Congress Church

Congress Church Mbewe wa Dzalanyama ndi liwu la Isaiah Emmanuel Sunganimoyo yemwe amayankhula pa nkhani za ndale, zipembedzo, uzimu, chikhalidwe ndi mbiri ya anthu.

08/05/2026

Mlandu omwe andimangitsira a Sosola ndi a Kaomba ndi umenewo. Ku Khothi next week..

Andimanga pa mlandu omwe a Sosola ndi Team ya anadzasuma. Ndinapempha a Police kuti nkhani ipite pa court, kuti Bwalo li...
08/05/2026

Andimanga pa mlandu omwe a Sosola ndi Team ya anadzasuma. Ndinapempha a Police kuti nkhani ipite pa court, kuti Bwalo likamvetsere mlandu omwe ndachimwa.

08/05/2026
07/05/2026

Kalonga Sosola 9, ngakhale akasuma ku Polisi komabe akumutukwana Isaiah Emmanuel Singanimoyo. Mvetselani kutukwana kwake kochokera mkamwa mwa Mfumu.

Press Release from the Office the 6th President of the Republic of Malawi His Excellency Dr. Lazarus M. Chakwera.
07/05/2026

Press Release from the Office the 6th President of the Republic of Malawi His Excellency Dr. Lazarus M. Chakwera.

06/05/2026

Ma Shop akulu akulu ndi otsekedwa mmizinda yonse ya dziko lino. Ndipo anthu mu MZINDA WA MZUZU akupanga zionetsero lero pa 6 May 2026.

06/05/2026

Musalowetse ndale pa maphunziro, za umoyo ndi za ulimi. Mukupha dziko.

Zikumveka kuti mu MZINDA WA Lilongwe, masiku ena akuletsedwa kukhazikitsa Boarding za ophunzira a Standard 8 pomwe akukonzekera mayeso.

03/05/2026

Fellow Malawians and International Community,

We here today with heavy hearts, for our nation has witnessed acts that shame our values and betray our Constitution. The Mayor of Blantyre City has assaulted women, humiliated a pregnant mother, and stood before us with arrogance, declaring he will never apologize. This is not leadership. This is abuse of power.

Let us be clear: Malawi is a secular state. Our Constitution protects every citizen—Christian, Muslim, Hindu, traditionalist, and non-believer alike. No one has the right to impose laws outside of it. Mob justice is not justice. It is lawlessness. It is cruelty. And it has no place in our democracy.

Mob justice is nothing more than violence dressed up as order. It bypasses the courts, it denies due process, and it strips away human dignity. Our Constitution does not recognize it. Our government ethics reject it. And our people must never allow it to take root among us.

The Mayor has no excuse. He must resign. But resignation is not enough. He must be arrested. He must be charged. He must face the courts of Malawi, just as any citizen would. The Malawi Police Service has the mandate and the responsibility to act. We call upon them to fulfill their duty.

Let us remind ourselves: Malawi belongs to all of us. Our diversity is our strength. Our Constitution is our shield. And our justice system is the path to peace. We will not allow mob justice to replace the rule of law. We will not allow arrogance to replace accountability. And we will not allow violence to replace dignity.

Malawi is not an Islamic State. Malawi is not a Christian State. Malawi is not a state of any single religion. Malawi is a nation of laws, a nation of rights, and a nation of people united in their humanity.

So let us stand together. Let us demand justice. Let us protect our Constitution. And let us say, with one voice: No leader is above the law. No citizen is beneath its protection.

02/05/2026

Kudzudzula a Jomo Osman, MEYA WA MZINDA WA BLANTYRE, chifukwa chomenya mzimayi.

01/05/2026

Kodi Dr. Lazarus Chakwera ndi woyenera kutchedwa MWANA WA MULUNGU? Kodi MWANA WA MULUNGU NDI NDANI?

Address

P. O. Box 20131, Kawale
Lilongwe
265

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Congress Church posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share