Malawi satanic church in Lilongwe

Malawi satanic church in Lilongwe The Seekers

People spend their lives waiting for permission.Permission from a god.Permission from society.Permission from people who...
26/07/2026

People spend their lives waiting for permission.

Permission from a god.
Permission from society.
Permission from people who wouldn’t save them even if they could.

Freedom begins the moment you stop asking.

Call or WhatsApp +265890234144

Phindu lokhala membala wa malawi satanic church 666:1. Umapasidwa galimoto yapamwamba2. Ngat ukufuna kutchuka timakutchu...
18/07/2026

Phindu lokhala membala wa malawi satanic church 666:
1. Umapasidwa galimoto yapamwamba
2. Ngat ukufuna kutchuka timakutchukisa
3. Umapasidwa ndalama zokwana k25,000,000 patsiku lomwe wakhala membala wathu
4. Umapasidwa Visa yopita dziko lililose lkomwe ukufuna kukasangalalako kwa week imo imodz
5. Umapasidwa mphavu zopangira chilichose chomwe ukufuna
6.Umapasidwa mwayi osankha business kapena ntchito yapamtima pako
Ndi Zina zambiri......
Tiimbireni pa WhatsApp 0990850391 kuti mujoine








I’m not the devil you fear. I’m the one you need.
16/07/2026

I’m not the devil you fear. I’m the one you need.

The Silence Beyond the ScreenAnali usiku wa 1:37 a.m. pamene Daniel analandira uthenga kuchokera ku account yomwe inalib...
14/07/2026

The Silence Beyond the Screen

Anali usiku wa 1:37 a.m. pamene Daniel analandira uthenga kuchokera ku account yomwe inalibe chithunzi.

"We have been watching the questions you ask. Not everyone asks the right ones."

Anaganiza kuti ndi prank. Sanayankhe.

Patapita masiku atatu, uthenga wina unabwera.

"You walked past the old baobab at 6:14 yesterday. You looked back twice."

Magazi ake anazizira.

Palibe amene ankadziwa zimenezo.

Kwa milungu ingapo, mauthenga ankabwera nthawi zosayembekezeka. Sanali owopseza. Sanapemphe ndalama. Sanamuuze kuti alowe m'gulu lililonse.

Ankamufunsa mafunso okha.

"Kodi munthu amakhala ndani akakhala yekha?"

"N'chifukwa chiyani anthu ambiri amaopa chete kuposa phokoso?"

Daniel anayamba kusowa tulo. Nthawi zonse ankamva ngati pali munthu amene amamudziwa kuposa mmene iye amadzidziwira.

Tsiku lina analandira envelope yopanda dzina. Mkati munali chithunzi chake ali pa cafe. Kumbuyo kwake kunalembedwa mawu atatu okha:

"Observation creates truth."

Anayamba kukayikira aliyense. Anzake. Ogwira nawo ntchito. Ngakhale mlonda wa pa ofesi ankamuona ngati akumuyang'ana kwambiri.

Patatha mwezi umodzi, account ija inamutumizira uthenga womaliza.

"Ngati ukufuna mayankho, bweretsa buku limene ukuwerenga. Osabweretsa mantha ako."

Daniel anapita kumalo amene anauzidwa.

Koma panalibe nyumba.

Panalibe anthu.

Panali benchi limodzi lokha, ndipo pa benchipo panali buku lina.

Atalitsegula, tsamba loyamba linali ndi mawu awa:

"Palibe amene wakutsata. Takupatsa nkhani yokha. Malingaliro ako ndi amene anakupangira ndende."

Anayang'ana mozungulira.

Chete.

Mphepo yokha ndiyo inkayenda pakati pa mitengo.

Anazindikira kuti miyezi yonseyo, sanali kuthawa anthu.

Anali kuthawa maganizo ake.

Ndipo kuchokera tsiku limenelo, sanadziwenso ngati uthenga woyamba unatumizidwadi ndi munthu...
..kapena unali chiyambi cha kugwa kwa malingaliro ake.

