One Ummah Islamic Foundation of Malawi

One Ummah Islamic Foundation of Malawi One ummah was created with the purpose of teaching about the fear of Allah to the Nation of Malawi

BREAKING: Iran's Supreme Leader Ayatollah Ali Khamenei has been killed and his body has been found, reports Reuters, cit...
28/02/2026

BREAKING: Iran's Supreme Leader Ayatollah Ali Khamenei has been killed and his body has been found, reports Reuters, citing Israeli media reports.

Mtsogoleri Wamkulu wa Iran Ayatollah Ali Khamenei waphedwa ndipo thupi lake lapezeka, malinga ndi malipoti a Reuters, ponena za malipoti a atolankhani aku Israeli.

koma Akulu akulu ku Iran ak*ti Tsogoleriyu alimoyo ndipo alakhula ku Mtundu wa Anthu posachedwapa.


🔴 LIVE updates: aje.news/s9152d

NKHANI ZOMWE ZILI MKAMWA MKAMWA ZIMENE ZIKUCHITIKA PA USIKU WA 28 FEBRUARY 2026pomwe Israeli Prime Minister Benjamin Net...
28/02/2026

NKHANI ZOMWE ZILI MKAMWA MKAMWA ZIMENE ZIKUCHITIKA PA USIKU WA 28 FEBRUARY 2026

pomwe Israeli Prime Minister Benjamin Netanyahu akunena k*ti pali zizindikiro zoti Ayatollah Ali Khamenei, mtsogoleri wa pa mfundo za boma ku Iran, wafa pomwe Ma bomba a US ndi Israel agwera ku nyumba Kwake

Netanyahu akunena k*ti pali zizindikiro k*ti Khamenei ‘satha kukhala ali ndi moyo’ pambuyo pa mazana a ma bomba a US‑Israel omwe atsekula nyumba zoyambira za mtsogoleriyo ku Tehran.
kuphatikiza kubowola malo ena okhudzana ndi utsogoleri wa Iran ndi pulogalamu yake ya nyukiliya.

Komabe, palibe umboni wovomerezeka k*ti Khamenei wafa kapena k*ti ali ndi moyo,
kuchokera kumabungwe a boma lililonse la Iran, la United States kapena la Israel.

Iran ik*ti mtsogoleri wake ali ndi moyo, ngakhale k*ti Ma news akupitilira popanda umboni weniweni.

Netanyahu akulangiza anthu aku Iran k*ti adzuke ndi kuchita zomwe iwo amawona k*ti ndi zoyenera ndi kulimbikitsa k*ti boma lawo lisinthe, pomwe limodzi ndi US akupitiliza kuwononga malo a utsogoleri wa Iran.

22/12/2025

Sheikh Siraj Hussein writes:

ومن طلب غريب الحديث كذب

NDIPO AMENE AMASAKASAKA NKHANI ZA CHILENDO AMANAMA.

Kavuto kena komwe kamapezeka mu zifuwa za ma student panthawi yomwe akusakasaka maphunziro a deen ndi:-

Kufuna kubweletsa zinthu za new-one kugulu zoti ambili sanazinveko ndi cholinga choti apange shine pamaso pa anthu.

Ndizodziwika k*ti munthu amene ali ndi Ilm yambiri komaso amadziwa zinthu zambili zoti ena samadziwa, amakhala munthu osililika komaso oyamikilidwa ndi anthu. Zimenezi zimapangitsa ma student ena k*ti akomedwe ndipo azisakasaka zinthu zooneka za chilendo komaso zosowa cholinga anthu akazinva, aziwayamilira ndikuwaona k*ti iwo ndi ozama pa Ilm.

Mchitidwe umenewo umakhala ndi mavuto ambiri kuyambira kwa iwe student komaso anthu ok*tsata. Apart from kusowetsa Ikhlaas, mavuto ena awili akulu omwe amabwela ndi mchitidwe umenewo ndi awa:-

1. Kuthawitsa anthu k*ti asanve uthenga wako.
Munthu ukakhala k*ti nkhani zako za deen zomwe umabwela nazo nthawi zonse zimakhala zachilendo komaso zosemphana ndi zomwe anthu amaziziwa, anthu amakukayikira ndipo amak*tenga ngati ndiwe munthu wabodza ongofuna attention. Mentality imeneyo imadza poona k*ti mchifukwa chani awa nthawi zonse amabwela ndi zinthu zoti ena sakamba? Tiziti odziwa ndi iwo okha? Nde anthu amakukayikira.

2. Kuwapatsa anthu uthenga osathyakuka pa kafukufuku.
Pokhala k*ti iweo cholinga chako ndichak*ti uwapatse anthu uthenga wa chilendo, sumalabada kwambiri za tsatane tsatane wa uthengawo. Sumafufuza k*ti ma Ulama ena anati chani pa nkhaniyo, koposaposa sulabada k*ti mchifukwa chani nkhaniyo ili yosaziwika ndi yosatchuka pamaso pa ambili.

