09/06/2026
ZOMUYENEREZA MUNTHU KUTI SWALA YAKE IKHALE YOLANDILIDWA
Pempholo la MUNTHU mnsilamu Kuti lilandilidwe PAMASO pa Allah Pali zinthu zofunikila Kuti munthuyo azikwanilitse.
Zinthuzi zimatchedwa ( شروط الصلاة ) ndipo zilipo zisanu NDI zinayi 9.
Kusasamala mfundo 9 izi Swala singakhale YOLANDILIDWA.
Popeza mpovuta kutchula mfundo zonsezo tiyeni tingonena ya pa number 1.
الاسلام kukhala mnsilamu
Mfundo iyi ikuchokera pa aya iyi
فاقيم الصلاة ، ان الصلاة كانت علامامنين كتاب الموقوتا
👉 Imikana swala , ñdithudi swala inakhazikitsidwa Kwa anthu okhulupilila ( asilamu ) kuti ipempheledwe munthawi yoikika.
Kukhala mnsilamu NDI makiyi achilichonse Kwa Allah الله ndipo ngati munthu sikhala mnsilamu tchito iliyonse imapita pachabe.
Pamene munthu wapanga ,شاهاد ndiye watsekula khomo lakuti tchito zake zizilandilidwa kuphatikizilapo swala.
فجتنبو الشرك
Mnsilamu ophatikiza الله ndizinthu zinà swala yake imakhala yosalandilidwa.
Shirk imawononga tauhid
Tipewe zinthu zotitulutsa muchisilamu ,,, matalazimu, kuwombeza , kukhwama, kudalila nyanga.
Izi ndizinthu zimene ZIDAMPANGITSA munthu kuchoka chikonda Cha ,الله , kudalila Allah
Mkuyamba kudalila shayitwan.
U munafuq, ndizonse zotitalikitsa NDI الله ، cholinga tiziswali tilidi asilamu enieni kuti
Condition yoyamba ya swalayi ikhale yamoyo , ndikuti swala yathu izikhala YOLANDILIDWA pamaso pa الله
Pangani like page iyi ndikupanga share , kuti nkhani izi zifikile ambili , ndikuti nawo aphunzile nawo
,السلام عليكم