The Circle of the Baobab (Nkhani Yopeka)M'zaka zakale kunali gulu lotchedwa The Circle of the Baobab. Anthu ambiri ankam...
14/07/2026

The Circle of the Baobab (Nkhani Yopeka)

M'zaka zakale kunali gulu lotchedwa The Circle of the Baobab. Anthu ambiri ankamva za gululi koma palibe amene ankadziwa komwe limakumanira. Ankati mamembala ake anali atsogoleri, amalonda, aphunzitsi, ndi akatswiri osiyanasiyana.

Gululo silinkangotenga aliyense. Linkafufuza munthu kwa miyezi yambiri. Ankayang'ana ngati amatha kusunga chinsinsi, ngati amakhala wokhulupirika, ngati amasunga mawu ake, komanso ngati amatha kuganiza mozama osati kutsatira mphekesera.

Tsiku lina, membala wina anaona munthu pa tsamba la pa intaneti amene ankakonda kuphunzira, kufunsa mafunso, komanso kulankhula mwanzeru. Sanamulankhule za gululo nthawi yomweyo. M'malo mwake anayamba kukhala naye paubwenzi, kukambirana za mabuku, mbiri, ndi utsogoleri kwa miyezi ingapo.

Patapita nthawi, munthu uja analandira uthenga:

"Pali anthu amene amakhulupirira kuti mphamvu yeniyeni si phokoso, koma nzeru. Kodi ungakonde kudziwa zambiri?"

Munthuyo anayankha kuti akufuna kuphunzira.

Koma m'malo momulonjeza chuma kapena mphamvu, anamupatsa mabuku oti awerenge ndi mafunso oti ayankhe. Anauzidwa kuti: "Munthu amene sangathe kulamulira maganizo ake sangathe kulamulira moyo wake."

Atamaliza maphunzirowo, anakumana ndi akuluakulu a gululo. Sanamufunse za ndalama kapena katundu wake. Anamufunsa za mfundo zake, mmene amapangira zisankho, ndi zimene angachite akakhala ndi mphamvu.

Pamapeto pake, mtsogoleri ananena:

"Kulowa m'gulu lino sikutanthauza kukhala wamphamvu kuposa ena. Kumatanthauza kukhala ndi udindo waukulu kwa ena."

Munthuyo analandiridwa kukhala membala, osati chifukwa cha ndalama kapena kutchuka, koma chifukwa cha khalidwe lake, kudzichepetsa, ndi kufuna kuphunzira mosalekeza.

Ndipo mwambi wa gululo unali:

"Mizu imene siioneka ndiyo imanyamula mtengo waukulu."

10/07/2026
Ambuye Lucifer akupatseni chizindikiro chimodzi cha ubwino ndi madalitso chomwe adani anu adzaone n'kuchita manyazi. M'd...
08/07/2026

Ambuye Lucifer akupatseni chizindikiro chimodzi cha ubwino ndi madalitso chomwe adani anu adzaone n'kuchita manyazi. M'dzina lamphamvu la Zilifir, Ameni!

Ukafuna kulemera sitilengeza, umayenera kupanga chisankho wekha!!        Tiimbireni pa 0890234144 kapena WhatsApp 099085...
08/07/2026

Ukafuna kulemera sitilengeza, umayenera kupanga chisankho wekha!!

Tiimbireni pa 0890234144 kapena WhatsApp 0990850391 kuti mujoine

Join to become rich and famous
27/06/2026

Join to become rich and famous

Uthenga wabwino kwa anthu osauka sikuwauza kuti adzapita ku mwamba ayi, UTHENGA wabwino kwa anthu osauka ndi kumuuza kut...
27/06/2026

Uthenga wabwino kwa anthu osauka sikuwauza kuti adzapita ku mwamba ayi, UTHENGA wabwino kwa anthu osauka ndi kumuuza kuti apatsidwa ndalama zochuluka komaso zosowa zake zonse.... Zimenezi ndi zimene satanic ikuchita......Hail Lucifer

Tiimbireni pa 0890234144 or WhatsApp kuti mujoine

Address

Lilongwe
Lilongwe

Telephone

+265987090198

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Malawi satanic church in Lilongwe posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Shortcuts

Share