Lisanjala SDA Church

Lisanjala SDA Church Contact information, map and directions, contact form, opening hours, services, ratings, photos, videos and announcements from Lisanjala SDA Church, Church of God, Robert Mugabe Highway, Blantyre.

The official Facebook presence of Lisanjala Seventh-day Adventist Church located in Bangwe, Blantyre under Malabvi District in Eastern Malawi Conference of Seventh-day Adventists

๐— ๐—”๐—ฆ๐—œ๐—ž๐—จ ๐—”๐—๐—” ๐—”๐——๐—ญ๐—œ๐—ช๐—œ๐—ž๐—”Mpingo wa Seventh-day Adventist nchigawo chakumawa cha Eastern Malawi Conference walengeza pulogalamu...
21/05/2026

๐— ๐—”๐—ฆ๐—œ๐—ž๐—จ ๐—”๐—๐—” ๐—”๐——๐—ญ๐—œ๐—ช๐—œ๐—ž๐—”

Mpingo wa Seventh-day Adventist nchigawo chakumawa cha Eastern Malawi Conference walengeza pulogalamu yayikulu ya ulaliki yotchedwa Kholola Machinga kapena Kuti IMPACT MACHINGA nchingerezi yomwe idzachitike m'boma la Machinga kuyambira pa 4 mpaka 31 October chaka chino cha 2026. Ntchitoyi igawika m'magawo awiri: Gawo Loyamba kuyambira 4 mpaka 17 October, ndipo Gawo Lachiwiri kuyambira 18 mpaka 31 October. Cholinga chake ndi kufikitsa uthenga wa chipulumutso kwa anthu ambiri m'derali kudzera mu ulaliki, mapemphero, ndi ntchito zachifundo.

Malingana ndi Pastor Dr. Sanned Lubani, yemwe ndi mtsogoleri wachigawochi ino ndi nthawi yoyenera kulalikira chifukwa posachedwa zinthu sizidzabwerera mwakale. Iye wati tiyenera kugwiritsa ntchito mwayi umenewu pamene zitseko zilipobe zotseguka, chifukwa masiku akudza pamene ntchito ya Mulungu idzakhala yovuta kuchita momasuka. "Tiyeni tigwire ntchito usiku ndi usana, chifukwa usiku ukudza pomwe palibe amene angagwire ntchito," adatero.

Msonkhanowu ukupempha thandizo la ndalama kuchokera kwa anthu okoma mtima, abusa, ndi mabungwe osiyanasiyana kuti ntchitoyi ikayende bwino. Zosowa zazikulu zikuphatikizapo zakudya za oitanidwa, zipangizo za ulaliki, ndi zoyendera za amishonale omwe adzakhale akugwira ntchito m'madera osiyanasiyana a Machinga. Aliyense amene akumva mu mtima mwake kuthandiza ntchito ya Ambuye ali olandiridwa.

IMPACT MACHINGA ikuyembekezeka kubweretsa chitsimutso chauzimu komanso kusintha kwa miyoyo ya anthu ambiri. Tiyeni tonse tigwirizane mu pemphero ndi mu ntchito kuti dzina la Ambuye lilemekezedwe.

Olemba : McAllan Mapinda
EMC Media

Ndipo tsikuli la ma Adventurer padziko lonse silingadutse popanda khekheHappy Sabbath
15/05/2026

Ndipo tsikuli la ma Adventurer padziko lonse silingadutse popanda khekhe

Happy Sabbath

15/05/2026

๐—”๐—–๐—›๐—œ๐—ก๐—ฌ๐—”๐— ๐—”๐—ง๐—” ๐—” ๐—ญ๐—”๐—ž๐—” ๐Ÿฐ ๐— ๐—ฃ๐—”๐—ž๐—” ๐Ÿต ๐—”๐—ž๐—ข๐—ก๐—ญ๐—˜๐—ž๐—” ๐—ญ๐—” ๐—ง๐—ฆ๐—œ๐—ž๐—จ ๐—Ÿ๐—”๐—ช๐—ข

Mawa, la Sabata pa 16 May 2026, ana athu a zaka 4 mpaka 9 a ku kalabu ya Adventurer limodzi ndi atsogoleri awo adzakondwerera World Adventurer Day pansi pa mutu wakuti "KUYENDA NDI YESU".

Chaka chino kalabu yayi ikukwanitsa zaka 37 chikhatsireni mu 1989 ku likulu la mpingo wa Seventh-day Adventist padziko lonse ku America, ndipo tikuyamikira Mulungu chifukwa cha chikondi ndi chitsogozo chake pa ntchito imeneyi ya ana aangโ€™ono.

