CCAP-Capso on the Move in Spreading Gods Words

CCAP-Capso on the Move in Spreading Gods Words let's fight the good fight of faith ...let's let the love of the Christ lead us

We are here to provide and lead the way of the truth and care in the arms of the father Jesus Christ

11/11/2025

mwaswera bwanji kumeneko lero?

04/01/2025

werengani Levitiko 18:5-20, 22-24

Choncho sungani malangizo ndi malamulo anga, popeza munthu amene amvera zimenezi adzakhala ndi moyo. Ine ndine Yehova. “ ‘Munthu aliyense asagonane ndi wachibale wake. Ine ndine Yehova. “ ‘Usachititse manyazi abambo ako pogonana ndi amayi ako. Iwo ndi amayi ako. Usagonane nawo. “ ‘Usagonane ndi mkazi wa abambo ako (osakhala amayi okubala). Ukatero ukuchititsa manyazi abambo ako. “ ‘Usagonane ndi mlongo wako, mwana wamkazi wa abambo ako, kapena mwana wamkazi wa amayi ako, kaya anabadwira mʼnyumba mwanu kapena kwina. “ ‘Usagonane ndi mdzukulu wako: mwana wa mwana wako wamwamuna kapena mwana wa mwana wako wamkazi. Kutero nʼkudzichotsa ulemu. “ ‘Usagonane ndi mwana wamkazi wa mkazi wa abambo ako, amene abambo akowo anabereka; popeza ameneyo ndi mlongo wako. “ ‘Usagonane ndi mlongo wa abambo ako; popeza ameneyo ndi thupi limodzi ndi abambo ako. “ ‘Usagonane ndi mchemwali wa amayi ako chifukwa ameneyo ndi thupi limodzi ndi amayi ako. “ ‘Usachititse manyazi mchimwene wa abambo ako pogonana ndi mkazi wake popeza amenewo ndi azakhali ako. “ ‘Usagonane ndi mpongozi wako popeza ameneyo ndi mkazi wa mwana wako. Choncho usamuchititse manyazi. “ ‘Usagonane ndi mkazi wa mchimwene wako popeza potero ukuchititsa manyazi mʼbale wakoyo. “ ‘Usagonane ndi mkazi ndiponso mwana wake wamkazi. Usagonane ndi mwana wamkazi wa mwana wake wamwamuna, kapena mwana wamkazi wa mwana wake wamkazi. Amenewo ndi thupi limodzi ndi mkaziyo. Kutero ndikuchita chinthu choyipa kwambiri. “ ‘Usakwatire mchemwali wa mkazi wako ndi kumagonana naye mkazi wakoyo ali moyo ngati wopikisana naye. “ ‘Usamuyandikire mkazi k*ti ugonane naye pa nthawi yake yosamba. “ ‘Usagonane ndi mkazi wa mnzako ndi kudziyipitsa naye. “ ‘Usagonane ndi mwamuna ngati mkazi; chimenecho ndi chinthu chonyansa. “ ‘Usagonane ndi nyama ndi kudziyipitsa nayo. Mkazi asadzipereke kwa nyama k*ti agonane nayo. Chimenecho ndi chisokonezo. “ ‘Musadzidetse ndi zinthu zimenezi chifukwa umo ndi mmene mitundu ina imene

04/01/2025

Mwachilowa bwanji chakachi anthu amulungu???

 Ku Chiradzulu, anthu makumi awiri ndi m'modzi avulala pa ngozi ya pa nseu, Minibasi yomwe anakwera itagubuduzika pa mal...
13/09/2024



Ku Chiradzulu, anthu makumi awiri ndi m'modzi avulala pa ngozi ya pa nseu, Minibasi yomwe anakwera itagubuduzika pa malo otchedwa Satari m'bomali.

Ofalitsa nkhani za apolisi m’bomali a Cosmas Kagulo wauza Zodiak Online lero k*ti izi zachitika pomwe dalaivala wa Minibasiyi, a Isaac Makwinja a zaka 32 zakubadwa amafuna kupitilira galimoto ina pa malowa.

Malinga ndi a Kagulo, chifukwa chothamanga kwambiri,dalaivala wa minibasiyo yomwe imalowera mtauni ya Limbe mu nzinda wa Blantyre analephera kuongolera bwino zomwe zinachititsa k*ti igubuduzike mbali ina ya nseu komwe inakawombanso mtengo.

Iwo ati mwa ovulalawa omwe awiri mwa iwo ndi ana athamangila nawo ku chipatala cha ching'ono cha Nkando pomwe ena ali ku chipatala cha Mulanje komwe a Kulandira thandizo.

28/08/2024

Heloo good morning
OSAIWALA kupemphera NGOZI ndie zikuchuluka pa Malawi pano

12/08/2024

Heloo mwaswera bwanji lero?? lunch inali bwa???

10/03/2024

KDI SATANA AKULAMULIRA???
Mwambo wamapemphero unasokonekera pa mpingo wa katolika wa Mipande ku Lunzu ku Blantyre pamene wansembe anamenya mtsogoleri gulu loyimba nyimbo.

Malingana ndi mtsogoleri wa gululi Issac Edward yemweso ndi wapampando wa pa mpingowo, izi zinachitika kamba koti mmodzi mwa oyimba anayambitsa nyimbo yomwe siyoyenera kuimbidwa pomwe mpingowu ukukumbuka masautso a Yesu.

Edward wauza MIJ Online wansembeyu anawafunsa k*ti "Mutchula bwanji k*ti Aleluya mu nyimbo nyengo ino ya masautso a Yesu?. Ndipo nthawi yomweyo anandimenya mbama koma sindinabwezere," watero Edward polankhula ndi MIJ Online.

Iye wati wansembeyu atangomaliza kumenya mkuluyo anakakwera galimoto yake mkumapita.

Padakali pano, mmodzi mwa opemphera pa mpingowu omwe anali mu tchalitchimu pa nthawiyi Siza Felix watiuza k*ti mapemphero athera panjira ndipo anthu akubalalika

16/12/2023

Morning Good people

 let's be in the shoes ya anthu omwe anamwalira they're in Hades waiting for a judgement day....Do you know that those g...
13/12/2023



let's be in the shoes ya anthu omwe anamwalira they're in Hades waiting for a judgement day....

Do you know that those guys amafunitsitsa atangopasidwa 1 minute kubwera padziko la pansi adzalape ,

Inuyo you're alive koma mukungochimwa , kuyenda ndi azibambo, kusokoneza mabanja a eni zibwezi Zambiri mbiri, kupusisa anthu in the name of prophet yet you're fake, kuminula

You think you're alive k*t inuyo ndi opambana? Or it's normal k*t basi muyenera kukhala moyo? Have you ever asked yourself why you're still alive??

Mulungu akukupasani mwai k*ti mwina muzindikira mulape,koma akangoti enough basitu kwanu kwantha?

One thing you have to know,every second yadutsa umakhala wachosera nthawi yako yokhala padziko lapansi, apapa mukuchotsera nthawi yanu

Enanu mumwalira simulowa chaka chamawa apa,enanu mumwalira next year koma simukuziwa you're there busy uchimo

Anzanu Ali nchipatala uko kuphupha ndi imfa kufuna atamuziwa yesu before Kumwalira and you're there playing with lives ...

Repent , repent ,repent kumanda kulibe kulapa,once wasiya kupuma basi.....Acts:2.38
Peter replied, "Repent and be baptized, every one of you, in the name of Jesus Christ for the forgiveness of your sins. And you will receive the gift of the Holy Spirit.

Address

Blantyre

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when CCAP-Capso on the Move in Spreading Gods Words posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share