Ndirande Kachere CCAP Youth Ministry

Ndirande Kachere CCAP Youth Ministry Ndirande Kachere Youth Department

Muyende mu nzeru ndi iwo akunja, kuchita changu nthawi ingatayike. Mawu anu akhale m’chisomo nthawi zonse wokoleretsa, k...
29/05/2026

Muyende mu nzeru ndi iwo akunja, kuchita changu nthawi ingatayike. Mawu anu akhale m’chisomo nthawi zonse wokoleretsa, kuti mukadziwe inu mayankhidwe anu a kwa yense akatani.
Akolose 4 vs 5-6

Koma inu ndinu mbadwa yosankhika, ansembe achifumu, mtundu woyera mtima, anthu amwini wake, kotero kuti mukalalikire zop...
27/05/2026

Koma inu ndinu mbadwa yosankhika, ansembe achifumu, mtundu woyera mtima, anthu amwini wake, kotero kuti mukalalikire zoposazo za Iye amene adakuyitanani mutuluke mumdima, mulowe kuwunika kwake kodabwitsa;
1 Petro 2 vs 9

Tiyeni Tiyeni!!!Kodi inu simukufuna kupita ku Nyanja? away from noise , kukapanga appreciate nature komanso kukamutamand...
26/05/2026

Tiyeni Tiyeni!!!
Kodi inu simukufuna kupita ku Nyanja? away from noise , kukapanga appreciate nature komanso kukamutamanda Mulungu??

Nkhani ndiyomweyi, Tiyankhuleni!!!

Pakuti kale mudali mdima, koma tsopano muli kuwunika mwa Ambuye; yendani monga ana a kuwunika;Aefeso 5 vs 8
26/05/2026

Pakuti kale mudali mdima, koma tsopano muli kuwunika mwa Ambuye; yendani monga ana a kuwunika;
Aefeso 5 vs 8

Kuti mukakhale wopanda chilema ndi wowona, ana a Mulungu wopanda chilema pakati pa mbadwo wokhokhota ndi wopotoka, mwa i...
25/05/2026

Kuti mukakhale wopanda chilema ndi wowona, ana a Mulungu wopanda chilema pakati pa mbadwo wokhokhota ndi wopotoka, mwa iwo amene monga nyali m’dziko lapansi.
Afilipi 2 vs 15

Inu ndinu kuwunika kwa dziko lapansi. Mudzi wokhazikika pamwamba pa phiri sungathe kubisika. Mateyu 5 vs 14
24/05/2026

Inu ndinu kuwunika kwa dziko lapansi. Mudzi wokhazikika pamwamba pa phiri sungathe kubisika.
Mateyu 5 vs 14

Therefore I tell you, whatever you ask for in prayer, believe that you have received it, and it will be yours. Mark 11:2...
23/05/2026

Therefore I tell you, whatever you ask for in prayer, believe that you have received it, and it will be yours.
Mark 11:24 NIV

The LORD is near to all who call on him, to all who call on him in truth. He fulfills the desires of those who fear him;...
22/05/2026

The LORD is near to all who call on him, to all who call on him in truth. He fulfills the desires of those who fear him; he hears their cry and saves them.
Psalms 145:18-19 NIV

Therefore confess your sins to each other and pray for each other so that you may be healed. The prayer of a righteous m...
21/05/2026

Therefore confess your sins to each other and pray for each other so that you may be healed. The prayer of a righteous man is powerful and effective.
James 5:16 NIV

HAPPY BIRTHDAY BROTHER GIFT
20/05/2026

HAPPY BIRTHDAY BROTHER GIFT

Rejoice evermore. Pray without ceasing. In every thing give thanks: for this is the will of God in Christ Jesus concerni...
19/05/2026

Rejoice evermore. Pray without ceasing. In every thing give thanks: for this is the will of God in Christ Jesus concerning you. Quench not the Spirit.
1 Thessalonians 5:16-19 KJV

Address

Ndirande
Blantyre

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Ndirande Kachere CCAP Youth Ministry posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share

Category