Prophetess NANCY Carlos Ministry

Prophetess NANCY Carlos Ministry God wants to change your life, so follow Jesus

"There will come a time when your tears will fall, not because of your troubles, but because God has answered your praye...
24/05/2026

"There will come a time when your tears will fall, not because of your troubles, but because God has answered your prayers.”

— 𝖧𝖠𝖡𝖠𝖪𝖪𝖴𝖪 𝟤:𝟥

Congratulations daughter 👏



18/05/2026

Mukuoneka kuti mwabalalika...Koma osadandaula Mulungu amakukondani.

13/05/2026

Penaso umadzaona ngati Mulungu akuchedwa kukuyakha mapephero ako osadziwa udzichedwetsa wekha🤔

Tayesani kusithako anzanu ocheza nao.
Mudzabwera ndi Umboni.



12/05/2026

Your comeback is going to confuse people who thought your life was over.

07/05/2026

Mulungu sayala Gome popanda Adani

Mulungu akuyalireni Gome kuona kwadani anu.

Aliyense amene akusaka ntchito chisomo ichi chikufikireni.
05/05/2026

Aliyense amene akusaka ntchito chisomo ichi chikufikireni.



05/05/2026

Prophecy confirmation.
Uneneri wakwanilitsidwa.

Ubwino wa mulungu.



04/05/2026

Wina Aliyese Amene Anatemberela Dzina lanu kuti mudzafa osawuka,ena adanenera kuti simudzachita bwino.Ine Lero ndikulengeza Chisomo Cha madalitso pa moyo wanu, Pa banja Panu, pa business yanu Ndipo kumene mdani aliliko Chaka chake ndichino Adan anu ose samvetsetsa ndi zimene mulungu achite Chaka chino mudzina la yesu khristu.



30/04/2026

Some problems don't need fasting and prayers.

Go and apologise to those innocent people you caused Tears!!

Address

Chilomoni Center
Blantyre
0992720284

Telephone

+265881110280

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Prophetess NANCY Carlos Ministry posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share