
Zonse ziyera kwa iwo amene ayera mtima; koma kwa iwo odetsedwa ndi osakhulupira kulibe kanthu koyera; komatu zadetsedwa nzeru zao ndi cikumbu mtima cao

NZERU IPOSA ZIDA NKHONDO Yakobo 1:5Koma wina wa inu ikamsowa nzeru, apemphe kwa Mulungu, amene apatsa kwa onse modzala m...
27/05/2026

NZERU IPOSA ZIDA NKHONDO

Yakobo 1:5
Koma wina wa inu ikamsowa nzeru, apemphe kwa Mulungu, amene apatsa kwa onse modzala manja, niwosatonza; ndipo adzampatsa iye

Mateyu 11:28Idzani kuno kwa Ine nonsenu akulema ndi akuthodwa, ndipo Ine ndidzakupumulitsani inu. 29Senzani gori langa, ...
25/05/2026

Mateyu 11:28
Idzani kuno kwa Ine nonsenu akulema ndi akuthodwa, ndipo Ine ndidzakupumulitsani inu. 29Senzani gori langa, ndipo phunzirani kwa Ine; cifukwa ndiri wofatsa ndi wodzicepetsa mtima: ndipo mudzapeza mpumulo wa miyoyo yanu.
30 Pakuti gori langa liri lofewa, ndi katundu wanga ali wopepuka

Ngakhale zovuta za moyo uno nzambiri, koma thawira kwa Yesu ndipo Mulungu azakupulumutsa.
Mtulire Yesu lero.
Hallelujah

Yohane 15:7Ngati mukhala mwa Ine, ndi mau anga akhala mwa inu, pemphani cimene ciri conse mucifuna ndipo cidzacitika kwa...
22/05/2026

Yohane 15:7
Ngati mukhala mwa Ine, ndi mau anga akhala mwa inu, pemphani cimene ciri conse mucifuna ndipo cidzacitika kwa inu

Zinthu zambiri kuti zikhazikike pamoyo wanu.
Nthawi zina sizifuna kukakamiza koma Kuchita chifuniro cha Mulungu.
Ngati ukuyenda molingangana ndi mawu a Mulungu zambiri zimachitika mwa Automatic.
Mulungu akuchitileni chachilendo mu Dzina la Yesu.

Yoweli 2:25Ndipo ndidzakubwezerani zaka zidazidya dzombe, ndi cirimamine, ndi anoni, ndi cimbalanga, gulu langa lalikuru...
21/05/2026

Yoweli 2:25
Ndipo ndidzakubwezerani zaka zidazidya dzombe, ndi cirimamine, ndi anoni, ndi cimbalanga, gulu langa lalikuru la nkhondo, limene ndinalitumiza pakati pa inu

Osalira pa zimene udataya.
Mulungu wathu ndi wobwezeretsa.
Lero, Ambuye akuyendere!
Mu Dzina La Yesu

Address

Mulanje
Blantyre

Telephone

+265888088544

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Life Ambassodors International Ministries posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Place Of Worship

Send a message to Life Ambassodors International Ministries:

Share