15/04/2026
*MALAWI ISLAMIC ARTS*
Malawi Islamic Arts ndi tsamba lomwe limathandiza Achinyamata aluso kuti afikile anthu ochuluka mukamphindi kochepa ndipo ndi tsamba lokhalo la pa internet lomwe lili ngati nkhokwe yopezela mitsangalutso yosiyana siyana komanso Zina zokhudza Chikhululupiliro Cha Chisilamu.
Monga mukudziwa tsambali limapezeka ndi zinthu Monga:
- Ma Ulaliki (Bayan)
- Quran (yotanthauzila muchichewa komaso Chizungu
- Ndakatulo
- Ma Nasheed
ndizina zambili.
Pakufuna kupitiliza ndi zintchito zimenezi komaso Kuthandiza Achinyamata aluso muno MMalawi, tsopano pa tsambali Achinyamata Aluso atha Kutsekula account yomwe iziwapatsa mwayi opanga:
1. Kuika zinthu pa Internet (Mwaokha
2. Kugulitsa komaso kukhazikitsa mitengo ya Ma luso awo
3. Kuona momwe Maluso awo akuchitila patsambali monga kuona chiwelengelo Cha ovela, Ogula komaso omwe apanga download Maluso awo.
4. Kutha kulumikizitsa zinthu zawo ndi tsamba la *YouTube* kuti zisavute kagawidwe.
Zakhale nafe Limodzi pa Mkumano wapa Internet omwe tizakhale tikuonetsa kaonekedwe Ka tsopano Ka website komanso Kuphunzitsa kapangidwe upload kazinthu zanu.
Tsikundi pa *25 April* kudzera pa *Google Meet.*
Kuti mudziwe zambili tipeze pa
WhatsApp: +265 998 737 873
Malawi Islamic Arts
Provision of dhikr through Arts