Kasungu Bible Believers Mtambalala Tabernacle

Kasungu Bible Believers Mtambalala Tabernacle PSALMS 71:18 NOW that Iam old and gray headed forsake me NOT O LORD....

24/07/2026

James 4:17 (KJV)
"Therefore to him that knoweth to do good, and doeth it not, to him it is sin."

19/07/2026

Sunday Service 17/05/202610:00AM TO 12:00 pm

18/07/2026

⌚4:47 min

Pastor Paddington Ngwira

Kuchitila Umboni Za Ubatizo Wolondola ,Wa Mdzina La Ambuye Yesu Khristu, Panyumba Zinazake

:38

15/07/2026

⌚4:33 min

Pastor Paddington Ngwira

14/07/2026

⌚2:58 min

Pastor Martin Mkandawire



NGATI MUFUNA MUZAPITE UFUMU WAKUMWAMBA MUKUYENERA MULANDILE UBATIZO WA MZIMU WOYERA. ( _This is A Must_ )

Kuti Mulandile Ubatizo Wa Mzimu Woyera Muyenela Mulape Mosweka Mtima ( Osasiyako Ntchimo losalapidwa) , Mukatelo Mubatizidwe Mdzina La Ambuye Yesu Khristu Kuloza Kuchikhululukiro Chama Chimo Anu, Ndipo Muzalandila Mphatso Ya Mzimu Woyera.

Zichitike monga Zinaliri Matsiku Aah Atumwi, Pomwe Anthu ankawabatiza Mdzina La Ambuye Yesu Khristu. Osati Kunena kuti tikukubatiza iwe Mdzina la Atate Mwana Mzimu Woyera monga Mipingo ichitila lero, Osatchula dzina ,zimenezo Ayi . Satilani Momwe Ubatizo Ulili Monga Mwa Malemba,Kutengela ndi Vumbulutso lomwe linadza Patsiku La Pentecost, Muka Mabatizidwa Mdzina La Ambuye Yesu Khristu,Mubatizidwe Madzi Ambiri monga Zinaliri nthawi Ya Aah Atumwi,komanso Yesu Iye mwini Anapita Ku Madzi Ambiri.

MUKATELO Musanjikidwe manja ndi Atumiki Alindi Mzimu Woyera,kuti Akupempheleleni Kuti Mulandile Ubatizo Wa Mzimu Woyera ,Musate Dongosolo lonse loyenela lanenedwa Apa Mulandila Ubatizo Wa Mzimu Woyera.

Inuyo Ndindani Kuti Musamvele ??? Ndi Zoona kuti Atumwi ankabatiza m’dzina la Yesu Khristu ,ndipo ankabatiza Ubatizo omiza m’madzi ambiri, monga pa Machitidwe 10:48, 19:5. Kenako anasanjikidwa manja ndi atumiki odzazidwa ndi Mzimu Woyera kuti alandire Mzimu Woyera.

Dongosolo limeneli silinasinthe. Mipingo yambiri lero yasintha chiphunzitsocho, koma Mau a Mulungu akadali omwewo.

M’buku la Machitidwe 2:38.

Petro anati
- Lapani – tembenukani ku machimo anu
- Mubatizidwe m’dzina la Ambuye Yesu Khristu – kuloza ku chikhululukiro cha machimo
- Mudzalandira mphatso ya Mzimu Woyera

NDE PALI ENA AMATI NDINA BATIZIDWA KALE
- Muwelenge Machitidwe 19:1-6 , Pamenepo Anthu Ata Zindikila kuti Sanabatizidwe Ndi Mzimu Woyera Anabatizidwanso Kenaka Kulandila Ubatizo Wa Mzimu Woyera Uja.

Malemba Awonjezera Awubatizo

Maliko 16:16
Yohane 3:5
Yohane 3:23
Efeso 4:5

Ambuye Akudalitseni Pamene Mukuchita chimenechi

14/07/2026

⌚4:03 min

Pastor Paddington Ngwira

14/07/2026

⌚3:03 min

Pastor Paddington Ngwira

12/07/2026

Mulungu Azalanga Onse Akukana Kulowa Muimfa Ya Ambuye Yesu Khristu (Kufa, Kuyikidwa ndi Wukisidwa Naye Mmanda)

08/07/2026

⌚8:58 min

Pastor Paddington Ngwira

Address

Kasungu
Kasungu

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Kasungu Bible Believers Mtambalala Tabernacle posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Shortcuts

Share