Mtumiki Joshua

Mtumiki Joshua TIYENI TIYITANILE YEHOVA PA NYENGO YANU, NDIPEPHELO NDIPO NDICHIKHULUPILILO YEHOVA ASINTHA NYENGOYO (NDI MULUNGU NDIZOTHEKA (MATEYU 19:26) CALL/WSP 0982144285

01/09/2026

*AKUFA KU TCHIMO*

Hallelujah!!

Kumwamba kulandile ulemu chifukwa cha moyo komaso nthawi yomwe tapasidwa, moti ndichisomo ndithu kupezeka ndi moyowu Hallelujah!!!

Lero Mulungu mwabvumbuluso akufuna kutitengela kuchiziwitso pama Funso awiri; Loyamba ndi lonena kuti :
*[1]_(AKUFA KU TCHIMO, ZIKUTATHAUZANJI?)_*
Hallelujah!!!!
Mwa mau wopezeka m'buku la *(Aroma 6:11)*
Kotero inunso, mudzione nokha ngati akufa Ku tchimo koma a moyo kwa Mulungu mwa Khristu Yesu
__________

So kutengela ndi mau omwe tawelenga tiwona za *IMFA* Kuti ndichiyani ndipo yimakhala yotani, kuyakha kapena kufotokozela kwa gawo ili, zitisogolela kuzindikila za tathauza LA Funso loyamba Hallelujah!

Tikamati imfa, ndichithu chomwe chimadza ku chithu chilichonse cha moyo, ndipo imfayi yimaza mwazizi, ndipo imfa yikakumana ndi chithu cha moyo, nde kuti chamoyochi chimasiya kugwila nchito iliyonse, chifukwa, mtima umasiya kugunda ndipo magazi amawuma mphweya umachoka Hallelujah!! So m'menemu ndimomwe imfa yimakhalila

So *UTCHIMO* Umakhala wa moyo, pa moyo wamunthu wina aliyense amene akuchita..... So kukhala akumfa kuuchimo nde kuti kusamvomekeza kuyenda kapena kuchita choyipa, kumene kuja kumfa Ku utchimo, chifukwa uchimo uja sugwilaso nchito pa iwe, monga tamvela kuti chakufa sichimachita kalikonse Hallelujah!!

So chilakolako chomwe chimabwela kuti tichite chigololo, kapena kuonela zolaula or kuzigona tokha, zimachitika pa ife chifukwa choti uchimo uja uli active, koma titavomekeza kumulandila Yesu, uchimo umafa ndipo zilakolako zathupi sizimakula mphamvu Hallelujah!!!!!!!
______________________

Tiyimile apa lero
Ndipo tipitiliza pa verse lomweli kuona za *KUKHALA A MOYO MWA MULUNGU* Kuti zimatathauza chani

*_MTUMIKI JOSHUA_*

Funso kapena ndemanga 0880310689
Kwamene muli pa group funsani pa group popa tiyakha
AMEN AMEN

(Miyambo 29 : 25-27)25. Kuopa munthu kudzakhala ngati msampha, koma aliyense amene amadalira Yehova adzatetezedwa. 27. A...
31/08/2026

(Miyambo 29 : 25-27)
25. Kuopa munthu kudzakhala ngati msampha, koma aliyense amene amadalira Yehova adzatetezedwa.

27. Anthu olungama amanyansidwa ndi anthu achinyengo; koma anthu oyipa amanyansidwa ndi anthu a mtima wowongoka.

Hallelujah!!!

26/08/2026

Luka 21 : 3-4
3. Iye anati, “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti mkazi wamasiye wosaukayu wapereka zambiri kuposa ena onsewa.
4. Anthu onsewa atapa mphatso zawo kuchokera pa zochuluka zimene ali nazo; koma uyu, mwa umphawi wake, wapereka zonse zimene ali nazo.”

AMEN
24/08/2026

AMEN

Wumu ndimomwe tikuyendela mwezi wunoKutumikila kwa nkhomo ndi nkhomoPamene tikudikila chisomo chomanga kachisiWofuna kut...
22/08/2026

Wumu ndimomwe tikuyendela mwezi wuno
Kutumikila kwa nkhomo ndi nkhomo
Pamene tikudikila chisomo chomanga kachisi

Wofuna kuthandiza
Kugula udzu
Kaya mitengo
Kaya plastic
Misomali
Zilona zokhalila
Call or wsp 0982144285
SHALLOM

Note: kwamene akuchimva
Is not by force
AMEN

ANZANENA ZAUBWINO WANU MUKAZAKHALA KUTI MWACHOKA KAPENA KUMFA!!!!!
21/08/2026

ANZANENA ZAUBWINO WANU MUKAZAKHALA KUTI MWACHOKA KAPENA KUMFA!!!!!

Pangani tsiku la lero kukhala lofunika kwambiri mwa kukhala ndi maganizo abwino, kuchitapo kanthu pang'onopang'ono kuti ...
19/08/2026

Pangani tsiku la lero kukhala lofunika kwambiri mwa kukhala ndi maganizo abwino, kuchitapo kanthu pang'onopang'ono kuti mukwaniritse zolinga zanu, komanso kukumbukira kuti kutuluka kwa dzuwa kulikonse kwatsopano ndi mwayi woyambiranso kupanga chinthu chabwino.

AMBUYE AKUDALITSENI
AMEN AMEN

17/08/2026

CHISOMO

Day 2 on the mountain(Psalm 121:1-2) "I lift up my eyes to the mountains—where does my help come from? My help comes fro...
11/08/2026

Day 2 on the mountain

(Psalm 121:1-2) "I lift up my eyes to the mountains—where does my help come from? My help comes from the Lord, the Maker of heaven and earth."

Hallelujah!!!

Address

T/A MAGANGA
Benoni

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Mtumiki Joshua posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Shortcuts

Share