Katekisim WA CCAP Blantyre Synod

Katekisim WA CCAP Blantyre Synod The Lord is my shepherd i shall not want

30/08/2022

Go therefore and make disciples of all nations, baptizing them in the name of the Father and of the Son and of the Holy Spirit. ' Teaching them to observe all that I have commanded you . And behold , Iam with you always, to the end of the age"(MATHEW 28 V 19 _ 20)

30/07/2022

Olengedwa ndi Mulungu amulemekeze

Masalmo 100

13/11/2021

Fuulirani kwa Yehova inu dziko lonse lapansi
Tumikirani Yehova ndi Chikondwelero idzani pamaso pake ndikumuimbira mokondwera
Dziwani kuti Yehova ndiye Mulungu iyeyu anatilenga
Ndife anthu ake ndi nkhosa zapa busa pake
Mlemekezeni lilemekezeni dzina lake
Pakuti Yehova ndiye wabwino
Chifundo chake chimanka muyaya ndi chikhulupiliro chake ku mibadwomibadwo

16/10/2021

Tomorrow is Sunday again
Mukapemphera kuti

'tmisschurchservice!!

11/08/2019
29/03/2019

KUSALA KUDYA
Mawu oyamba
Phunziro la kusala kudya ndi lachilendo kwa akhristu ambiri. Chifukwa mawu akuti kusala amalumikizana kwambiri ndi zipembedzo zina osati chachikhristu. Muphunzilori tifuna kufotokozerana za kusala kudya koyenera ndi kosayenera pa chipembedzo chachikhristi.

KODI KUSALA KUDYA NDI KUTANI
Kusala kudya ndi kukhala osadya ndi osamwa kathu kwa masiku angapo. Ayuda ankasala kudya kawiri kawiri pa zifukwa zosiyanasiyana monga:
1. Kukonzekera chipembedzo
2. Chifukwa cha mavito, maliro , nkhondo
3. Kuonetsa kugonja pamaso pa Mulungu ndi zina zambiri. (2 Samuel 12:16, Genesis 50:10, Exsodo 34:28)

Address

Balaka
Balaka

Telephone

+265995814027

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Katekisim WA CCAP Blantyre Synod posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Place Of Worship

Send a message to Katekisim WA CCAP Blantyre Synod:

Share