Pa msonkhanowu, achinyamata a mu bungwe la Adventist Youth Ministries mu kalabuyi adzatenga nawo mbali monga kuimba nyimbo za ulemerero wa Mulungu komanso kulalikira Mawu a Mulungu. Atsogoleri athu, Master Guide Dorothy Njunga ndi Master Guide Madalo Mapinda, akonzekeretsa anawa bwino kwambiri kuti tsikuli likhale lopambana ndi lodzaza ndi madalitso. Pulogalamuyi iyamba kuyambira 8:00 mโ€™mawa mpaka 4:30 madzulo ku Lisanjala SDA Church mumzinda wa Blantyre.

Tikuitana nonse abale ndi alongo a mโ€™mpingo ndi kunja kwa mpingo kuti mudzakhale nafe pa tsiku lino lapadera. Kwa iwo amene sadzatha kubwera mwakuthupi, musadandaule, pulogalamuyi idzaulutsidwa LIVE pa tsamba la Facebook la Lisanjala SDA Church.

Bwerani tidzakondwerere limodzi, tidzaphunzire, tidzaimbe, ndipo tidzayende ndi Yesu.

Olemba: McAllan Mapinda
Lisanjala Media

Happy International Nurses Day. TimakunyadiraniPtilizani kutumimira miyoyo komanso kupemphera.
12/05/2026

Happy International Nurses Day.
Timakunyadirani
Ptilizani kutumimira miyoyo komanso kupemphera.

Obrigado
11/05/2026

Obrigado

๐—ฃ๐—ฅ๐—˜๐—ฆ๐—œ๐——๐—˜๐—ก๐—ง๐—˜ ๐——๐—” ๐—ฆ๐—œ๐—— ๐——๐—œ๐—ฅ๐—œ๐—š๐—˜-๐—ฆ๐—˜ ๐—”๐—ข๐—ฆ ๐—ฃ๐—ฅ๐—˜๐—š๐—”๐——๐—ข๐—ฅ๐—˜๐—ฆ ๐—ค๐—จ๐—˜ ๐—˜๐—ฆ๐—งรƒ๐—ข ๐—” ๐—ฆ๐—˜๐—ฅ๐—ฉ๐—œ๐—ฅ ๐—˜๐—  ๐— ๐—ขร‡๐—”๐— ๐—•๐—œ๐—ค๐—จ๐—˜

O Pastor Dr. Harington Akombwa, presidente da Igreja Adventista do Sรฉtimo Dia na Divisรฃo Sul-Africana e Oceano รndico (SID), falou hoje aos pregadores um dia apรณs o inรญcio das sรฉries evangelรญsticas do Impacto Moรงambique ontem, encorajando-os a trabalhar com esperanรงa.

Akombwa lembrou que a obra de Deus estรก a avanรงar rapidamente nesta regiรฃo da SID, mas ainda exige mais dedicaรงรฃo. Em 2023, o Projeto Impacto realizou-se na รfrica do Sul e no Botswana. Em 2024, vimos grandes bรชnรงรฃos na Zรขmbia, com 133.000 batismos. Em 2025 fomos a Madagรกscar e todas as ilhas, onde foram batizadas 25.000 pessoas. Agora, em 2026, estamos em Moรงambique; em 2028 iremos ao Zimbabuรฉ, e em 2029 estaremos no Malawi.

Trabalhando juntos podemos terminar a obra juntos, porque o Senhor da colheita conhece o nรบmero de almas que serรฃo salvas, disse o pastor Akombwa.

Lendo Atos 1:4-8, o lรญder afirmou que Jesus ordenou aos discรญpulos que nรฃo saรญssem de Jerusalรฉm antes de serem cheios do Espรญrito Santo. Nรณs tambรฉm fomos instruรญdos a pregar em Jerusalรฉm, Judeia, Samaria e atรฉ aos confins da terra. Atos 5:4 lembra-nos que os discรญpulos foram dispersos para pregar. O problema dos dias de hoje รฉ que muitas pessoas querem realizar milagres sem pregar a Palavra. Mas ele disse que os milagres sรฃo uma confirmaรงรฃo da Palavra de Deus que foi pregada. Viemos aqui para terminar a obra que os anjos jรก comeรงaram.

As pessoas que ouviram esta mensagem encheram-se de alegria. Nรณs tambรฉm viemos a Moรงambique para trazer alegria. O povo moรงambicano precisa de um Filipe que lhes explique as Escrituras para que compreendam. A alegria do povo de Moรงambique depende do trabalho que temos aqui. A alegria deles estรก nas nossas mรฃos, por isso nรฃo sejamos tรญmidos nem nos desculpemos. Vamos com as boas novas do Senhor. Nรณs tambรฉm sairemos de Moรงambique com alegria, concluiu Dr. Akombwa.

