Mvunguti CCAP Nkhoma Synod

Mvunguti CCAP Nkhoma Synod The core point is to reach out to people's lives with the Gospel of God ��

24/05/2026
24/05/2026

KUPITILIZA CHITSITSIMUTSO PA 24/05/2026

OTUMIKIRA KACHIWIRI:REV JK MNTHINDA

STAY BLESSED

24/05/2026

TAKULANDILANI KU CHITSITSIMUTSO

OTUMIKIRA :REV JK MNTHINDA & MRS M THOMSON

STAY BLESSED

17/05/2026

TAKULANDIRANI LERO PA 17TH MAY, 2026 CHIPEMBEDZO CHA LERO.

BY OUR REV. JK MTHINDA PHIRI.

Aroma 12:2"Musafanizidwenso ndi makhalidwe a dziko lino koma musandulike pokonzanso maganizo anu. Ndipo mudzadziwa ndi k...
16/05/2026

Aroma 12:2
"Musafanizidwenso ndi makhalidwe a dziko lino koma musandulike pokonzanso maganizo anu. Ndipo mudzadziwa ndi kuzindikira chifuniro chabwino cha Mulungu chomwe ndi chokondweretsa ndi changwiro."

Pamene Yesu anasandulika maonekedwe, maonekedwe ake ndi zonse za iye zinasintha. Kusandulika sikuli kwa thupi lokha, komanso ndi kwa mzimu. Titha kukhala ndi mwayi wolowa m'Ufumu wa Mulungu tikamasandulika. Timachoka pokhala akapolo n’kumatchedwa ana komanso mabwenzi a Mulungu. Osatinso atumiki, koma mabwenzi, odziwa ntchito ya Atate ndikukhala ndi zonse zimene amatiphunzitsa.

Pachifukwa chimenechi pemphelo lathu likhale motele
"Atate Athu Akumwamba, chonde mundisinthe ndi kundipatsanso mtima watsopano. Ndithandizeni kuti ndisatengere makhalidwe a dziko lino, koma m'malo mwake ndiumbikenso ndi Mawu Anu. Ndilengereni mtima woyera, ndipo musandulike moyo wanga ndi zonse zimene zimandikhudza. Ndikukhulupirirani Inu, Ambuye. M'dzina la Yesu, Ameni."

08/05/2026

08/05/2026
DAY 5
Welcome to today's Block Teaching with REV. T.A.D. Juma Phiri
Live from MVUNGUTI Mvunguti CCAP Nkhoma Synod See less

07/05/2026

07/05/2026
DAY 4
Welcome to today's Block Teaching with REV. T.A.D. Juma Phiri
Live from MVUNGUTI Mvunguti CCAP Nkhoma Synod

05/05/2026

05/05/2026
Welcome to Block Teaching with Rev T.A.D Juma Phiri

04/05/2026

04/05/2026
DAY 1
Welcome to today's Block Teaching with REV. T.A.D. Juma Phiri
Live from MVUNGUTI CCAP

28/04/2026

Uku kunali ku overnight ku Chitimbe CCAP, pamene Chigwirizano cha mtsogolo chapa Mvunguti chimavina ndi ntima onse😇

26/04/2026

TAKULANDIRANI KU CHIPEMBEDZO CHA LERO PA 26 APRIL,2026.

OTUMIKIRA. : REV J.K MTHINDA


Address

Chinsapo, Chimphangu
Lilongwe
±265

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Mvunguti CCAP Nkhoma Synod posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share