21/05/2026
Today its thursday, Ndimafuna ndilankhule ndi iweyo, uthengawu ndiwako koma pokupasa ulemu sindinafune kukutchula Dzina lako, umalimbikira, ndiwe wa khama, ndipo khalidwe uli nalo , ntchito umathanso kupemphera nde umapemphera, achibalenso nde uli nawo komano, moyo wako ukamphera nde ngati siukupemphera chitonzo chosatha, kupekeredwa nkhani, kuiwalidwa, amuna kukupanga chipongwe, kuyamba business kuduka, ubwenzi kuyamba kutha basi just like that pano moyo wako ukuwawa ndipo you feel like ungozisiya chifukwa watopa,
Tamvetsera, kumwamba kuli mulungu, akuziwa, akuona komanso akumva mapemphero ako, komano zikungosowekera mulungu akulumikizitse ndi mtumiki wa mulungu amene wanyamula yankho lako, mamasulidwe ako komanso chisomo chako.
DONT GIVE UP SOON UGONJETSA MU DZINA LA YESU CHRISTU.
Shalom
Minister Gracious