06/06/2026
Mpingo wakatolika ku Diocese ya Zomba lero wakhazikitsa Gulu la Atumiki a Chifundo. Mwambo Wu unayamba ndi mdipiti omwe unayambira kwa Jali Trading center kukathera ku Our lady Pirimit Parish. Ndipo mau akulu patsiku li anali Bwerani Mudzaone (Yohane 1:38-39. Anatsogolera Mwambo wa Nsembe ya Ukaristia ndi Olemekezeka Ambuye Alfred Mateyu Chaima Episcope wa Diocese ya Zomba. Bungwe la Atumiki Achifundo kuno ku Zomba Anayambitsa ndi Mayi Jane Mkandawire