Saved By Grace Ministries MW

Saved By Grace Ministries MW An SDA Ministry of Families aimed at Serving God through Music,Evangelistic Crusades &Social Welfare.

17/08/2026
14/08/2026

Mwana wa bwana wina anameza singano akuseweretsa, ndipo mwachanguchangu makolo ake anathamangila naye kuchipatala.

Madotolo anayesesa kumbali yawo koma zimaonesa kuti zinali zovuta kuti singanoyo achoke.

Mwadzidzizi kunabwera wamisala wina yemwe amadya zakudya zake zoola.Panthawiyi n'kuti makolo amwanayo ali busy kuyankhulana ndi adotolo kuti atani kwenikweni kuti mwana athandizidwe.Mwanayo analilira chakudya cha wamisalayo ndipo wamisala anatenga ndikumpasa.

Makolo amwanayo ataona izi anamududuluzila wamisalayo panja mwachipongwe uku akumuswa makofi ponyasidwa kuti adamupasa mwana wawo chakudya choola.

Chifukwa cha kachakudyacho mwana uja anayamba kusaza ndipo anasaza limozi ndi singano uja.Adotolo ataona kuti mwanayo wasaza anati tiyamike wamisala uja popasa chakudya mwanayi.Chifukwa ndi chakudya choola chija chimene chapangisa kuti mwanayi asanze singano uja.

Apa makolo aja anasangalala kwambiri ndipo anatuluka panja kuti akamuthokoze wamisala uja koma sanamupeze anali atapita.

*PHUNZIRO:*

*Mulungu amadzera mwa anthu ena onyozekanyozeka ngati awoooo kuti chithandizo chathu chipezeke.Sibwino kuwaonera ena pansi chifukwa choti ndife okongola,achuma,ophunzila kapena otchuka.Tonsefe pamaso pa Mulungu ndiife chimodzimodzi*

*Sabata Lopambana*

🙏🙏🙏

07/08/2026

For You, Lord, are good, and ready to forgive, and abundant in mercy to all those who call upon You.
• Psalm 86:5

Prayer is the opening of the heart to God as to a friend. Not that it is necessary in order to make known to God what we are, but in order to enable us to receive Him.

We never come to a reluctant Saviour who must be persuaded to help us. We come to One who invites us, understands us, and delights to answer.

Goodmorning🙏

28/07/2026

Good morning
Ps 91:1-2 "Whoever goes to the LORD for safety, whoever remains under the protection of the Almighty can say to him, "You are my defender and protector. You are my God, in you I trust."

Amen

Have a wonderful day

26/07/2026

Whoever brings blessing will be enriched, and one who waters will himself be watered.
• Proverbs 11:25

The spirit of unselfish labour for others gives depth, stability, and Christlike loveliness to the character and brings peace and happiness to its possessor. The aspirations are elevated. There is no room for sloth or selfishness... Those who thus devote themselves to unselfish effort for the good of others are most surely working out their own salvation.
Unselfish labour isn’t just about helping people. It’s about becoming more like Jesus in the process.
Good morning

19/07/2026

Good morning
Prov 3:25-26 "You will not have to worry about sudden disasters such as come on the wicked like a storm. The LORD will keep you safe. He will not let you fall into a trap."

The LORD looks out for us🙏

Have a wonderful day

HAPPY SABBATH
11/07/2026

HAPPY SABBATH

Happy Sabbath
20/06/2026

Happy Sabbath

Meet some of the members of Saved By Grace Ministries.
17/06/2026

Meet some of the members of Saved By Grace Ministries.

@
26/05/2026

@

Address

P O BOX 695 ZOMBA
Zomba

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Saved By Grace Ministries MW posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Shortcuts

Share