Evangelical Church of Malawi, ECOM - Chitawira Centre

Evangelical Church of Malawi, ECOM - Chitawira Centre This is a page for ECOM Chitawira Church Centre. Nyasa Mission, Ntambanyama Synod

23/08/2026
23/08/2026

English Service
Preacher: Mr H. Kantora
Scripture: Revelations 2:7
Spiritual Sensitivity

THURSDAY'S PRAYER AND FASTINGGETTING THE WISDOM AND KNOWLEDGE OF GODMatthew 22:29Jesus replied, “You are in error becaus...
20/08/2026

THURSDAY'S PRAYER AND FASTING

GETTING THE WISDOM AND KNOWLEDGE OF GOD

Matthew 22:29
Jesus replied, “You are in error because you do not know the Scriptures or the power of God.

Apa Yesu akuti anthu zinthu zimativuta kapena kuti timasokoneza zinthu pa Moyo wathu chifukwa tikusowekela chidziwitso... Sitidziwa kuti Mulungu ndi ndani and Mphanvu yake ndi yotani.

Hosea 4:6
(NIV) my people are destroyed from lack of knowledge. “Because you have rejected knowledge, I also reject you as my priests; because you have ignored the law of your God, I also will ignore your children.

Apanso tikuona ku Hosea akuti anthu anga akuonongeka chifukwa akusowa chidziwitso.. Ndikuuzani lero kuti, Kulephera kwathu, Umphawi wathu ndi uchimo wathu ndi chifukwa choti tilibe chidziwitso.

Today as we are praying for Knowledge and wisdom:
We are coming out of our poverty
We are coming out of our reproach
We coming out of our sins
We coming out of our failures
And we are becoming Kings and Queen's, In Jesus Name, Amen 👏

10/08/2026

Word of Encouragement
Exercise your faith. Exercise what you have recrived from God. Dont just keep it idle

09/08/2026

English Service
Minister: Pastor Dan Litta
Topic: Carriers of the Blessings of God Part 1
Genesis 12:1-3

THURSDAY PRAYER AND FASTINGKUMENYA NKHONDO YAMADALITSO PA MOYO WATHUMunthu wina Aliyense Ali ndi Dalitso wake umene Mulu...
06/08/2026

THURSDAY PRAYER AND FASTING

KUMENYA NKHONDO YAMADALITSO PA MOYO WATHU

Munthu wina Aliyense Ali ndi Dalitso wake umene Mulungu anamupatsa kuti ayendemo, koma Madalitso Aliwonse amalumikizika ku Nkhondo imene winaaliyense amaenela kumenya kuti Madalitsowa ayambe kuonekela ku moyo wako, komanso to your Generation.

Genesis 32:23
He took them, sent them over the brook, and sent over what he had.
Genesis 32:24
Then Jacob was left alone; and a Man wrestled with him until the breaking of day.
Genesis 32:25
Now when He saw that He did not prevail against him, He touched the socket of his hip; and the socket of Jacob’s hip was out of joint as He wrestled with him.
Genesis 32:26
And He said, “Let Me go, for the day breaks.” But he said, “I will not let You go unless You bless me!”
Genesis 32:27
So He said to him, “What is your name?” He said, “Jacob.”
Genesis 32:28
And He said, “Your name shall no longer be called Jacob, but Israel; for you have struggled with God and with men, and have prevailed.”
Genesis 32:29
Then Jacob asked, saying, “Tell me Your name, I pray.” And He said, “Why is it that you ask about My name?” And He blessed him there.

Jacob was a man who carried the Generational blessings, but he had to fight with the Angel for the blessing to start manifesting on his life... Akuti pambuyo panali Laban apongozi ake amene amamusaka Yakobo, and kutsogolo kunali Esau yemwenso amafuna Yakobo kuti amalize, koma Yakobo anazindikila kuti nkhondoyi siyaabale anga akundisakawa, Nkhondo ndiya ine ndi Mulungu. Ndipo Yakobo anamuuza Ngelo kuti sindikusiyani Mpaka ntayamba kuwaona Madalitso amenewa. Mulungu anangomusintha dzina ndipo Nkhondo zonse zinatha.

Pamoyo wanu pali Madalitso, koma mwina simukuwaona chifukwa cha Nkhondo zomwe mukukumana nazo, Lero pamene tikusala kudya, Tikufuna timuuze Mulungu kuti "INE SINDIKUSIYANI MPAKA NTAYAMBA KUONA MADALITSO PAMOYO WANGA".

Lero tikulengeza Chipambano pa Nkhondo za :Banja Lanu, Business yanu, Ana anu, School yanu, Mpingo wathu ndi Chilichonse cha Moyo wathu, Ndipo tikayamba KUONA Madalitso a Mulungu mu Dzina la Yesu Khrisitu... Ameni!!

02/08/2026

MGONERO SERVICE (1)🙏

Address

P. O. Box 40111, Soche, Blantyre 4
Blantyre
0000

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Evangelical Church of Malawi, ECOM - Chitawira Centre posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Place Of Worship

Send a message to Evangelical Church of Malawi, ECOM - Chitawira Centre:

Shortcuts

Share