Zomba Cathedral Parish

Zomba Cathedral Parish Evangelisation

Mpingo wakatolika ku Diocese ya Zomba lero wakhazikitsa Gulu la Atumiki a Chifundo. Mwambo Wu unayamba ndi mdipiti omwe ...
06/06/2026

Mpingo wakatolika ku Diocese ya Zomba lero wakhazikitsa Gulu la Atumiki a Chifundo. Mwambo Wu unayamba ndi mdipiti omwe unayambira kwa Jali Trading center kukathera ku Our lady Pirimit Parish. Ndipo mau akulu patsiku li anali Bwerani Mudzaone (Yohane 1:38-39. Anatsogolera Mwambo wa Nsembe ya Ukaristia ndi Olemekezeka Ambuye Alfred Mateyu Chaima Episcope wa Diocese ya Zomba. Bungwe la Atumiki Achifundo kuno ku Zomba Anayambitsa ndi Mayi Jane Mkandawire

23/05/2026
Amati Akatolika amodzi pa Utumiki.Uwu ndi mutu umene Bambo Stanislaus Confidence Mchenga adagawana nawo azimayi a CWAZom...
22/02/2026

Amati Akatolika amodzi pa Utumiki.
Uwu ndi mutu umene Bambo Stanislaus Confidence Mchenga adagawana nawo azimayi a CWAZomba Deanery Ku Zomba Cathedral Church.

Fr Mchenga walangidza amayi kuti utumiki si mpikitsano ayi
Ndipo bambowa apempha amayi kukhala ozichepetsa monga amayi Maria ankachitita, Iwo ati ngati amayi azithanso kukhala ndi udindo opempherera ena komanso Mpingo.
Potsilidza Iwo awapempha amayi kuti akagawane ndi amayi amdzawo za zomwe amva Ku Bindikiro kuti onse ayendere limodzi.
Mayi Caro Solomon Kayange yemwe ndi wapampando mu Zomba Denary wayamikira amayi chifukwa chobwera mwa unyinji Ku Bindikirowu mayi Kayange walimbikitsa amayi omwe anabwera kuti akagawireko amayi anzawo za bindikirowu

Amayi a Zomba Deanery akhala ndi Bindikiro wawo mawa Ku Zomba Cathedral, ndipo udzayamba  nthawi ya 8 koloko mawa. Ochit...
20/02/2026

Amayi a Zomba Deanery akhala ndi Bindikiro wawo mawa Ku Zomba Cathedral, ndipo udzayamba nthawi ya 8 koloko mawa.
Ochititsa ndi a Dean a Zomba Deanery FR R Mbendera omwenso ndi bambo mfumu a Sacred Heart Parish.
Amayi nonse mukupemphedwa kufika mwa unyinji.

20/02/2026
Ngat misa ya 6:00am yakuphonyani, misa ya 8:00am mwachedwa musatayi mtima misa ina ikhalapo nthawi ya 4:00pm ..lent yapa...
18/02/2026

Ngat misa ya 6:00am yakuphonyani, misa ya 8:00am mwachedwa musatayi mtima misa ina ikhalapo nthawi ya 4:00pm ..lent yapambana kwa inu nonse

CWA Zomba Diocese lero inakabzala Mitengo yokwana 500 Ku Thondwe pafupi ndi nyumba ya Ambuye opuma Ambuye Allan Chamgwer...
14/02/2026

CWA Zomba Diocese lero inakabzala Mitengo yokwana 500 Ku Thondwe pafupi ndi nyumba ya Ambuye opuma Ambuye Allan Chamgwera

Ana opotsa 100 asonkhana Ku nyumba Kwa Ambuye Alfred Mateyu Chaima Zomba Diocese lero, cholinga ndi kokachedza ndi Ambuy...
31/12/2025

Ana opotsa 100 asonkhana Ku nyumba Kwa Ambuye Alfred Mateyu Chaima Zomba Diocese lero, cholinga ndi kokachedza ndi Ambuye olemekeza mu nyengo ino ya khrisimas.

Ana ochokera ma church 5 omwe akupanga Scared Heart Parish ndi omwe afika Kwa Ambuye Chaima kuimiriraa ana onse omwe ali mu Dioceseziyi .

Anawa lero pafupifupi tsiku lonse akhala akuchedza , kuvina ndi kudya nkhomaliro pamodzi ndi Ambuye Chaima.

Mwambo wa nsembe ya Ukalistia, Chaka cha Stephano Oyera, Malitiri oyamba. Omwe ukuchitikira mu Zomba Cathedral, ndipo ak...
26/12/2025

Mwambo wa nsembe ya Ukalistia, Chaka cha Stephano Oyera, Malitiri oyamba. Omwe ukuchitikira mu Zomba Cathedral, ndipo akutsogolera nsembe ya Ukalistia umenewu ndi olemekeza Ambuye Alfred Mateyu Chaima.

Mwambowu ndi opephereranso atumiki onse amumpingo. Komanso pamapeto pake pakhala pakuchitika Fundraising yothandizira a Semino a Zomba Diocese omwe ali mu maseminale osiyanasiyana Malawi muno.

Address

Sacred Heart Zomba Cathedral, P. O Box 106, Zombaa
Zomba

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Zomba Cathedral Parish posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share