A regiรฃo da SID tem 23 paรญses, e pregadores do Malawi, Zimbabuรฉ, รfrica do Sul, para mencionar apenas alguns, jรก comeรงaram este ministรฉrio no dia 10 de Maio e terminarรฃo no dia 23 de Maio de 2026.

O Dr. Akombwa falou com estes ministros atravรฉs da internet via ZOOM.

O presidente da Igreja Adventista do Sรฉtimo Dia em Moรงambique, pastor Josรฉ Moreira, agradeceu aos ministros pela dedicaรงรฃo, dizendo que o trabalho aqui em Moรงambique รฉ vasto. Atualmente, existem 380.000 cristรฃos batizados em Moรงambique, um paรญs com 36.639.851 habitantes.

Moรงambique รฉ um dos maiores paรญses de รfrica, mas o nรบmero de adventistas ainda รฉ pequeno.

Autor: McAllan Mapinda
EMC Media

Amen
11/05/2026

Amen

๐—ฆ๐—œ๐—— ๐—ฃ๐—ฅ๐—˜๐—ฆ๐—œ๐——๐—˜๐—ก๐—ง ๐—”๐——๐——๐—ฅ๐—˜๐—ฆ๐—ฆ๐—˜๐—ฆ ๐—ฃ๐—ฅ๐—˜๐—”๐—–๐—›๐—˜๐—ฅ๐—ฆ ๐—ฆ๐—˜๐—ฅ๐—ฉ๐—œ๐—ก๐—š ๐—œ๐—ก ๐— ๐—ข๐—ญ๐—”๐— ๐—•๐—œ๐—ค๐—จ๐—˜

Pastor Dr. Harington Akombwa, President of the Seventh-day Adventist Church in the Southern Africa-Indian Ocean Division (SID), today addressed preachers one day after the Impact Mozambique evangelistic meetings began yesterday, encouraging them to work with hope.

Akombwa reminded them that Godโ€™s work is moving fast in this SID region, yet it requires more effort. In 2023, the Impact Project was held in South Africa and Botswana. In 2024 we saw great blessings in Zambia with 133,000 baptisms. In 2025 we went to Madagascar and all the islands, where 25,000 people were baptized. Now in 2026 we are in Mozambique, in 2028 we will go to Zimbabwe, and in 2029 we will be in Malawi.

By working together we can finish the work together, because the Lord of the harvest knows the number of souls that will be saved, said Pastor Akombwa.

Reading from Acts 1:4-8, the leader said that Jesus commanded the disciples not to leave Jerusalem until they were filled with the Holy Spirit. We too have been instructed to preach in Jerusalem, Judea, Samaria, and to the ends of the earth. Acts 5:4 reminds us that the disciples were scattered to preach. The problem today is that many people want to perform miracles without preaching the Word. But he said miracles are a confirmation of Godโ€™s Word that has been preached. We have come here to finish the work that the angels have already started.

People who heard this message were filled with joy. We too have come to Mozambique to bring joy. The people of Mozambique need a Philip who can explain the Scriptures so they understand. The joy of the people of Mozambique depends on the work we are here to do. Their joy is in our hands, so letโ€™s not be shy or apologetic. Letโ€™s go with the good news of the Lord. We too will leave Mozambique with joy, Dr. Akombwa concluded.

The SID region has 23 countries, and preachers from Malawi, Zimbabwe, South Africa, to mention just a few, have already begun this ministry on May 10 and will finish on May 23, 2026.

Dr. Akombwa spoke to these ministers via the internet on ZOOM.

The President of the Seventh-day Adventist Church in Mozambique, Pastor Jose Moreira, thanked the ministers for their dedication, saying that the work here in Mozambique is vast. Currently, there are 380,000 baptized Christians in Mozambique, a country of 36,639,851 people.

Mozambique is one of the largest countries in Africa, yet the number of Adventists is small.

Written by: McAllan Mapinda
EMC Media

๐— ๐—ง๐—ข๐—ฆ๐—š๐—ข๐—Ÿ๐—˜๐—ฅ๐—œ ๐—ช๐—” ๐—ฆ๐—œ๐—— ๐—”๐—ฌ๐—”๐—ก๐—ž๐—›๐—จ๐—Ÿ๐—” ๐—ž๐—ช๐—” ๐—”๐—Ÿ๐—”๐—Ÿ๐—œ๐—ž๐—œ ๐—ข๐— ๐—ช๐—˜ ๐—”๐—ž๐—จ๐—ง๐—จ๐— ๐—œ๐—ž๐—œ๐—ฅ๐—” ๐—ž๐—จ ๐— ๐—ข๐—ญ๐—”๐— ๐—•๐—œ๐—ค๐—จ๐—˜M'busa Dr Harington Akombwa yemwe ndi mtsogoleri w...
11/05/2026

