14/05/2024
Romans 8:35
Adzatisiyanitsa ndani ndi cikondi ca Kristu? nsautso kodi, kapena kupsinjika mtima, kapena kuzunza, kapena njala, kapena usiwa, kapena zoopsya kapena lupanga kodi?
Kuzipeleka kwathu kwa Mulungu palibe chomwe chingatilekanise
Palibe chomwe chingatilekanise ndi chikondi cha Mulungu
Akhristu ena amasiya kupephera chifukwa cha zopyinja zomwe akukumana nazo.
Ena amafika ponyoza Mulungu kuti Sakuva kulira kwawo, sakuona nyengo zawo zomwe akukumana nazo.
Paulo akulimbikisa mpingo wa ku Aroma kuti palibe nyengo yomwe ingatipangise kusiya kupephera, kulambira Mulungu kutumikira Mulungu.
Munyengo zonse Mulungu amakhala nafe. Mulungu amava kulira kwathu Amaona nyengo zathu ndipo muthawi yake yoikika azayankha. STAY BLESSED
By Apostle J Adams Phiri
088 280 6598