Apostle ralph Elijah mwasiyambiri jumah ministry

Apostle ralph Elijah  mwasiyambiri jumah ministry 2Co 5:20 Now then we are ambassadors for Christ, as though God did beseech [you] by us: we pray [you] in Christ's stead, be ye reconciled to God. JESUS IS LORD

we believe God's power is still at work
we believe in forgiveness, healing , deliverance and prophecies

27/05/2026

MUSATHAWE ZIMENE MULUNGU WATUMIZA KUTI ZIKUKONZENI!!!

Okhulupirira enieni samasunthidwa ndi mantha a nthawi yovuta, koma ndi mawu a Mulungu. Pamene mavuto abwera, chinthu choyamba chimene munthu amafuna kuchita ndi kuchita mantha. Koma chikhulupiriro chimatiphunzitsa kukhala chete ndi kumvera mawu ofatsa a Mzimu Woyera.

Chimene chikuwoneka ngati kubwerera m’mbuyo lero, mwina ndi kukonzedwa kwa Mulungu k*ti mudzakhale ndi chinthu chachikulu mawa.

Musaweruze tsogolo lanu potengera momwe zinthu zilili pano. Mulungu akugwira ntchito mobisika, kusintha kuchedwa kulikonse kukhala kukonzekera, ndipo mavuto onse kukhala mwayi wakukula.

funeral program
19/03/2026

funeral program

Moni nonse,Ndikufuna kukudziwitsani k*ti ndataya amayi anga akulu ku Zomba. Iwo ndi amene anandisamalira bwino kuyambira...
18/03/2026

Moni nonse,
Ndikufuna kukudziwitsani k*ti ndataya amayi anga akulu ku Zomba. Iwo ndi amene anandisamalira bwino kuyambira ndili mwana mpaka ndinakula n’kuyamba kukhala ndekha.

Maliro akayikidwa ku Mzimba, ku Embangweni, Loweruka. Thupi lidzanyamulidwa kuchokera ku mortuary ya ku Zomba Lachisanu m'mawa 10 koloko.

Zikomo.

miyambo 6 vs 16 - 1916 Pali zinthu zisanu ndi chimodzi zimene Yehova amadana nazo,zinthu zisanu ndi ziwiri zimene zimamu...
13/02/2026

miyambo 6 vs 16 - 19
16 Pali zinthu zisanu ndi chimodzi zimene Yehova amadana nazo,
zinthu zisanu ndi ziwiri zimene zimamunyansa:
17 maso onyada,
pakamwa pabodza,
manja akupha munthu wosalakwa,
18 mtima wokonzekera kuchita zoyipa,
mapazi othamangira msanga ku zoyipa,
19 mboni yonama yoyankhula mabodza
komanso munthu amene amayambitsa mikangano pakati pa abale.

16/12/2025

Never stop believing

MULUNGU aliko🙏ndipo maphero ayankhidwa

Miyambo 14:6Wonyoza anzake amafunafuna nzeru koma osayipeza,koma munthu womvetsa bwino amadziwa zinthu msanga.Moyo uno n...
17/10/2025

Miyambo 14:6
Wonyoza anzake amafunafuna nzeru koma osayipeza,
koma munthu womvetsa bwino amadziwa zinthu msanga.

Moyo uno nazindikila k*t anthu ena omwe mumawapepusa kumbali ndi anthu amene akuziwa zinthu zomwe munakaziwa moyo wanu ukhoza kufikila patali

Every man is a pillar in the things that they know best at, mlimi ndi president pa yekha chifukwa alesi osalima amafuna chimanga chake , opanga feltilizer ndi president mu nthawi yake, angakhale osauka amakulimilani uja ndi waphindu mu Nthawi yake value them

Even every minister of God is useful to another minister , members are useful , your partners are useful in their time coz what they know and have is something you don't know

Respect and lean from all
Apostle ralph Elijah mwasiyambiri jumah ministry

"Remember, your heart holds unique experiences, both bitter and joyful. Though others may not fully understand your stru...
29/07/2025

"Remember, your heart holds unique experiences, both bitter and joyful. Though others may not fully understand your struggles or share your joys, know that your emotions are valid and you have the strength to navigate them. Lean on your faith and trust that God is with you in every season."

‭Proverbs 14:10 NIV‬
[10] Each heart knows its own bitterness, and no one else can share its joy.

Nthawi zina umagwira ntchito, kupanga ma business, kupanga school molimbikira koma opanda phindu lililonse.....Pena iman...
07/06/2025

Nthawi zina umagwira ntchito, kupanga ma business, kupanga school molimbikira koma opanda phindu lililonse.....

Pena imangokhala nthawi chabe koma nthawi zinanso, amakhala anthu ena oipa amene amakhala busy kumanenerera zoipa pa zomwe ukuchita k*ti usapambane.....

Ndipemphero langa k*ti aliyense waife ayambe kupindula pa zomwe akuchita, ndipo ngati alipo ena amene akulimbana nanu ameneyo alimbane ndi Mulungu mudzina la Khristu Yesu 🙌🏼🙌🏼🙌🏼🙌🏼🙌🏼

Tanenani k*ti
"Amen zichitike ndi moyo wanga "

Don't miss this service
30/05/2025

Don't miss this service

No one pays attention to the seed when it's under the earth. They only see the finished result, the flower. Beauty grows...
27/05/2025

No one pays attention to the seed when it's under the earth. They only see the finished result, the flower. Beauty grows through the darkness. Your season of bloom is coming. Continue working on yourself and being patient.

Address

Blantyre

Telephone

+265888751919

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Apostle ralph Elijah mwasiyambiri jumah ministry posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share