Living Faith Ministries International-LIFAM

Living Faith Ministries International-LIFAM Miracles, blessings and healings of Jesus Christ should be with you.
•Preaching about the end time, salvation of mankind has come through Jesus Christ.

KUFUNIKIRA KWA MAPEPHERO A UTSIKUMateyu 25:1-10 (bukhu lopatulika)Pomwepo Ufumu wa Kumwamba udzafanizidwa ndi anamwali k...
09/01/2026

KUFUNIKIRA KWA MAPEPHERO A UTSIKU

Mateyu 25:1-10 (bukhu lopatulika)

Pomwepo Ufumu wa Kumwamba udzafanizidwa ndi anamwali khumi, amene anatenga nyali zao, natuluka kukakomana ndi mkwati. 2Ndipo asanu a iwo anali opusa, ndi asanu anali ochenjera. 3Pakuti opusawo, m'mene anatenga nyali zao, sanadzitengeranso mafuta; 4koma anzeruwo anatenga mafuta m'nsupa zao, pamodzi ndi nyali zao. 5Ndipo pamene mkwati anachedwa, onsewo anaodzera, nagona tulo. 6Koma pakati pa usiku panali kufuula, Onani, mkwati! Tulukani kukakomana naye. 7Pomwepo anauka anamwali onse amenewo, nakonza nyali zao. 8Ndipo opusa anati kwa ochenjera, Tipatseniko ena a mafuta anu; chifukwa nyali zathu zilikuzima. 9Koma ochenjera anayankha nati, Kapena sangakwanire ife ndi inu; koma makamaka mukani kwa ogulitsa malonda, mukadzigulire inu nokha. 10Ndipo pamene iwo analikumuka kukagula, mkwati anafika; ndipo okonzekawo analowa naye pamodzi muukwati; ndipo anatseka pakhomo.

-Apapa tikuona kuti mkwati anafika pakati pa usiku, pakati pa usiku ndi pamene pamachitika zithu zambiri, Paulo ndi Sila ali mu ndende anapephera ndipo pakati pa usiku ndi pamene zitseko zinaseguka, ndipo maunyolo a mmanja ndi mmapazi anaduka.
Pakati pa usiku maunyolo amaduka, pakati pa usiku zitseko zimatha kutseguka kapena kukhala zotsekeka.

-Mu Mateyu 25:10 tikuona kuti anamwali khumi opusa aja ali kogula mafuta, chitseko chinasekeka ndipo sanakwanitse kulowa, chitseko choboleza chanu chitha kusekeka kapena kuseguka pakati pa usiku, anamwali khumi opusa chinasekeka, pomwe Paulo ndi Sila ali mu ndende pakati pa usiku chiseko chinaseguka,,, osati chinangoseguka chokha ai, koma anapephera ndi kuimba nyimbo zoyamika Mulungu.

-Inuyo pamene muli otanganidwa ndi kugona, otanganidwa ndikupita kogula mafuta ngati anamwali asanu opusa aja, chitseko chanu chimakhala chikusekedwa. Pomwe pamene mukhala mukupephera ndi kuimba nyimbo zoyamika Mulungu, chitseko chanu chimakhala chikuseguka....

-Anthu ambiri saziwa kufunika kodzuka utsika ndikupephera,, makamaka kumayambiriro a chaka, izizi zimathandiza kuti chiseko choboleza chanu chikhale chosegulidwa chaka chonse, mwezi uno wa Januwale ndi ofunika kwambiri chifukwa ndi mwezi oyamba,, ndi mwezi omwe timayenera kupatulira pamaso pa Mulungu...ndi kupephera ndi kutsala kudya. Ndi mwezi omwe timapuputha thupi lathu pamaso pa Mulungu.

-Ndi pephero ndi pembezero langa kuti chitseko chanu cha madalitso ndi kuboleza chikhale chotsegula chaka chonse chino cha 2026, zomwe mwakhala mukulephera kukwaniritsa mu 2025, mukwaniritsa mopweka kwambiri mu chaka chino cha 2026, chaka cha kudzoza kwatsopano, chaka chimene mulandire zithu zimene simunaganizepo...

-Chaka chimene mukalilira kwa Ambuye Yesu, azikuyankhani.

Ambuye Yesu akudalitseni nonse.
Amen

HEAR WORD OF GOD AND BE HEALED!!
07/10/2025

HEAR WORD OF GOD AND BE HEALED!!

Cain killed Abel, not because Abel wronged him or they were fighting, NO, but because Cain cannot stand FAVOUR OF GOD in...
25/05/2025

Cain killed Abel, not because Abel wronged him or they were fighting, NO, but because Cain cannot stand FAVOUR OF GOD in life of Abel.

Listen, why are people fighting you?
Have you wronged them?
Answer is NO, you have not wronged them nor you are problem, but because those people fighting you CANNOT STAND FAVOUR of God in your life.

Why are people blackmailing you?
Because you have God's favour that they cannot stand.

Never stress yourself because of those fighting you, know that you are favoured.

Never be shaken, stand firm in the sight of God.

(pic credit-Men's day at Chirimba Church in Blantyre-Malawi)

GENESIS 1:26God gave you authority over the spirits of the waters (mermaid spirits), spirits wandering in airs, and spir...
20/05/2025

GENESIS 1:26
God gave you authority over the spirits of the waters (mermaid spirits), spirits wandering in airs, and spirits of the land of the dark powers of this age.

Command they out of your life, command them out of your financial areas.
Be free in Jesus name!!

Whosoever has been anointed with evil tongue to speak evil against your life, destiny, marriage, business, work, career,...
10/02/2025

Whosoever has been anointed with evil tongue to speak evil against your life, destiny, marriage, business, work, career, I command fire from above to consume them in Jesus name!!!

There will come a time when your tears will fall, not because of problems, but because God has answered your prayers.
10/02/2025

There will come a time when your tears will fall, not because of problems, but because God has answered your prayers.

05/02/2025

In 2025, attempt great things for God.

04/11/2023
It looks impossible, that one egg can produce two yolks, right?It is unmaginable to have two yolks in an egg, is it?The ...
03/11/2023

It looks impossible, that one egg can produce two yolks, right?

It is unmaginable to have two yolks in an egg, is it?

The blessing coming your way, are beyond human imagination.
What no eye has seen,
What no ear has heard,
And what no human mind has conceived, are blessings that God has prepared for you.

Don't lose hope, keep on praying.

It is not over because God is not yet done with you!!There is something great!!!
26/08/2023

It is not over because God is not yet done with you!!
There is something great!!!

Address

Limbe
Blantyre
HOLYSPIRIT@WORK

Telephone

+265999720993

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Living Faith Ministries International-LIFAM posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Place Of Worship

Send a message to Living Faith Ministries International-LIFAM:

Share