22/08/2024
Civumbutso 19 v 10
Pakuti umboni ya Yesu christ ndi mzimu "wakunenera"
mawu oti "kunenera" mukunena kwina ndikoti "kuchitira umboni",mvesera mulungu(YEHOVAH) akachita zinthu pa moyo wako,iwe mwini ndikumati ambuye ndapambana bwanji ineyo kuti munditere,amakhakuti akukupanga iwe kukhala mboni yodalirika ya uthenga wabwino kwa anthu onse