๐— ๐—ง๐—ข๐—ฆ๐—š๐—ข๐—Ÿ๐—˜๐—ฅ๐—œ ๐—ช๐—” ๐—ฆ๐—œ๐—— ๐—”๐—ฌ๐—”๐—ก๐—ž๐—›๐—จ๐—Ÿ๐—” ๐—ž๐—ช๐—” ๐—”๐—Ÿ๐—”๐—Ÿ๐—œ๐—ž๐—œ ๐—ข๐— ๐—ช๐—˜ ๐—”๐—ž๐—จ๐—ง๐—จ๐— ๐—œ๐—ž๐—œ๐—ฅ๐—” ๐—ž๐—จ ๐— ๐—ข๐—ญ๐—”๐— ๐—•๐—œ๐—ค๐—จ๐—˜

M'busa Dr Harington Akombwa yemwe ndi mtsogoleri wa mpingo wa Seventh-day Adventist mmaiko akumwera kwa Africa koma zilumba za Indian Ocean (SID) lero walankhula ndi alaliki tsiku limodzi maulaliki a Impact Mozambique atayamba dzulo, kuwalimbikitsa kuti agwire ntchito ndi chiyembekezo.

Akombwa wakumbutsa kuti ntchito ya Mulungu ikuyenda mofulumira mโ€™chigawo chino cha SID komabe oakufubika kulimbika. Mu 2023 Impact Project inachitika ku South Africa ndi Botswana. Mu 2024 tinaona madalitso aakulu ku Zambia ndi ubatizo wa anthu133,000. Mu 2025 tinapita ku Madagascar ndi zilumba zonse ndipo panabatizidwa anthu 25,000. Tsopano mu 2026 tili ku Mozambique, mu 2028 tipita ku Zimbabwe, ndipo mu 2029 tikhala ku Malawi.

Pogwira ntchito limodzi titha kumaliza ntchitoyi limodzi, chifukwa Ambuye wa zokolola akudziwa chiwerengero cha miyoyo yomwe idzapulumutsidwe. Atero abusa Akombwa

Powerenga pa Machitidwe 1:4-8, mtsogoleri yu ananena kuti Yesu analamula ophunzira kuti asachoke ku Yerusalemu asanadzazidwe ndi Mzimu Woyera. Ifenso tinalangizidwa kukalalikira ku Yerusalemu, Yudeya, Samariya, ndi ku malekezero a dziko lapansi. Machitidwe 5:4 akutikumbutsa kuti ophunzira anamwazikana kukalalikira. Vuto la masiku ano ndi loti anthu ambiri amafuna kuchita zozizwitsa popanda kulalikira Mawu. Koma iye anati zozizwitsa ndi chitsimikizo cha Mawu a Mulungu amene alalikidwa. Tabwera kuno kudzamaliza ntchito imene angelo anayamba kale.

Anthu amene anamva uthengawu anadzazidwa ndi chimwemwe. Ifenso tabwera ku Mozambique kudzabweretsa chimwemwe. Anthu aku Mozambique amafunikira Filipo amene angawafotokozere Malembo kuti amvetse. Chimwemwe cha anthu a ku Mozambique chidalira ntchito imene tili nayo pano. Chimwemwe chawo chili mโ€™manja mwathu, choncho tisachite manyazi kapena kupepesa. Tiyeni tipite ndi uthenga wabwino wa Ambuye. Ifenso tidzachoka ku Mozambique ndi chimwemwe. Anamaliza Dr Akombwa.

Chigawo cha SID chili ndi maiko 23 ndipo alaliki ochokera ku Malawi, Zimbabwe, South Africa kungotchulapo ochepa chabe ayamba kale utumikiwu pa 10 May ndipo amaliza pa 23 May 2026

Dr Akombwa anayankhula ndi atumikiwa kudzera pa makina a internet pa ZOOM.

Mtsogoleri wa mpingo wa Seventh-day Adventist ku Mozambique m'busa Jose Moreira wayamika atumikiwa podzipereka ponena kuti ntchito kuno ku Mozambique ndiyambiri. Pakadali pano Akhristu obatizodwa ku Mozambique alipo 380, 000 dziko la anthu 36, 639, 851.

Mozambique ndi limodzi mwa maiko akuulu kwambiri mu Africa koma chiwerengero cha ma Adventist ndichochepa.

Olemba : McAllan Mapinda
EMC Media

Address

Robert Mugabe Highway
Blantyre

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Lisanjala SDA Church posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share

Category