Mu Sharh ya Aqeedah twahawiyyah ya Naasr Al Aql polongosola mawu a Abu Yusuf onena k*ti

Munthu amene amafunafuna nkhani za chilendo amazanama anatu:-

إذا طلب غريب الحديث -سواء ما يتعلق بالأحاديث المكذوبة مثلاً أو بالأحاديث التي فيها نوع من الإشكال أو الاشتباه أو غيرها-

Munthu akamasakasaka nkhani za chilendo kaya zikhala ma Hadeeth abodza kaya nkhani zoti nkati mwake muli ma complications kapena kulowana kapena kusakanikirana kapena zina zotero

وولج في هذا الباب وأكثر منه فلابد أن يتأثر على نحو يجعله يتعلق ببعض الإشكالات،

Ndikulowa pa khomo la nkhani zimenezi nkumachulutsa za izi, munthu ameneyo zimapezeka k*ti basi amakhala ndi zinthu zoti zimampangitsa k*ti alowe mma complications ena.

فتثير في نفسه الشك، أو تجعله ممن يثيرون الشكوك بدعوى أن عنده علماً وأن عنده طرائف، وأن عنده أشياء ليست عند الناس،

Nde amatha kuzibweletsera zikayiko mu mtima mwake kapena kuwabweletsera ena zikayiko poganizira k*ti iye ali ndi ilm yoti ena alibe kapena ali ndi zinthu zoti ena sazidziwa.

فيقع في هذه الظواهر التي تئول بالإنسان إلى الكذب والدجل والشك والريب.

Nde amagwela mu izi zomupititsa ku kunama, kupena chinyengo komaso chikayiko

Sheikh Manyamba Abdul Aziz writes:وَلَأُضِلَّنَّهُمْ وَلَأُمَنِّيَنَّهُمْ وَلَآمُرَنَّهُمْ فَلَيُبَتِّكُنَّ آذَانَ الْأَ...
22/12/2025

Sheikh Manyamba Abdul Aziz writes:

وَلَأُضِلَّنَّهُمْ وَلَأُمَنِّيَنَّهُمْ وَلَآمُرَنَّهُمْ فَلَيُبَتِّكُنَّ آذَانَ الْأَنْعَامِ وَلَآمُرَنَّهُمْ فَلَيُغَيِّرُنَّ خَلْقَ اللَّهِ ۚ وَمَن يَتَّخِذِ الشَّيْطَانَ وَلِيًّا مِّن دُونِ اللَّهِ فَقَدْ خَسِرَ خُسْرَانًا مُّبِينًا

Surat An-Nisaa’ (4:119)

“Ndithu ndidzawasokeretsa, ndidzawapatsa ziyembekezo zabodza, ndidzawalamulira motero adzadula mak*tu a ziweto, ndipo ndidzawalamuliranso motero adzasintha chilengedwe cha Mulungu. Ndipo aliyense amene amamupanga Satana kukhala mtetezi wake kusiya Mulungu, ndithu watayika k*tayika koonekera.”

Kusintha chilengedwe nkoletsedwa kwa Msilamu munjira iliyonse yomwe angaichitire, kaya ndi HD yokhala ndi filter yosintha mmene munthu alili kapena kudzola mafuta osintha chilengedwe( oyeretsa) kukuza zida, ma hip, mabere, matako, kukuza maso, njira ya operation, , , ma apps kapena ma software ndi kumwa mankhwala zonsezi ndi Haram.

16/08/2025

ABU DHAR AL GHIFAR NDI ZAYT
PANGANO LA KUPHEDWA.

Assalam Alaykum Awa ndi Anthu omwe anapha Shanaaz Yusuf Allah Wafewetsa Mpaka apezeka Koma Funso Nkumati Why Anapanga zi...
14/07/2025

Assalam Alaykum

Awa ndi Anthu omwe anapha Shanaaz Yusuf Allah Wafewetsa Mpaka apezeka Koma Funso Nkumati Why Anapanga zimenezi?

Ma dua Anu Allah walandira tizingodikira timve chirango komanso Chifukwa chomwe Anachitira izii

Anaika Moyo wa Ena Pachiphinjo

Musanachitepo kanthu, ganizirani zotsatira zake; chisankho chilichonse chimakhala ndi zotsatira. Ganizirani musanachitepo kanthu, ndipo sankhani chifundo m’malo mwaukali kapena Tinene Mkwiyo; Chifundo chimatha kusintha moyo wanu.

Innalillah wainna ilaih rajiuna Sister Shanaaz Yusuf

Allah Wamphamvu kwa Akapoli ake tikupepha k*ti Musitse Chilungamo pa kuphedwa kwa Shanaaz Yusuf. Tipempha kwa ALLAH k*ti...
03/07/2025

Allah Wamphamvu kwa Akapoli ake tikupepha k*ti Musitse Chilungamo pa kuphedwa kwa Shanaaz Yusuf. Tipempha kwa ALLAH k*ti awapanse Ofufuza Ukadaulo ndi Mphamvu komanso Kusagwera mphwayi k*ti afufuze mozama za kuphedwa kwake komvetsa chisoni komanso kugwiriridwa. Amene ali ndi mlandu wuuu Mmanja mwake Apezeke ndipo aweruzidwe, ndipo banja lake lipeze mphamvu pa nthawi yovutayi. Moyo wake unali wofunika, ndipo imfa yake sidzapita pachabe. Tikupempha Allah k*ti awatsogolere akuluakulu aboma k*ti Akhale ndi chidwi pakufufuza mpaka chowonadi chipezeke komanso k*ti ochita zoipa wooo awaweruzidwe. Allah atonthoze banja lake ndi okondedwa ake. Ameen." Innalillah wainna ilaih rajiuna

27/04/2025

❤💙💚💛❤🤎🧡

07/04/2025



Uthenga Kwa Ma Banja a Asilamu"

Monga Msilamu, ndikofunika kuika patsogolo kugawana nzeru za Deen ndi banja lanu.

