01/06/2026
*ZOTSATIRA ZA KUSANKHA YEHOVA KUKHALA LINGA LAKO ππ½ππ½ππ½πͺπΌπͺπΌπͺπΌππ½ππ½ππ½*
Masalimo : 91 : 2-9. Ndidzanena za Yehova, βIye ndiye pothawira panga ndi linga langa, Mulungu wanga amene ndimadalira.β 7. Anthu 1,000 atha kufa pambali pako, anthu 10,000 kudzanja lako lamanja, koma zoopsazo sizidzafika pafupi ndi iwe.9. Pakuti wasankha Wammwambamwamba kukhala malo ako okhalamo; wavomera Yehova kukhala kothawira kwako.
*Hallelujah ππ½ππ½ππ½ππ½!!Nthaw zonse anthufe timavutika,kuphedwa kuzuzika kmaso nyengo zowawa osatha cifukwa ca cisankho cathu,Nthaw ina ake mukaona kt anthu amene amalimbana ndi Davide ambiri a iwo amakhulupirira ziwanda kapena kt mafano,and muona kt anthu onsewa akafika pamaso pa Davide amagonjetsedwa,Davide amapambana nkhondo zambiri cifukwa anaika Mulungu patsogolo ndikudalira Iye nthaw zonse,Ndipo Davide waona mitundu ambiri a anthu akufa ku nkhondo,Ena mbali iyi,enaso mbali inayi kmaso nkhondo irionse amapambana,Izi cinali chifukwa cosankha Yehova kukhala pasogolo pake ππ½ππ½ππ½ππ½ππ½ππ½ππ½ππ½ππ½*