Victory Outreach Ministry

Victory Outreach Ministry Victory Outreach Ministry
"The Home of Freedom"
Registered & Founded by ~ Prophet Gracious Wasibu

Today its thursday, Ndimafuna ndilankhule ndi iweyo, uthengawu ndiwako koma pokupasa ulemu sindinafune kukutchula Dzina ...
21/05/2026

Today its thursday, Ndimafuna ndilankhule ndi iweyo, uthengawu ndiwako koma pokupasa ulemu sindinafune kukutchula Dzina lako, umalimbikira, ndiwe wa khama, ndipo khalidwe uli nalo , ntchito umathanso kupemphera nde umapemphera, achibalenso nde uli nawo komano, moyo wako ukamphera nde ngati siukupemphera chitonzo chosatha, kupekeredwa nkhani, kuiwalidwa, amuna kukupanga chipongwe, kuyamba business kuduka, ubwenzi kuyamba kutha basi just like that pano moyo wako ukuwawa ndipo you feel like ungozisiya chifukwa watopa,

Tamvetsera, kumwamba kuli mulungu, akuziwa, akuona komanso akumva mapemphero ako, komano zikungosowekera mulungu akulumikizitse ndi mtumiki wa mulungu amene wanyamula yankho lako, mamasulidwe ako komanso chisomo chako.
DONT GIVE UP SOON UGONJETSA MU DZINA LA YESU CHRISTU.

Shalom
Minister Gracious

21/05/2026

They don’t like you because they can’t control and manipulate you. So, they make up false stories and recruit people to hate you with them.

When they dislike you for no reason, they are left with bitterness because they can't change God's Destiny and plan for you.

May The Good Lord Fight all your battle and expose all your enemies in Jesus name.

With love and Respect,
Minister Gracious.

Every marriage experiences disappointment because imperfect people marry imperfect people. Always choose grace and recon...
13/05/2026

Every marriage experiences disappointment because imperfect people marry imperfect people. Always choose grace and reconciliation instead of pride, bitterness and condemnation.

Marriage grows strong when you value the person more than being right. Let grace cover the small offenses, and choose reconciliation over keeping score. In the end, love that forgives quickly builds a home that lasts.

New wisdom, New insights & Changed mindset.

Yours Sincerely,
CA Prophet Gracious Wasibu

Ndalama/Chuma zimakuitanira akazi onyenga padziko lapansi.  Umphawi umakuonetsa mkazi mmodzi amene amakukonda ndithu. ❤️...
19/04/2026

Ndalama/Chuma zimakuitanira akazi onyenga padziko lapansi.
Umphawi umakuonetsa mkazi mmodzi amene amakukonda ndithu. ❤️

Koma cholinga si kukhala osauka kuti akazi akukonde, kapena kukhala olemera kuti akazi akunyenge.
Gwirani ntchito molimbika, pempherani kwa Ambuye Mulungu kuti akupatseni ndalama _ndi_ nzeru — kuti mukhale odalirika kwa mkazi wanu.

Chifukwa umphawi umatukwanitsa... koma chuma popanda khalidwe chimaononga nyumba.

With Love,
Prophet Gee

13/04/2026
13/04/2026

Nothing else but the truth

13/04/2026

Back then

Is your life passing through shame, disgrace, disappointments and strange dreams of which you are tired of that mess? Do...
21/12/2025

Is your life passing through shame, disgrace, disappointments and strange dreams of which you are tired of that mess? Don't worry and don't worst your time complaining, Come to Jesus and trust him unconditionally he will surely meet you and fix your life...

As you are about you are remaining with 10 days only to finish the year 2025, May the game changer the mighty father God give you the good news that will make your enemies and haters shut-up their
month in Jesus name. Your friend and the fellow follower and believer is happy and thankful to the lord for what God has started doing in their lives.

Shalom
Gracious Wasibu

Apart from the Breakthrough, happy and celebration  Moments in life, Sometimes we need hard days to know who is family, ...
17/12/2025

Apart from the Breakthrough, happy and celebration Moments in life, Sometimes we need hard days to know who is family, who is a friend, who is a partner or a monitoring spirits, and who is a passenger in our lives.

That's why it is really good and you need to be thankful when you are passing through hard times and other uncertain predicuments

NKJV, 1 Thessalonians 5:18
18.In everything give thanks; for this is the will of God in Christ Jesus for you

Ena aja simuwadziwe khalidwe lawo until When something happen

Ndikweze volume?

Shalom
Gracious Wasibu

Pamene tikudutsa munyengo ya Christmas ndi chisangalalo, ndikulengeza chitetezo pa ana anga. Palibe aliyense mwa iwo ame...
09/12/2025

Pamene tikudutsa munyengo ya Christmas ndi chisangalalo, ndikulengeza chitetezo pa ana anga. Palibe aliyense mwa iwo amene alodzedwe. Palibe achite ngozi kapena kubeledwa. Palibe imfa.

𝗦𝘂𝗹𝗼𝗱𝘇𝗲𝗱𝘄𝗮, 𝘀𝘂𝗰𝗵𝗶𝘁𝗮 𝗻𝗴𝗼𝘇𝗶, 𝘀𝘂𝘁𝗮𝘆𝗮 𝗺𝗼𝘆𝗼 𝘄𝗮𝗸𝗼 𝗸𝗮𝗽𝗲𝗻𝗮 𝘄𝗮 𝘄𝗮𝗰𝗵𝗶𝗯𝗮𝗹𝗲 𝗮𝗹𝗶𝘆𝗲𝗻𝘀𝗲. 𝗔𝘁𝗲𝗹𝗼 𝗬𝗲𝗵𝗼𝘃𝗮𝗵 𝗠𝘂𝗹𝘂𝗻𝗴𝘂 𝘄𝗮𝗸𝗼. Masalimo 91:10 akhala gawo lako.
_________________________________
As we go through the festive season, no evil shall befall my children. No death. No accidents. No loss. Psalm 91:10 will be your portion.

Shalom

Address

Blantyre

Telephone

+265881255824

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Victory Outreach Ministry posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share