Bible Society of Malawi

Bible Society of Malawi God's Word, Life for All. Mau a Mulungu Ndiwo Moyo Kwa Onse.
(1)

Pakuti tsiku limodzi m'mabwalo anu likoma koposa masiku ambirimbiri akukhala pena.Masalimo 84:10
24/05/2026

Pakuti tsiku limodzi m'mabwalo anu likoma koposa masiku ambirimbiri akukhala pena.

Masalimo 84:10

Ndikhoza kuchita zonse kudzera mwa Iye amene amandipatsa mphamvu.Afilipi 4:13
23/05/2026

Ndikhoza kuchita zonse kudzera mwa Iye amene amandipatsa mphamvu.

Afilipi 4:13

Ife timakhala mwachikhulupiriro, osati mwa zooneka ndi maso.2 Akorinto 5:7
22/05/2026

Ife timakhala mwachikhulupiriro, osati mwa zooneka ndi maso.

2 Akorinto 5:7

Mulungu ndiye kothawira kwathu ndi mphamvu yathu,thandizo lopezekeratu pa nthawi ya mavuto.Masalimo 46:1
21/05/2026

Mulungu ndiye kothawira kwathu ndi mphamvu yathu,
thandizo lopezekeratu pa nthawi ya mavuto.

Masalimo 46:1

Koposa zonse muzikondana wina ndi mnzake kwambiri, chifukwa chikondi chimaphimba machimo ambiri. 1 Petro 4:8
19/05/2026

Koposa zonse muzikondana wina ndi mnzake kwambiri, chifukwa chikondi chimaphimba machimo ambiri.

1 Petro 4:8

Makhalidwe ochitira ena chifundo ndi owonetsa kukhulupirika asakuchokere.Uwamangirire mʼkhosi mwako ngati mkanda ndi kuw...
18/05/2026

Makhalidwe ochitira ena chifundo ndi owonetsa kukhulupirika asakuchokere.
Uwamangirire mʼkhosi mwako ngati mkanda ndi kuwalemba pa mtima pako. Ukatero udzapeza kuyanja ndi mbiri yabwino pamaso pa Mulungu ndi anthu.

Miyambo 3:3-4

Tiziganizira mmene tingalimbikitsirane wina ndi mnzake pokondana ndi kuchita ntchito zabwino. Tiyeni tisaleke kusonkhana...
17/05/2026

Tiziganizira mmene tingalimbikitsirane wina ndi mnzake pokondana ndi kuchita ntchito zabwino. Tiyeni tisaleke kusonkhana kwathu pamodzi monga mmene ena amachitira, koma tizilimbikitsana

Ahebri 10:24-25

Ndipo popanda chikhulupiriro nʼkosatheka kukondweretsa Mulungu, chifukwa aliyense amene amabwera kwa Iye ayenera kukhulu...
16/05/2026

Ndipo popanda chikhulupiriro nʼkosatheka kukondweretsa Mulungu, chifukwa aliyense amene amabwera kwa Iye ayenera kukhulupirira kuti Mulungu alipodi ndi kuti Iye amapereka mphotho kwa amene akumufunitsitsa.

Ahebri 11:6

Mukomerane mtima ndi kuchitirana chifundo wina ndi mnzake. Khululukiranani wina ndi mnzake, monga momwe Mulungu anakukhu...
15/05/2026

Mukomerane mtima ndi kuchitirana chifundo wina ndi mnzake. Khululukiranani wina ndi mnzake, monga momwe Mulungu anakukhululukirani mwa Khristu.

Aefeso 4:32

Tisatope nʼkuchita zabwino, pakuti pa nthawi yoyenera tidzakolola ngati sititopa. Agalatiya 6:9
14/05/2026

Tisatope nʼkuchita zabwino, pakuti pa nthawi yoyenera tidzakolola ngati sititopa.

Agalatiya 6:9

Chilichonse mungachite, muchite ndi mtima wanu onse, monga mmene mungagwirire ntchito ya Ambuye osati ya anthu.Akolose 3...
13/05/2026

Chilichonse mungachite, muchite ndi mtima wanu onse, monga mmene mungagwirire ntchito ya Ambuye osati ya anthu.

Akolose 3:23

Address

Victoria Avenue, Box 740
Blantyre

Opening Hours

Monday 08:00 - 16:00
Tuesday 08:00 - 16:00
Wednesday 08:00 - 16:00
Thursday 08:00 - 16:00
Friday 08:00 - 16:00

Telephone

+265888228722

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Bible Society of Malawi posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Place Of Worship

Send a message to Bible Society of Malawi:

Share