Ine M'bale wanu pa Deen Ndikukulimbikitsani k*ti mutengepo mbali pophunzitsa Deen azi kazi anu,

ndithu iwo ndi amene angathe kuphunzisa Ndi kufalitsa Deen kwa ana anu mosavuta.

Amayi ali ndi udindo wapadera pakupanga malingaliro ndi zikhalidwe za ana awo, ndipo chikoka chawo kwa Ana awo Ndichoposa Chikoka cha Azibambofe. akazi anu, nda amene ali abwenzi apamtima a ana anuwo, ndipo mukuphunzisa deen Azi kazi anu Ana anu Azailandila Deen Ndi Maphunziro Ake Akadali Achichepele izi zimapangitsa k*ti maphunziro awo akhale osavuta chifukwa amatha k*tenga zambiri kuchokera kwa omwe amawakhulupirira omwe ndi Azimayi Awo. Mwana Dua pakudya, pogona, polowa kuchimbuzi, ngakhale kupeleka Salaam ndi kupanga Isthja(Kuzisuka Malo obisika) Izi Ndizithu zomwe Akuyenera mwana kuphunzira Mmanja mwa Mayi ake kuchokera kwainu Osati Ku Madrasa kokha ayi."

Ndi zomvesa Chisoni Kuti Azimayi Ambiri Achisilamu Sakuziwa Udindo wawo Ndipo Mayendedwe,Mavalidwe, ngakhale kasekedwe kawo ndi kopanda nako Manyazi Muona dzimayi Ndithu Ali belu belu Usiku ndi usana Kulowela uku ndi uku Kamba ka kusowa Ilim yochoka kwa Azibambo Anyumba mwawo Izi ndizithu zoti Zimayi ndi Povuta kuphunzira kuchokera kwa Sheikh ayii koma inuyo
Take your family in order

Njira imeneyi ingathandize kulimbikitsa ma kuphunzira ndi k*thandiza ana anu Kukhala ana akhalidwe Ndi oziwa Deen yanu.

Best regards
Farooq Issah Abou Afzal

01/06/2024

Sheikh Siraji Hussein writes:

Alie ibn Abie Twalib Allah ﷻ asangalare naye anati:-

كفى بالعلم شرفاً أن يدعيه من ليس بأهله

Umboni okwanira oti maphunziro ndi chinthu cha ulemelero ndiwak*ti even amene alibe maphunzirowo amazitchula k*ti ndiophunzira.

وكفى بالجهل عاراً أن يتبرأ منه من هو فيه

Ndipo umboni okwanira oti umbuli ndi chinthu chochititsa manyazi ndioti amene ali nawo umbuliro amazitalikitsa nazo

Bungwe la African human trust ndilokondwa kulengeza za mwai wantchito ya u sheikhat,,,, ma sheikhat amene akufunika pa n...
28/05/2024

Bungwe la African human trust ndilokondwa kulengeza za mwai wantchito ya u sheikhat,,,, ma sheikhat amene akufunika pa ntchitoyi akhale k*t ali ndi certficate ya islamic studies komanso k*t amatha kulankhula ndikumva chiyankhulo cha arabic ,,amantha kulewelenga bukhu lolemekezeka la Qur'an mwa tajweed,, komanso akhale ndi chitupa cha umzika (national id) .kwa onse amene ali ndi zowayenelezazi ndipo akufuna ntchitoyi akuyenela azabwere kuzachita nao mayeso kapena k*ti ma interview a ntchitoyi omwe achitike

loweluka lapa 1 June 2024. Kuyambila
nthawi ya 8 koloko mmawa .
Ndipo mayesowa akachitikila pa markaz salmaan al faarisiyy yomwe ikupezeka ku lunzu pafupi ndi kaphuka stage .
Ndipo kwa nonse amene mukubwera kuzachita nawo ma interview wa pobwela osaiwala k*tenga ma certificate kapena k*t ma shahada komanso national id yanu,,, mukafuna kumva zambir zama interview wa lumikizanani ndi sheikh Ismail Mansoor pa 0982768250.

Mukamva uthengau ziwitsan anzanu.

Address

Sankontshe Masjid, Hammarsdale, , Mr430 Road, Sankontshe, Ilanga, 3700
Hammarsdale
FEARALLAH

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when One Ummah Islamic Foundation of Malawi posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Place Of Worship

Send a message to One Ummah Islamic Foundation of Malawi:

Share